No video

Times Exclusive featuring Professor Arthur Peter Mutharika - 24 March 2023

Times Exclusive’s Brian Banda engages former president Professor Arthur Peter Mutharika on his life after presidency, DPP issues and his relationship with the current president.

Пікірлер: 152

  • @tonykapito2899
    @tonykapito2899 Жыл бұрын

    I didn't know that this man Mr Mutharika is so calm and collective. He has the ability of getting our country to a better place.

  • @obreykolopo8766
    @obreykolopo8766 Жыл бұрын

    Pr. Arthur Peter Mutharika, you're a big man with full wisdom. sizinazi ayi zomasekelera mu denge ngati ana.

  • @Study-Bible-daily

    @Study-Bible-daily

    5 ай бұрын

    ZOONA NDITHU, ngatidi ali proffesor akanaganiza izi..leave this for fresh people like Dr Kabambe etc

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs8 күн бұрын

    I pray for you APM that God continue to keep you with good health. To lead again this country

  • @jacquelinewasili-eh3uv
    @jacquelinewasili-eh3uv Жыл бұрын

    Mr Brian you were called to be mtolankhani pitilizani musadzaisiye ntchitoyi mudzalakwira mtumdu wa Malawi Mwacheza nawo bwino aAPM. monganso mmachitira ndi ena.Keep your fire burning .Simukondera.Wishing you all the best in your.. career.

  • @LeviKapyola
    @LeviKapyola3 ай бұрын

    Dr ,you are still strong, we need you to read us again even in another full 10 years. I know you are clever enough and I have 100% assurance that will win in the upcoming elections. Wishing you all the best.

  • @johnw.posomanchanel4023
    @johnw.posomanchanel4023 Жыл бұрын

    I think chakwera bringing his own chair and coffee smells something of what joice banda and bushiri did to Bingu wa Mutharika .That assassination plan was done by them, now calling on this meeting of cyclone was another plan of dealing with someone in a tactical way. So yeah APM did good not to attend that call. And we are living in a technology world where by meetings can be held online hence the whole total production of corona was to control people and work from home then why wouldn't they hold online page conference

  • @chifundonkhoma-uv4bw

    @chifundonkhoma-uv4bw

    Жыл бұрын

    He brought his coffee and chair... later he calls for a meeting where he expects others to sit on his chair and drink from his cup ...how does he judge himself....angelic that he can do evil to others?

  • @georgesmart3791
    @georgesmart3791 Жыл бұрын

    Hate Munthalika or love Him koma He still is a power house of wisdom and still got the malawi' best interest at heart ♥ ❤❤

  • @denechisomo
    @denechisomo Жыл бұрын

    APM is very smart and well educated the way he is answering the questions 💪💪

  • @jamesjolichi2026

    @jamesjolichi2026

    Жыл бұрын

    Apm vs BB

  • @bi8942
    @bi8942 Жыл бұрын

    Only three lawyers in the world ,the most powerful full of intelligence and high professional ,apm is one of these three , simaswera ayi ,this Man of a great man

  • @JairosNthala
    @JairosNthala3 ай бұрын

    This is one of the best exclusive interviews so far

  • @usherkays4379
    @usherkays4379 Жыл бұрын

    Brian Banda you're not a joke but a big deal and the entire country Malawi should be proud to have you,we are extremely happy for your amazing courage in your career keep it up

  • @michaelemmanuel257
    @michaelemmanuel257 Жыл бұрын

    My dear President sir

  • @lewisbonongwe8518
    @lewisbonongwe8518 Жыл бұрын

    Brian your the man and APM is blessed talent good man

  • @blessingkamanga1781
    @blessingkamanga1781 Жыл бұрын

    The man is in good health now

  • @MeekJrr
    @MeekJrr5 ай бұрын

    This man sounds very educated and wise

  • @charleskwapata265
    @charleskwapata265 Жыл бұрын

    APM for pple

  • @kamwazabonomali825
    @kamwazabonomali825 Жыл бұрын

    Brian Banda my favourite media personality.

  • @user-pc3zt3gp5x
    @user-pc3zt3gp5x7 ай бұрын

    Thank you for going to our former president APM.

  • @user-pc3zt3gp5x
    @user-pc3zt3gp5x7 ай бұрын

    Mr Brian Banda nothing I can say for the great job you are doing may God bless you .

