Skeffa Chimoto -'' Ine Si wa sataniki'' kuchoka kogulisa zipewa Pano Ndi Billionare

Kupatula kuyimba, Skeffa amapangano ma business. Iyeyu ali ndi MAGalimoto ambiri omwe amanyamula katundu . Mu kanthawi kena, anayamba kutchuka ndi mbiri yosakhala bwino yoti iyeyu ndi mmodzi wa anthu a Satanic ndziko lino.
kuchoka kogulisa zipewa Pano Ndi mponda matiki
from sellingTsotsi Hat to a multi-millionaire
the story of skeffa chimoto

Пікірлер: 79

  • @victorkazembe9631
    @victorkazembe9631 Жыл бұрын

    Vuto la ife amalawi munthu akatukuka timayamba kupeka nkhani. Skeffa wavutika pamoyo wake. Pano mulungu wamuona anthu mwayamba kukamba zambili.

  • @estoriasikwewa1893

    @estoriasikwewa1893

    Жыл бұрын

    Inu amalawi sazatheka samafuna kuti. Azawo alemele

  • @ngomajohn1751
    @ngomajohn1751 Жыл бұрын

    Watching live & direct from zambia , chipata , kasenegwa district - John Ngoma..skefa chimoto my blessing

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw3 ай бұрын

    Asikefa kodi kalata anasiya chinga sipanatuluke zina lanu kumbukilani kalata imeneyi mboni ndi grace chinga anasiya kalata dziko lonse likuziwa ndithu

  • @clementbanda1137
    @clementbanda1137 Жыл бұрын

    Watching from Port Elizabeth South Africa,,

  • @rasheedmalunga9212
    @rasheedmalunga9212 Жыл бұрын

    Watching from UK

  • @mwayikayuza8164
    @mwayikayuza8164 Жыл бұрын

    I like chimoto so much

  • @ruthtimothy9583
    @ruthtimothy9583 Жыл бұрын

    Watching from Cape town

  • @lastonnthenda2309
    @lastonnthenda2309 Жыл бұрын

    I lke that guy n he is so humble from thyolo

  • @kelvinmwasinga1706
    @kelvinmwasinga1706 Жыл бұрын

    Watching from Namibia

  • @GraceTandani
    @GraceTandani2 ай бұрын

    Watching live from United States

  • @blessingsmtambalika358
    @blessingsmtambalika358 Жыл бұрын

    Sikefa chimoto Amadidalitsa ndi nyimbozake

  • @TaitusNyamula-iv2mr
    @TaitusNyamula-iv2mr9 ай бұрын

    watching from kenya

  • @EliseuMoffatliver-vn1xg
    @EliseuMoffatliver-vn1xg3 ай бұрын

    Musatinamizepo apa it's only God who knows everything

  • @user-lq2zj1vy5e
    @user-lq2zj1vy5e2 ай бұрын

    Ndichifukwa chake amatilimbikisa kwambiri munyimbo zake

  • @harrymaganga5977
    @harrymaganga5977 Жыл бұрын

    Muthuyu ndi luso lake Koma Muthu akatchuka kapena kulemela anthu amamukamba Koma skeffa usaoke ndithawi yako nyimbo zako Ife dzinatisitha

  • @macdonaldkorea2928

    @macdonaldkorea2928

    Жыл бұрын

    Amalawi tili ndi bvuto mchifukwa ambiri tili osauka mpaka panopo komano kusaukaku ndi kwammutu mwathu, tikadzalemera mmutu pamaganizidwe tidzayamba kutukulana tokha tokha like Indians...... Ukatukuka akuti walowa satanic, ukasauka akuti anasemphanitsa chizimba, umphawi udzatipha kwabasi.....sinthani maganizidwe potero kuti Mulungu atisinthe nafe

  • @kinlosmachemba5046
    @kinlosmachemba5046 Жыл бұрын

    Amalawi tidzitha kuyamika mzathu akachita bwino.Uyu ndi mmalawi akuyimba ku malawi akutukula malawi.Chonde tiphunzire kuyamika zimene wina wachita.

  • @ajisonchimombo88
    @ajisonchimombo88 Жыл бұрын

    Jealous people always loose

  • @user-gd6zb2bv8f
    @user-gd6zb2bv8f6 ай бұрын

    Nthawi yotsiliza ino Satana akugwira nthito kwambiri ndi anthu omwe mukuti ndi alusowo, Tamawelengani za kutha kwa nthawi ya pansi pano , komanso mudzisegula ma website ena mudzaseguka m'mitu mwanu, Inenso ndinkamukonda koma zomwe ndinapeza ku ma website ena zinandipangitssa kufuta nyimbo zake zonse komanso si yenkhayo ayi, alipo kagulu moti ena amati ndi a gospel koma akutumikila satana kuseli , inu simukuziwa komanso mwini wakeyo sangavomere ayi. Chomwe mukuona inu ndi nyimbo basi

  • @mwale1154
    @mwale115411 ай бұрын

    Wa was wa akulu akulu!

