Paulo ndi Sila anamangidwatu. Iweyo nd ndani kut umupange declare kut iyeyo ndi olakwa pamene pamaso pa malamulo he is a free man. What if analapa ngat analakwadi? Komanso munthutu amawoneka kudzera muzochita nzake if anakulakwira chitchure chabwino iweyo chomwe anakulakwiracho. Kundale munthuyu samandisangalatsa not coz ndimadana naye koma chisankho basi, koma mmuzochitika zake amawonetsa kuti anali munthu wabwino. Nzanga winawakenso anazandiuza kuti "ngati uli mwamuna ukamati sudzagonako ku police uzinamiza, and ngat sunagoneko uziyamika Mulungu". Ulingarire mawu amenewo. It's better to celebrate someone's life kuwona ubwino wake ndichikhulupiriro zinazo tikawona kumwamba komweko.
@madalitso1000
Ай бұрын
Who told you kuti amaba?Who proved kuti anabapo?No one is guilty until proven,mind your words.
@SandraIssa-lo8il
Ай бұрын
My friend you are so stupid, anaba kunyumba kwako? Wopusa iwe eti...zochita kumupangira pa upon zo????
@user-jn9tz3li3v
Ай бұрын
@@madalitso1000Who should prove? Any reference from the bible kuti Mulungu azadalira someone to prove that one is not a sinner. Zinazi do not be emotional.
@madalitso1000
Ай бұрын
@@user-jn9tz3li3v Ofcoz God is the owner of judgement,but I remember even Tabitha atamwalira people was mourning kumanena zabwino zomwe ankachita which proved kuti anali wabwino.Similarly we should not judge,all what we should see is the good.😊
Пікірлер: 29
Mwana wa nkaziyotu ndye saulosi tu weni weni km abale chilima waswa mitima ya ana wo beautiful daughter like father Like daughter
this speech has made me drop tears of sorrow.
Great man indeed. Zambia mourns with you.
Well said beautifully said..❤
Mi Condolences to the family nd Malawi country for their loss. May his Soul rest in Peace. South Africa
A powerful tribute. May Dr. Saulozi Chilima nestle in the arms of the Creator.
Those who die in the Lord, their lives do not change but transformed🎉 Rest in peace
Beautiful daughter
Beautiful speech
Condolonces from Zimbabwe ana Chimwene😢😢
So touching
By miles the best life entailing speech through the entire ceremony
RIP SKC mwnawevu❤
❤❤❤❤
RIP SKC❤
Ndendende zoona like father like daughter
Koma a name angawotu nkhope kungoti ndendendee bambo ake,mzimu wa saulos uziusa muntendere
Rlp 😭😭😭
Bwanji amaba kristu wachonad samangidwa siyan zomwe mukunena anthu alemela sakhala olakwa akamwalila mlungu ndiamene atakamuweluzey
@Czarnder-im6pj
Ай бұрын
Paulo ndi Sila anamangidwatu. Iweyo nd ndani kut umupange declare kut iyeyo ndi olakwa pamene pamaso pa malamulo he is a free man. What if analapa ngat analakwadi? Komanso munthutu amawoneka kudzera muzochita nzake if anakulakwira chitchure chabwino iweyo chomwe anakulakwiracho. Kundale munthuyu samandisangalatsa not coz ndimadana naye koma chisankho basi, koma mmuzochitika zake amawonetsa kuti anali munthu wabwino. Nzanga winawakenso anazandiuza kuti "ngati uli mwamuna ukamati sudzagonako ku police uzinamiza, and ngat sunagoneko uziyamika Mulungu". Ulingarire mawu amenewo. It's better to celebrate someone's life kuwona ubwino wake ndichikhulupiriro zinazo tikawona kumwamba komweko.
@madalitso1000
Ай бұрын
Who told you kuti amaba?Who proved kuti anabapo?No one is guilty until proven,mind your words.
@SandraIssa-lo8il
Ай бұрын
My friend you are so stupid, anaba kunyumba kwako? Wopusa iwe eti...zochita kumupangira pa upon zo????
@user-jn9tz3li3v
Ай бұрын
@@madalitso1000Who should prove? Any reference from the bible kuti Mulungu azadalira someone to prove that one is not a sinner. Zinazi do not be emotional.
@madalitso1000
Ай бұрын
@@user-jn9tz3li3v Ofcoz God is the owner of judgement,but I remember even Tabitha atamwalira people was mourning kumanena zabwino zomwe ankachita which proved kuti anali wabwino.Similarly we should not judge,all what we should see is the good.😊
Uncle Jappie 😂😢
Rlp 😭😭😭