  • @mollymasangano473
    @mollymasangano473 Жыл бұрын

    Adadi my President, the intelligent Man if your going to run the presidential cadindent make sure right now you should advisor the people in the party to be accountable not akatangwe ,kapena kumaba it will be a good government keep on advasing them 🙄 👍 I Love ❤️ 😍 My President Exellence Pro Peter Muthalika good Lucky 👍

  • @kennethmajor-zm4pt
    @kennethmajor-zm4pt Жыл бұрын

    Mr former pr❤❤❤

  • @TawongaMguntha-mc3vc
    @TawongaMguntha-mc3vc Жыл бұрын

    Madala Brian you are just a complete journalist,enawa ali kutali heavy

  • @medisonkoroma9844
    @medisonkoroma984410 ай бұрын

    Our beloved Leader

  • @peternjolinjo1960
    @peternjolinjo1960 Жыл бұрын

    Anali Big man ameneyo...but those sorrounders were the problem

  • @GiftMunyonga-ko9dz
    @GiftMunyonga-ko9dz3 ай бұрын

    Genius 🙌💯

  • @usherkays4379
    @usherkays4379 Жыл бұрын

    You give us hope Brian, Cape town South Africa

  • @HappyMcjusticebetha-bh1gh
    @HappyMcjusticebetha-bh1gh Жыл бұрын

    Great man

  • @felixntaika6201
    @felixntaika6201 Жыл бұрын

    ❤️❤️❤️❤️❤️ timakunyadilan

  • @anthonyfeyokabuthu9
    @anthonyfeyokabuthu9 Жыл бұрын

    LONG LIVE YOUR EXCELLENCY.I SMILED COZ COULD SEE THAT U ARE STILL IN GOOD SPIRIT,KEEP THE FIRE BURNING N MAKE HATERS THINK OTHERWISE

  • @user-tu8fi4jl1f
    @user-tu8fi4jl1f5 ай бұрын

    Thanks big very wise speaking

  • @BrightMphamba-vd4oq
    @BrightMphamba-vd4oq3 ай бұрын

    Our President

  • @menslounge5722
    @menslounge5722 Жыл бұрын

    The man keeps all this data in his head and recalls it whenever he wants to, and we still call him nkhalamba, we must have special ranks of khalamba

  • @user-wm6bd6ll5x
    @user-wm6bd6ll5x6 ай бұрын

    APM chonde tipulumuseni umphawi wafika povuta Ku Malawi kuno. God bless you.

  • @user-qp2zu1ye7y
    @user-qp2zu1ye7y10 ай бұрын

    This is really a diplomatic interview then our Ken this is what we call interview

  • @bi8942
    @bi8942 Жыл бұрын

    Pa dziko lapansi pali ma lawyer oopsa kwambiri and apm is among these three. No one can trick this Man and win

  • @tatendazauya5761
    @tatendazauya5761 Жыл бұрын

    "He brought his own chairs and his own coffee" wow just wow

  • @dennisnamaona7753
    @dennisnamaona7753 Жыл бұрын

    My president

  • @thumbikonkwawazingwe4334
    @thumbikonkwawazingwe4334 Жыл бұрын

    I love the prof.

  • @Benty_Pro
    @Benty_Pro6 ай бұрын

    APM The Think Tank

  • @essahabdullah-jl8yg
    @essahabdullah-jl8yg Жыл бұрын

    respect you adad mumatilera osati iziiiiii

  • @lukainnocent5380

    @lukainnocent5380

    Жыл бұрын

    Vuto simuchedwa kuyiwala mumati ndi mbuzi pano mukuti ndi wabwino shame on u

  • @petermwakihana9879
    @petermwakihana9879 Жыл бұрын

    We not go round here azayimilile yekha the party will win. No need of choosing another one

  • @user-ux3ed3ni1p
    @user-ux3ed3ni1p Жыл бұрын

    Why did the IMF with hold funding when his Govt was "cooking the books" ....this denial of Katangale is problematic.😮

  • @wilsonsilasmkandawire
    @wilsonsilasmkandawire Жыл бұрын

    Peter Muthalika is a brain and a resource. I truely believe he was surrounded by bad people who were misrepresenting him.

