Ndikonda Mulungu. Chichewa Hym

Video from Mark Kamputa/ copied

Пікірлер: 33

  • @user-lp8nd5uq7g
    @user-lp8nd5uq7g2 ай бұрын

    When am sad it was make me happy.i love this song

  • @FabianPhiri-uo8ve
    @FabianPhiri-uo8ve8 күн бұрын

    My favorite hym Kamwala Rcz

  • @MaweleMawele
    @MaweleMawele3 ай бұрын

    That was my Mommy favorite song may your soul continue rest in peace 😭💔💔

  • @MsongaPhiri-gg6ct
    @MsongaPhiri-gg6ct Жыл бұрын

    I really appreciate and love your work i enjoyed your songs

  • @andrebinossegonondo3362
    @andrebinossegonondo336211 ай бұрын

    Ndikumbukila. Malemu Amatiase ndi bambo wanga a Binosse pá chito tá ambuye

  • @sallyouattara8390
    @sallyouattara83905 жыл бұрын

    10. Uthenga uwu ukunena kuti Chisilamu, Chikhristu ndi Chiyuda ndizo mizimu itatu ya chule mu Chivumbulutso 16:13. Zipembedzo zitatu izi zimati ndi za Abrahamu. Zipembedzo zitatu izi zimakhulupirira mwa Mose. Zipembedzo zitatu izi sizimakhulupirira mwa aneneri amoyo koma aliyense amadzinenera kuti ndi wa mneneri yemwe iyo sikumudziwa. Aliyense wa iwo ali ndi buku lake-lake loyera. Ndipo onse atatu akuyembekezera Mesiya. Iwo ali mizimu itatu ya chule mu Chivumbulutso 16:13. Uthenga ukukunena kuti zimenezi ndi ziwanda zimene zinaukitsa Elvis Presley, Bob Marley, James Brown, Madonna, Papa Wemba zimene lero zaukitsa magulu ndi oyimba a chikhirisitu monga Tabitha Lemaire, Don Moen, Exo Eclats, Yolanda Adams ndi Celine Dion …

  • @user-pg4qx3ng5l
    @user-pg4qx3ng5l4 ай бұрын

    Ndinyimbo ya Mulungu inde km munthu kuimba nyimbo yammbukhu mkumatchuka nayo ngat waimba ndiiiye sizimandinvekera bwino

  • @kattycampbell4802
    @kattycampbell48025 жыл бұрын

    Mau a Mulungu choncho, si chikhalidwe, sayansi kapena kulalikira pofalitsa uthenga wa zaka zikwi ziwiri zapitazo, koma vumbulutso la uneneri limene Mulungu analonjeza kwa m'badwo, ndipo ichi kudzera mwa munthu, m’neneri wam’thenga wamoyo wa kam'badwo kano. Ndipo mautumiki anayi a Aefeso 4:11 amawulutsa popanda kutsutsana nazo. [Mawu a Mkonzi: Msonkhano unati, "Ameni!] #ProphetKacouPhilippe

  • @memorychikumichaels2176
    @memorychikumichaels2176Ай бұрын

    ❤❤❤

  • @bernadettemunkombwe1800
    @bernadettemunkombwe1800 Жыл бұрын

    It touches my heart. Nice song.glad to be rcz.zambia.

  • @dakasainani5576
    @dakasainani5576 Жыл бұрын

    This very spiritually songs stay blessed

  • @annkarenmudzingwa556
    @annkarenmudzingwa556 Жыл бұрын

    It touches my soul... Lord is really grateful

  • @ChieftainLiganga
    @ChieftainLiganga3 ай бұрын

    Powerful song.

  • @zuluenny564
    @zuluenny564 Жыл бұрын

    I really missed the church service

  • @Lwendo.Jr2
    @Lwendo.Jr23 ай бұрын

    Mwe unkonge jesu umololo, ugwa ipyana, nine njege bo jujo, nine njege bo jujo, umolol' ugwa ipyana: Anyone know this song?

  • @parfaitkouassi5672
    @parfaitkouassi56725 жыл бұрын

    #pkpchaneltv 1. Ine ndatenga ndime yanga mmawa uno kuchokera pa Chivumbulutso 14: 6-10. Ndikuwerenga kuti: "Ndipo ndidawona m'ngelo wina alikuwuluka pakati-kati pa Kumwamba, wakukhala nawo Uthenga Wabwino wosatha, kuti akawuze iwo akukhala padziko lapansi, ndi kwa mtundu uliwonse, ndi fuko, ndi manenedwe, ndi anthu onse, Ponena ndi mawu akulu: Opani Mulungu, mpatseni ulemerero; pakuti ikudza nthawi ya chiweruziro chake; Ndipo lambirani kwa Iye amene adapanga kumwamba ndi dziko lapansi, nyanja ndi akasupe amadzi. Ndipo wina, m’ngelo wachiwiri, adamutsata, nati: Wagwa wagwa, Babulo Wamkulu, amene adawamwetsa amitundu onse vinyo wa m’kwiyo wa chigololo chake. Ndipo m’ngelo wachitatu adawatsata iwo, nanena ndi mawu akulu: Ngati munthu alambira chirombocho, ndi fano lake, nalandira chizindikiro pamphumi pake, kapena padzanja lake, adzamwanso za vinyo wa mkwiyo wa Mulungu, wokhetsedwa mu chikho cha m’kwiyo wake; Ndipo adzazunzidwa ndi moto ndi Sulfure pamaso pa angelo oyera ndi pamaso pa Mwanawankhosa."