  • @user-to8tp4ni1r
    @user-to8tp4ni1r11 ай бұрын

    I like Driemo cfkwa sapanga nao

  • @asmaljames9323
    @asmaljames9323 Жыл бұрын

    Bambo ngati kalankhulidwe kanu mumaganiza kuti ndikachikoka aaaaaiiii ndithu sinthani kalankhulidweko thats my opinion

  • @napsjnr3776

    @napsjnr3776

    Жыл бұрын

    Mbuzi ya munthu iyi kkkkk

  • @SamPhiri-ru8dc

    @SamPhiri-ru8dc

    Ай бұрын

    zowonadi man

  • @dicksonphili3466
    @dicksonphili3466 Жыл бұрын

    Sikefa kaya ndiwa sitac zilibe kanthu ine nyimbo zake zimandisintha

  • @alfredbanda1732
    @alfredbanda1732 Жыл бұрын

    Suziwa kumasulila nkhani ataaaa

  • @manuelmakonda2324

    @manuelmakonda2324

    Жыл бұрын

    I think better mukanapanga zanu tione, than kuti mukhale wazelu pazomwe wina wachita,

  • @ConcleyManeya

    @ConcleyManeya

    10 ай бұрын

    Osamadana ndi anthu olimbika pogwila ntchito .

  • @albertinamartins2593
    @albertinamartins2593 Жыл бұрын

    Ndimakukondani achimuene

  • @miracleeneah5861
    @miracleeneah5861 Жыл бұрын

    Komaso alibe Galimoto registered number skeffa 1

  • @AlfredbensonaogagmMunthali
    @AlfredbensonaogagmMunthali2 ай бұрын

    Vuto a Malawi munthu akayiphula amati ndiwa satanic

  • @miracleeneah5861
    @miracleeneah5861 Жыл бұрын

    Palibe chomwe mudziwa inu za skeffa aaaaaaaa dzina lake lenileni ndi joviara moti simuzidzuwaso

  • @snetawailiyasa3215
    @snetawailiyasa3215 Жыл бұрын

    watching from jamaica

  • @jabumohammednyanganya4435

    @jabumohammednyanganya4435

    Жыл бұрын

    Sk

  • @NumbDee

    @NumbDee

    4 ай бұрын

    Kodi iwe Hanifa sungamayakhule bwino bwino ine amanditopetsa kwabasi

  • @ericndizeye9490
    @ericndizeye949010 ай бұрын

    ooohhhh

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Жыл бұрын

    Inu taziyankhulani bwino bwino apa.

  • @cktutorials7998
    @cktutorials7998 Жыл бұрын

    Skeffa is a blessing love from Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲

  • @willsonmzumala
    @willsonmzumala Жыл бұрын

    Akutameni

  • @alexjeremanuel2541
    @alexjeremanuel2541 Жыл бұрын

    Nthawi zambiri chifukwa cha kulephera kapena kufooka kwa munthu mapeto ake wina amayamba kuda anthu ena posafuna kuvomeredza kulephera kwake

  • @agnesssomaliland
    @agnesssomaliland9 ай бұрын

    Koma tone ya voice mukanasitha please news zanu sizikubeba zuoneka ngati kukakamiza zithu kumangolakhula voice yanu bwanji😂

  • @SymonNamalomba-sh3fu
    @SymonNamalomba-sh3fu9 ай бұрын

    Sangavomeredze olo ali wasatanik kma akudzuza ndi mulungu ekha basi

  • @dondream5021
    @dondream5021 Жыл бұрын

    🙉🙉🙉🙉

  • @dorafaartsigns6188
    @dorafaartsigns6188 Жыл бұрын

    Vuto lakwathu kuno ku Malawi timadana ndi wolimbika ndipo wolimbikayo akalemera amampatsa nickname yotchedwa satanic.