  • @EnockChitukuta-yz5mk
    @EnockChitukuta-yz5mk Жыл бұрын

    More blessings to you Brian you impres us

  • @montmphepo3662
    @montmphepo3662 Жыл бұрын

    Ndikufinyafinyani still in my head 🗣️

  • @vinnie1nyirenda755

    @vinnie1nyirenda755

    Жыл бұрын

    Kkkk uziyiwalako

  • @EnockChitukuta-yz5mk
    @EnockChitukuta-yz5mk Жыл бұрын

    APM has shown that indeed he started politics in fifties,he knows what he is doing

  • @chifundonkhoma-uv4bw
    @chifundonkhoma-uv4bw Жыл бұрын

    Apa I understand that APM has defeated Brian .....has managed to respond correctly and wisely to all the tricks of the jounourist... 😂😂😂😂😂

  • @bi8942

    @bi8942

    Жыл бұрын

    Apm ndi machine ,

  • @Malani41
    @Malani41 Жыл бұрын

    Should have pressed him on the houses in the USA. He said he still has three houses and then something dawned on his mind that made him pivot to saying he has sold two of those. Suspicious!!!!

  • @JafaliAjusa-zg2xi
    @JafaliAjusa-zg2xi6 ай бұрын

    Mumakwana mr Brian Banda mukugwila ncthito kwambili

  • @jamesfany6636
    @jamesfany6636 Жыл бұрын

    He is very good man

  • @StevenPongolani-pp9by
    @StevenPongolani-pp9by Жыл бұрын

    Brian banda continue doing ur good job

  • @aaronguwechakwira
    @aaronguwechakwira Жыл бұрын

    Brian why did not mention those guys who was bringing cement on his name ?? Seems like you were scared to ask him deep wquestion .. if it was someone else you was going to hit those questions ' seems like you were scared of him

  • @innocentkandulu4982

    @innocentkandulu4982

    Жыл бұрын

    He did. APM refused to say anything since the issue is still in court.

  • @EmmaEmma-nb7qv

    @EmmaEmma-nb7qv

    8 ай бұрын

    Mmmm adani inu mafuso akufusa Brian WO achepa ndye kuti nayeso wasiyanisa ndi akanganya alipowa inuyo Atakupasani mpata mukakwanisa mmmmhhh

  • @VincentJonala-kd3fu
    @VincentJonala-kd3fu Жыл бұрын

    Malawian father we still need yiu

  • @nephaskalema-in5sm
    @nephaskalema-in5sm Жыл бұрын

    I like how Munthalika is responding...the guy isnt nkhalamba but a matured person !

  • @hanifpatelo6717
    @hanifpatelo6717 Жыл бұрын

    I wonder what kind of chair mr chakwera bring it

  • @tingamasi106

    @tingamasi106

    Жыл бұрын

    Brought not bring it

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d Жыл бұрын

    Brian Banda akatundu omanga ndi wire🔥🔥🔥

  • @chisomombeta6446
    @chisomombeta6446 Жыл бұрын

    Ife meeting imeneija sitinawalore adad athu mmafuna mukatibere mzeru iyhaaa...Mesa mmaenda ndi afana oganiza bho

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p Жыл бұрын

    Iwe usamadzinamize kuti natumbowoko azawinaso chakwela sadzawinaso patakalekale umuwuze chilungomo chakwelayo usamamunanize mbavayo chakwala

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 Жыл бұрын

    We miss u .......the greatest man ❤ 2025 in power again

  • @Mbesa09
    @Mbesa09 Жыл бұрын

    Funny that APM now sees the value of the local media. When he was in power, he thought he is untouchable.

  • @brightnyoni7802

    @brightnyoni7802

    Жыл бұрын

    for sure this is very interesting, politicians will only support what Favours them unlike what will affect them, by so doing there isn't transparency, now that he is in opposition, he feels the private media is important.

  • @afritouch4660
    @afritouch4660 Жыл бұрын

    I hate him saying Ministers can’t still money in government..! He’s totally blind..!!

  • @tingamasi106

    @tingamasi106

    Жыл бұрын

    Steal.....not still

  • @afritouch4660

    @afritouch4660

    Жыл бұрын

    @@tingamasi106 typing error.. but thanks that helped

  • @duncanchizizi6543

    @duncanchizizi6543

    Жыл бұрын

    Very ridiculous indeed. These people loot using all sort of ways

  • @malumbophiri
    @malumbophiri Жыл бұрын

    Machine APM

  • @user-lp5tm3br7k
    @user-lp5tm3br7k6 ай бұрын

  • @AbrahamIkombwe-cc7no
    @AbrahamIkombwe-cc7no Жыл бұрын

    Chakwera simulungu koma amayenera kuva za namodwe akanaimitsa ulendo wake

  • @meganabigail-ye7fw

    @meganabigail-ye7fw

    11 ай бұрын

    Amafuna kukapeleka umboni kuti zatheka zija

  • @user-mv1er5zr7e
    @user-mv1er5zr7e9 ай бұрын

    Sitikuva chigerezi next time try to speak Chichewa

  • @alexgweje8610
    @alexgweje8610 Жыл бұрын

    Mbudzi ndi iweyo amene ukumunena Mr President ndipo ndiwe chindere kwabasi think before you talk

