UTHENGA OPITA KU TONSE ALLIANCE BON KALINDO 11 July 2024

Пікірлер: 64

  • @Nelsonmatenda
    @Nelsonmatenda21 күн бұрын

    Bon kalindo akutiyankhulila anthu osawukafe we love you❤

  • @Nelsonmatenda
    @Nelsonmatenda21 күн бұрын

    Our own president kalindo you stand with poor people

  • @user-hl3xi3ok9g
    @user-hl3xi3ok9g22 күн бұрын

    Bon keep on fighting for the good of Malawians imagine ku Queens zoyezera malungo kulibe at 60years please

  • @HassanIzaya
    @HassanIzaya21 күн бұрын

    Bon kalindo amakwanila kwambili ❤❤❤

  • @Mphatsochibweya
    @Mphatsochibweya20 күн бұрын

    Since democracy came in I have never heard anything good from the people about ours leaders leaders here in malawi and Africa as a continent. The main reasons are regionalism, tribalism and favoritism. Kalindo has one or two of these effects that is why noising much .

  • @user-bq1mb4fk1b
    @user-bq1mb4fk1b22 күн бұрын

    Thank you so much Mr Bon kalindo for your information ❤❤

  • @BenMasangano
    @BenMasangano22 күн бұрын

    From njeza village T/A mabuka central Africa malawi mwana woopya kwambiri ndipo sindiopa

  • @DineMaku-p7e
    @DineMaku-p7e21 күн бұрын

    Mmakwa boss

  • @JafaliAjusa-zg2xi
    @JafaliAjusa-zg2xi22 күн бұрын

    Big up Mr kalindo

  • @DepsyNkosi-r2d
    @DepsyNkosi-r2d21 күн бұрын

    koma tu zinganizo znazitu president i hope sakuzwa ai

  • @PhillipLuhanga-e6t
    @PhillipLuhanga-e6t21 күн бұрын

    Wisely spoken

  • @dontreybanda278
    @dontreybanda27822 күн бұрын

    Powerful massage massage

  • @MapandoJoseph
    @MapandoJoseph21 күн бұрын

    Pano ndifuna ndikuyamike Bone ungoyambisa chako ife tikisata

  • @FrancissKenneth
    @FrancissKenneth21 күн бұрын

    Mumakwana bg 💪

  • @dorcasmwale6328
    @dorcasmwale632822 күн бұрын

    tikuyamikileni potitsegula mitu

  • @GloryLouis-x2l
    @GloryLouis-x2l21 күн бұрын

    Apa president wa anthu osauka wayooya eeeee

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma22 күн бұрын

    Anapha m'bale wake chifukwa chofuna kulamula Malawi mpaka 2060 akuti hehehe yomweyo chikangawa

  • @Nelsonmatenda
    @Nelsonmatenda21 күн бұрын

    Makolo ankatiuza kuti mcp ndiyoophya now pano tawonano

  • @marryphili5419
    @marryphili541921 күн бұрын

    Boma ili ndilopenga misara pompano ananena Kuti tisiye kudya nsima yoyera panopa akuti anthu asiye kuvuwura chenga pokhapokha atenge chilolezo Kodi ndarama zamisokho zachepa panopa mukufuna zamuchenga shame on you MCP

  • @frankchirwa2301
    @frankchirwa230121 күн бұрын

    Vuto ndife amalawi kupusa zinthu ziku onongeka wanthu ali mphee.

  • @MathewsBenard
    @MathewsBenard22 күн бұрын

    Adapenga uyu kuchita kunenerela kut kufuna kumangidwa ndiye tinene kut akamatuluka kupolisi amalandila ndalama eti

  • @TemboHaswell
    @TemboHaswell22 күн бұрын

    Km ineyo bone kalindoyi ineyo ndimamuda km nkhani akukambayi ndiyoona tizichita kugula Kaye kuboma nchenga 😂😂😂 kenaka kwamavenda noo this is not fair

  • @anthonynkhoma4265
    @anthonynkhoma426522 күн бұрын

    Kalondo ndi mbuzi yamunthu. Amandinyasa. Ameneyu sakudziwa kuti akubzala mbewu yachabe.

  • @user-re7fo3be2z

    @user-re7fo3be2z

    22 күн бұрын

    Iwe mutu uwumawo do you think zikutisangalasa ifeyo nkhope yonyasayo

  • @brightkaunda920

    @brightkaunda920

    22 күн бұрын

    Ngat kalindo ali mbuzi yamunthu iweyo ukhala ndani?

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf22 күн бұрын

    chakwera ndi chigawenga boma la mbava ili boma la zitsiru zokha zokha chakwera pantumbo pa make chitsiru mbava

  • @user-ty1vq9lq6w
    @user-ty1vq9lq6w22 күн бұрын

    Ayamba kulimbana ndi anthu osauka ndipo ziwanda zimenezi zalitenga dziko ngati ndi lao, zikanthidwa ndi zanja la Mulungu pompano

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v22 күн бұрын

    Agalu achabe chabe awa ndipo anthu atope naye chakwera

  • @ClementKampaka
    @ClementKampaka22 күн бұрын

    😂😂 komalizako eee sikusinja ndi gwenembe

  • @JozzyNthinda
    @JozzyNthinda21 күн бұрын

    Km aonjeza achoke mbomamo palibe akupanga km ukakwatila umadalila makolo kd

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace32122 күн бұрын

    Kell kay nanja lake lasokonekela

  • @user-sk3ld2ss7s
    @user-sk3ld2ss7s22 күн бұрын

    A Malawi, chomwe mumafuna sichidziwika, mumatangwanidwa ndi kuchitira m'sanje president ndi chipani cholamula, presidente akakwera udindo amakhala oyipa kwayinu, Kodi mumafuna president otani?