  • @yamie1
    @yamie1 Жыл бұрын

    Munthu ndi olimbikira uyu

  • @sesfikileshop7344
    @sesfikileshop7344 Жыл бұрын

    Komatu zoti ndi Billionaire mukumulakwira inde ali ndi kanthu koma zoti ndi Billionaire mukuzitenga kuti? Mu list yama Billionaires m'Malawi muno iyeyo mulibemo

  • @NespoliNanganga
    @NespoliNanganga9 ай бұрын

    Ndiwe dolo

  • @stainmilanzi5293
    @stainmilanzi5293 Жыл бұрын

    Palibe chilipo pamenepo guys

  • @ntchindikondowe643
    @ntchindikondowe643 Жыл бұрын

    Amalawi nzanu asachite bwino ndekuti ndi wa satanic inuyo mumayankhula chonchonu mumafuna kusauka mulinakoko ngati ndi wa satanic Inu mukulekelanji kukalowa kuti nanunso mulemele tamango kandani anthu opanda tsogolonu

  • @user-xj5qd6of5d
    @user-xj5qd6of5d5 ай бұрын

    Munipatseko nambar achimoto skef

  • @EliseuMoffatliver-vn1xg
    @EliseuMoffatliver-vn1xg3 ай бұрын

    A Malawi ambiri mukutiopsa kwambiri mwasintha modabwitsa koma Bible imati mwini nyumba akadadziwa kuti mbala ldza boola nyumba si bwenzi ata gona koma akadadikirira kuti mbala lsa boole 'koma a Malawi mwataya chamoyo mwatola chakufa

  • @DanielMbvundula-ft2zx
    @DanielMbvundula-ft2zx Жыл бұрын

    Ndi n'daliso wake basi

  • @henzomanzo9158
    @henzomanzo9158 Жыл бұрын

    You are the best skeffa not this guys gwambizo fukolo man

  • @b.i.gndunab.i.gnduna7441
    @b.i.gndunab.i.gnduna7441 Жыл бұрын

    Ai ndiwasataniki skefa yo guys

  • @rainfordisaacs6789

    @rainfordisaacs6789

    Жыл бұрын

    Muli ndi umboni inuyo?

  • @victormsika1538

    @victormsika1538

    6 ай бұрын

    Wasatanic yo ndi iweyo ka. Ukhalilanji ndi nsanje ngt siiwe wa satana. Mfiti yachabechabe

  • @masterevanschomora
    @masterevanschomora Жыл бұрын

    Vuto anthufe sitikufuna kuyesa zinthi kuti tiziwe mataleti athu mara muzati in ineso Wa Sataniki koma tikuyambila apa movutikira 👉aaronnemarere TV watch muone mmene timavutikila kuyamba zinthu

  • @mlezanyirenda2815
    @mlezanyirenda2815 Жыл бұрын

    Oyimba ambiri akwathu ose awonongeka ndi usatanic vuto asogoleri nde akakuwuza kut ulowe Umarowa u satanic kwathuko sakubisa kharidwe lonyasa

  • @graciousrobertrobert6928

    @graciousrobertrobert6928

    Жыл бұрын

    Its true hé is thé satanic one

  • @ipyanamwanyongo4169

    @ipyanamwanyongo4169

    Жыл бұрын

    you're speaking the truth my brother all of them Malawian musician alowa usatanic, chifukwa anampha uyimba but we need to pray for Malawi that God most delivered this country from powers of darkness,

  • @christopherbadson699

    @christopherbadson699

    Жыл бұрын

    Inu mumati angavomere kuti iye ndi wa satanic?

  • @alexbanda4982

    @alexbanda4982

    Жыл бұрын

    Kaya abale Inu

  • @ishmaelchiponda7806

    @ishmaelchiponda7806

    Жыл бұрын

    Koma ndinu omvetsa chisoni, satanic kulibeko ku malawi...

  • @hopekandle6707
    @hopekandle6707 Жыл бұрын

    🤣🤣🤣🤣 koma adolo inu nde mmadziwa kulongosola nkhan eti

  • @samuelbartolomeusadia1219

    @samuelbartolomeusadia1219

    Жыл бұрын

    Tenho uma ttt

  • @thebulonathaniel1772

    @thebulonathaniel1772

    Жыл бұрын

    Hie

  • @vettasanga3876
    @vettasanga3876 Жыл бұрын

    God bless you mr

  • @modyanthuachino2074
    @modyanthuachino2074 Жыл бұрын

    Ndi wa satanic uyu luso lake ija anakagulitsa kwa satana pano saimbanso bwino Mumuuze mmaso mwake skeffa yo

  • @truthtellerlastonk.m.p4985

    @truthtellerlastonk.m.p4985

    Жыл бұрын

    Prove it sir

  • @paramountcommodities3236

    @paramountcommodities3236

    Жыл бұрын

    Bring relevant information big,,it seems you know each other

  • @jumbradoone4164

    @jumbradoone4164

    Жыл бұрын

    Aliyese ophula pa Malawi paja ndi wa Satanic

  • @nenanimayinga716

    @nenanimayinga716

    Жыл бұрын

    Kkkkkkk km nkhan zakeso

  • @estoriasikwewa1893

    @estoriasikwewa1893

    Жыл бұрын

    Don't judge anyone please musiyileni mulungu yekha