  • @mcandrewsmaunda7921
    @mcandrewsmaunda7921 Жыл бұрын

    Deeply embittered.Learn to let go

  • @nyamatchelengamaclawrence
    @nyamatchelengamaclawrence5 ай бұрын

    I see alot of people be comes rich

  • @brinokalemba4503
    @brinokalemba4503 Жыл бұрын

    Those were Bible times 😂😂😂😂😂😂

  • @brightnyoni7802

    @brightnyoni7802

    Жыл бұрын

    this was a very interesting comment from the journalist it sounded like a joke but very true indeed, I enjoyed listening to this interview because I love politics and Iam a Zambian based.

  • @user-xg5mb9ql2i
    @user-xg5mb9ql2i7 ай бұрын

    Chizungucho muzivela nokha

  • @nammosieuVoBienTichNhuLai
    @nammosieuVoBienTichNhuLai10 ай бұрын

    Ước mơ thế giới lân hoà hảo Nhà phật con tiên hé miệng cười Xin quy y Phật Xin quy y Pháp Xin quy y tăng Thường niệm phật Cầu nguồn sống tại phật giáo hòa hảo nhé các con Không có cuộc chiến tranh nào được tính bằng công Mà đều phải ghi vào tội Chỉ nguồn sống yêu dân thương dân sống hết lòng vì dân Và biết tạo nguồn sống thật đạo đức sống cho nhân dân Và nên tạo cho dân rõ hiểu một cuộc sống thế giới của Nam mô a Di Đà Phật ạ Nam mô a Di Đà Phật

  • @Liki-Likiladies
    @Liki-Likiladies Жыл бұрын

    kkkkkk Brian👐👐👐👐👐

  • @hitsrecords_265
    @hitsrecords_265 Жыл бұрын

    Choikila interview muchizungu ndi chan

  • @DoYouKnow3838

    @DoYouKnow3838

    Жыл бұрын

    APM samathatu kulankhura Chichewa nthawi yayitali..... Paja tiliso ndi Goodall Edward Gondwe, can't even construct sentence in chichewa

  • @IndianaGama
    @IndianaGama6 ай бұрын

    Nzudufhchchcycycuc

  • @josephydeves5589
    @josephydeves5589 Жыл бұрын

    Brian lero wakumana nazo kuyankhidwa mosapsatira komanso osadodoma😂😂😂

  • @emmanuelchavula7144
    @emmanuelchavula7144 Жыл бұрын

    Adadi 😂

  • @LawrenceMoyo-kc5xx
    @LawrenceMoyo-kc5xx Жыл бұрын

    Dipipi

  • @stevemhone6998
    @stevemhone6998 Жыл бұрын

    Is it me or Brian's face looks like it has been embammed

  • @EmmaEmma-nb7qv

    @EmmaEmma-nb7qv

    8 ай бұрын

    Muli ndisoka mulungu anati zilibwino inu mukuika mau oipa pachithu chabwino cha mlungu

  • @AaronMuwaShani-vj7is

    @AaronMuwaShani-vj7is

    8 ай бұрын

    😂😂😂😂😂 Lol

  • @bonfacengwira9741

    @bonfacengwira9741

    6 ай бұрын

    It's yours it has been imbammed 😂

  • @CharlsChiyembekezo-xu4wk
    @CharlsChiyembekezo-xu4wk5 ай бұрын

    ntimakunyadilan

  • @richardmasina5454
    @richardmasina5454 Жыл бұрын

    Ndale ndi kanyama koyipa zedi adatero nkasa, all answers were nonsensical

  • @ImmanuelMkwindaNgwira
    @ImmanuelMkwindaNgwira9 ай бұрын

    "others" 😂😂

  • @successorisaac
    @successorisaac Жыл бұрын

    Naliya ku phalombe tikukusatilani

  • @williamowen4128
    @williamowen4128 Жыл бұрын

    kupuma kwa mdalayu nafenso tinapuma...ankaweta dzinkhanira dzambiri...pano dzaonda nayo njala mTown mu..