  • @dalitson3558

    @dalitson3558

    22 күн бұрын

    Aside kuba ndalama zamalawi

  • @BarnesMwase
    @BarnesMwase22 күн бұрын

    Koma kalindo ndi 1 kkkkkkkk

  • @user-zk7jw9up6m
    @user-zk7jw9up6m22 күн бұрын

    Kkkkk kkkk koma The DC

  • @chimwemwepitros5067
    @chimwemwepitros506722 күн бұрын

    Dc

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z22 күн бұрын

    Mpaka ntchenga koma eish

  • @PatrickNkumba
    @PatrickNkumba22 күн бұрын

    Sure

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience228322 күн бұрын

    Pamene ndimapemphera kupempherera dziko la Malawi ndinaona thambo la ziwanda. Tsiku lililonse limene Chakwera akilamula zithu ziwanda zikulowa m'Malawi. Mupemphere kuti Chakwera asadzawine. Chakwera ndi wa satanic.

  • @GabrielAdson-x6t
    @GabrielAdson-x6t22 күн бұрын

    Inu dzimvereni chisoni inuyo.Mukamawona usi mukumamva bwanji.Inuyo akalindo ngati achibale anu ngati ali anzeru bwanji osakutengani akakuwoneni kaganizidwe sikalibwino

  • @user-hm9nc7lz6e

    @user-hm9nc7lz6e

    22 күн бұрын

    Utsi watani munthu oipa mtima umapereka chilima mmanja mwa cakwera kuti amuphe ukuona ngati amalawi sitikudziwa bon kalindo sanaphapo munthu alibe magazi mmanja sanalowepo satanic ndipo usanalakhule udziganiza wamva anthu ambiri timamukonda kalindo ndi munthu yekhayo yemwe amatitothonza udzikamuudza

  • @brightkaunda920

    @brightkaunda920

    22 күн бұрын

    Bon kalindo musamamufanizile ndi usi chifukwa kalindo alibe dyera koma awo mukuti awusiwo ndi adyera

  • @samhussen708

    @samhussen708

    22 күн бұрын

    Mbuzi iwe usi Nd chigananga

  • @dalitson3558

    @dalitson3558

    22 күн бұрын

    Galu iwe ungafanizile Bon Kalindo ndi utsi what kind of you human being are you?

  • @ProsperBanda-ju2mq
    @ProsperBanda-ju2mq22 күн бұрын

    Koma mumapitadi ku vep bwana

  • @ChikumbutsoDzukwa
    @ChikumbutsoDzukwa22 күн бұрын

    Akuonjeza tsopano

  • @masterkaselema6396
    @masterkaselema639620 күн бұрын

    Opoila uyu

  • @samhussen708
    @samhussen70822 күн бұрын

    Gwenembe😂

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o22 күн бұрын

    Kodi amwene simukutopa mene munayambira aanzako Ali phee kuyendesa ziko

  • @user-hm9nc7lz6e

    @user-hm9nc7lz6e

    22 күн бұрын

    Adzatopa cakwera akadzacoka kapema kusitha maganizidwe ace onyasa chifukwa anthu ambiri itikuona ubwino wachakwera chimene tikuona mwacakwera ndi kupha kuononga ndi kusakadza mmm cakwera munthu oipa ukamuudze wamva ndi iweyo

  • @TemboHaswell

    @TemboHaswell

    22 күн бұрын

    Sangatope ameneyi chifukwa dzikoli eliyense akusata chamba atsogoleli akasiya kusuta nayeso asiya

  • @brightkaunda920

    @brightkaunda920

    22 күн бұрын

    Akulimbana ndi inuyo a mcp kut musiye kuzunza amasiyewo

  • @PemphorafaelBasilio
    @PemphorafaelBasilio22 күн бұрын

    Ya komadi e

  • @user-ln3zx6wo4w
    @user-ln3zx6wo4w22 күн бұрын

    Chifukwa chadyera 😂😂

  • @robsontyg3928
    @robsontyg392822 күн бұрын

    Shitombo shag'wako bon mathanyula

  • @reggieanthony7508

    @reggieanthony7508

    22 күн бұрын

    Matlamela a ng'uako nawenawe Robson nyompfi wako

  • @robsontyg3928

    @robsontyg3928

    22 күн бұрын

    @@reggieanthony7508 hunro nayar

  • @LukiahShaime
    @LukiahShaime22 күн бұрын

    Tingomenyana yamanja basi

  • @StainDandize
    @StainDandize22 күн бұрын

    😂

  • @JohnConar-kq4hi
    @JohnConar-kq4hi22 күн бұрын

    The DDDDDDDDDCCCCCCCCCCCC 🤔 🤔

  • @user-lk8kj9zv6x
    @user-lk8kj9zv6x22 күн бұрын

    Dangerous Child

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace32122 күн бұрын

    Komatu chakwela wafika pauchitsilu

  • @user-zk7jw9up6m
    @user-zk7jw9up6m22 күн бұрын

    Mfundo za boma zikakhale za nchenga koma mcp mwasowa zokambilana

  • @juliussamson6212
    @juliussamson621221 күн бұрын

    NDIMAGANIZA KUTI MWINA INU A UTM KUTI MAGANIZA NGATI ANTHU INU CHAKWERA ANAPHA CHILIMA LERO MUPANGASO ZAMGWILIZANO NDI SATANA MUGANIZA KUTI ASIYA KUPHA NOSE AKUPHA INUYO A UTM MUTHA