  • @DavidNdozi
    @DavidNdozi Жыл бұрын

    Mbuzi yeniyeni fundolence

  • @robsontyg3928
    @robsontyg3928 Жыл бұрын

    Peter Mathanyula, usamazinamize kuti DPP idzalowaso m'mboma, ma albino pano akuyenda mwa mtendele apuma kuphedwa ndi ma cadet a dpp

  • @felixntaika6201

    @felixntaika6201

    Жыл бұрын

    Dzikomo chifukwa cha maganizo anu osathekawo kkkkkkkk za Ana amuna iziih mwayesa ngati ndichipembezo et mwayamba mkare kunjenjemera

  • @blandinabonaventure

    @blandinabonaventure

    Жыл бұрын

    Albino, pano anthu akuvutika ndi njala mukudxiwa chifukwa cha bodza LA tonse tiziyamika zomwe boma LA dpp lidapanga osangoyang'ana zoipa ife chakwera ndi kwathu kma tikumudxiwa palibe chazeru chomwe tidachiwona kma tidavota tonse kusaka mtendere kma mmmm zanyanya tiyamike mulungu basi

  • @jafalijulius8051

    @jafalijulius8051

    Жыл бұрын

    Anachita bwino osapita

  • @robsontyg3928

    @robsontyg3928

    Жыл бұрын

    @@blandinabonaventure gwilani ntchito kapena business kuti mupeze zosowa zanu, pa dziko la pasi palibe president amene amagawa ndalama zaulele ngati ndi ulesi ukuphani

  • @robsontyg3928

    @robsontyg3928

    Жыл бұрын

    @@blandinabonaventure musakhale ngati nthawi ya Peter munthalika munkadya nyama, munabadwila mu umphawi mudzafa mumphawi chifukwa chofuna zaulele,

  • @ChilliesDamao
    @ChilliesDamao Жыл бұрын

    😂😂😂😂😂 iyaaaaa galu wachabe chabe

  • @willim9618
    @willim9618 Жыл бұрын

    👂👀✅️!

  • @esthergweje4038
    @esthergweje4038 Жыл бұрын

    Iwe ukumunena Peter kuti ndi mbudzi ulibe nzeru kwambiri chifukwa sukudziwa bwino kuti Peter anaonapo chani ndi nkona sanapiteko Chakwera ndi osamva kumene mesa anauzidwa kuti kubwere Namondwe ndi pamene amapita kunja kukadya sausage so why you blame Peter instead of Chakwera muziwe kuti Chakwera amaziwapo kanthu kuti anthu akunama ndi zoopsya ku Malawi

  • @lukainnocent5380

    @lukainnocent5380

    Жыл бұрын

    Iwe ndiwe galu kwabasi chakwera akaziwe ndi mulungu

  • @chisomomzunga8726
    @chisomomzunga8726 Жыл бұрын

    ???????

  • @jezalakaphuka7325
    @jezalakaphuka7325 Жыл бұрын

    Brains

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p Жыл бұрын

    2025 bom

  • @ibrahimwezely-pn6te
    @ibrahimwezely-pn6te Жыл бұрын

    Muulamuliro wake analowelera mma department a boma ndipo galimoto za polisi amakwera ma cadet ngakhale za escom komaso kupha albino . Uyuyu ndi matope enieni

  • @mandamandamanda2208
    @mandamandamanda2208 Жыл бұрын

    Mbuzi ndiwe wa comment ya number 3 peter anachita bwino kusapitako kunkumano umenewo Chakwera ndi munthu wosamva Komaso mzimayi ameneyo siwofunika kukhala naye pamodzi Satanic peter ndi munthu woganiza bwino musamusokoneze ndi tinkumano tanu tautsilu

  • @moosasame623

    @moosasame623

    Жыл бұрын

    Iwe wa number 3 comment zomwe mbuzi zanuzo zakambirilana mukuzidziwa kumangosekerela zopunsa anthu dziko akubvuto galu wa munthu iwe kwabas kwabas

  • @gifttilaya949

    @gifttilaya949

    Жыл бұрын

    Uyu akuthandizayo siwa satanic expect more n more money and other things from that under world ( satanic) to come those devastated areas

  • @sanudikasimu7559
    @sanudikasimu7559 Жыл бұрын

    Amalekelela alubino kuphedwa ngati nkhuku ameneyo zimenezo ndizina mwazimene ndikukumbukila

  • @jamesfany6636

    @jamesfany6636

    Жыл бұрын

    Economically things were OK by then

  • @petermwakihana9879
    @petermwakihana9879 Жыл бұрын

    Ndale ndizovuta kwambili. Kukonda zako chifukwa wakumana ndimavuto that’s not true and I doubt if pro Peter wamuthailka akanamuvela

  • @ancientnkhata1137

    @ancientnkhata1137

    Жыл бұрын

    Kumukonda kwake kukhale kotani .Mumafuna amupatse unduna ?

  • @judithchitukwi165
    @judithchitukwi165 Жыл бұрын

    Makape a DPP inu. Nthawi yanu inatha vomerezani kuti mdala wanuyu wakalamba basi.

  • @cadohjabu5565

    @cadohjabu5565

    Жыл бұрын

    Makape ndamene mukukukanika dzikokuyendetsanu Mavubwa

  • @MarkBilly-bl7em

    @MarkBilly-bl7em

    Жыл бұрын

    DPP apolisi adalibe mphamvu yomanga anthu, koma makadeti. Mwachidule nthawi ya dpp dziko limayenda lokha lopanda utsogoleri. Rest in peace dpp!

  • @macleanmachamo
    @macleanmachamo Жыл бұрын

    Leave this man he has still pain of losing election

  • @brightnyoni7802

    @brightnyoni7802

    Жыл бұрын

    he has to understand and rest he run his race and he is all grown

  • @judithchitukwi165
    @judithchitukwi165 Жыл бұрын

    Mbuzi ya munthu iyi. Kukanika kupita kokambirana . Munthu opusa kwambiri

  • @felixntaika6201

    @felixntaika6201

    Жыл бұрын

    Mbuzi ndi aja anabeleka iweyo aja patumbo pawoso mwana wa hule uzisamala mayakhulidwewo wava iwe wayiwala kuti chakwera yemweyo anakanopo mbuyomu kupanga zokambilana ndi peter nde lero you think kuti peter angapite kokambilana zichani lero ndilimene mwawona kuti peter ndiwofunikilano munkhuula

  • @jafalismart

    @jafalismart

    Жыл бұрын

    Usamunyoze munthu choncho ngat iweyo ukuziwapo kanthu pazomwe iwowo akuziziwa iweyo ngat Chakwela ali malume ako usapange compare ubale ndi ndale iweyo za ndale siuziwapo kanthu

  • @jomochirwa

    @jomochirwa

    Жыл бұрын

    Adad yesetsani kuti chipanichi mudzachiyimile nokha 2025 en mukadzawina mudzachite kumusiyila wina kuti adzapitilize kulamula ngati muja adachitila mandela muja.chonde musalole kusiyila anyamatawa tisadavote powopa kugawanitsa chipani chifukwa anyatawanuwa ndi a njala zeedi.

  • @blandinabonaventure

    @blandinabonaventure

    Жыл бұрын

    Kodi chakwera Anapanga chipongwe Peter mukudxiwa ndiye Peter akatani kwa chakwera aaa inu muxiganiza patakhala inu kutseka MA count ake chifukwa chani ngt iwowo sakuba muzaona akatuluka kut a a zingati wait

  • @ancientnkhata1137

    @ancientnkhata1137

    Жыл бұрын

    Ndipo mbuzi imeneyi

  • @judithchitukwi165
    @judithchitukwi165 Жыл бұрын

    Nde sunatitu ulira zeni zeni 2025 coz Chakwera akuzawinaso .

  • @felixntaika6201

    @felixntaika6201

    Жыл бұрын

    Aaaah kkkkk osawuka kuziwa mbalume hahaha 🤣🤣🤣🤣 tanenaniso

  • @robsontyg3928

    @robsontyg3928

    Жыл бұрын

    Chakwela ndi akatundu , alamilila until 2030

  • @shabannicks9897

    @shabannicks9897

    Жыл бұрын

    ​@@robsontyg3928 😂😂😂😂😂 uphawi sizithu😂😂😂

  • @duncanchizizi6543

    @duncanchizizi6543

    Жыл бұрын

    @@shabannicks9897 anyamata ojiya kuzilmbitsa mtima. Chakwera wakanika basi

  • @duncanchizizi6543

    @duncanchizizi6543

    Жыл бұрын

    Kulota samaletsa.

Келесі