  • @jeanlouisangelina4654
    @jeanlouisangelina46548 ай бұрын

    Am blessed

  • @kouassiyvonne8538
    @kouassiyvonne85385 жыл бұрын

    1. Monga aneneri a M’baibulo, mu Epulo 1993, ine, Kacou Philippe, mwamuna amene ndinali ndisanakhalepo ku mpingo, kupyolera m’masomphenya, ndinachezeredwa ndi M’ngelo amene anapereka kwa ine Uthenga wa kwa dziko lonse lapansi kukwaniritsa Mateyu 25:6 ndi Chivumbulutso 12:14. Iyi ndi nkhani ya kutembenuka kwanga, komanso masomphenya atatu a maitanidwe ndi utumiki wanga: 2. Ndinatembenuka mtima pa Epulo 24, 1993 molingana ndi Danieli 10:4 mpaka 11 kudzera m’masomphenya amene ndinadziona ndekha nditaima pa mchenga m’mbali mwa nyanja, kenako pamwamba pa piramidi yayikulu kenakonso pa mchenga wa m’mbali mwa nyanja mu malo ena ndipo ndinaona galimoto yachikale ya ankhondo ikutuluka kuchokera pansi pa nyanja ndikulowera chakumbuyo. Nditatembenuka ndinaona kuti munali anthu amoyo ndipo anali akazi okha-okha, mmodzi wa iwo anali wosakanizika mtundu. 3. Kenako nkhunda ziwiri zinabwera moyandikira kwa ine ndikubwereranso pamadzi. Ndipo panachitika kadamsana, ndipo munthu wamaonekedwe angati Mtambo atagwira lupanga anatsika kuchokera kumwamba ndi Mwana wa Nkhosa kenako kunawalanso. Iwo anaima pa madzi ndipo Mwana wa Nkhosa anayamba kulankhula nane m’chinenero chosadziwika. Phokoso la mawu ake litabwera mwa ine, ndinagwa, ndikufa, Moyo wanga unapita kukaima pa madzi ndi iwo pamene thupi langa linagona pa mchenga wa nyanja. Pamene Mwana wa Nkhosa yo anamaliza kulankhula nane moyo wanga unabwelera mu thupi langa ndipo ndinakhalanso moyo koma sindinawaonenso. 4. Kenako khamu la anthu linabwera kwa ine kuchokera kumbali ya kumanja ndipo ndinawafunsa ngati iwo adaona Mngelo ndi Mwan wa Nkhosa. Iwo anati, "Ayi!" Ndipo ine ndinati: "Koma, kodi simunaone Mngelo ndi Mwana wa Nkhosa ndi zinthu zonse Iwo achita?" Iwo anayankha kuti, "Ife sitinamuwone Mngelo ndi Mwana wa Nkhosa ndipo sitidamve Mawu Mwana wa Nkhosa wayankhula koma ife tikukhulupirira izo kwathunthu chifukwa chimene Mulungu anapatsa ndipo mdierekezi anatenga, chabwezeredwa kwa iwe". Nditayang'ana m’mwamba ndinaona makwelero atakhazikitsidwa pakati pa thambo ndi nthaka pamwamba pa madzi ndipo angelo akumakwera ndikutsika. Ndipo masomphenya anatha ndipo ndinamverera chimene tsopano ndikudziwa kuti ndi Mzimu Woyera ndipo ndinalira ndikukhulupilira Mulungu nthawi yomweyo. 5. Tsiku lotsatira cha m’ma 3 koloko masana pamene ine ndinali nditakhala ndi banja langa, ndinatengedwa kachiwiri mu masomphenya kupita kudziko la Ku chipululu chokha-chokha ndipo ndinaona chakum'mawa Mawu amene anali kutsika kuchokera Kumwamba m’mitambo. Atatha masomphenya awiriwa ndinanyamuka kupita ku mpingo kwa nthawi yoyamba. 6. Mu masomphenya achitatu, tinali chikhalire m'chipinda cholembera mayeso a msinkhu wapamwamba. Ndipo woyesa amagawa mapepala a mayeso. Ine ndinati kwa ine ndekha: "Kodi ndi chani chimene ine ndikuchita pano? Ine ndilibe muyezo wa sukulu wabwino ndipo kodi nanga ine ndilemba chani?" Ndipo kenako, ndinauzidwa kuti: "Njira yomweyo Maria anakhala woyembekezera mozizwitsa, popanda kudziwa mwamuna, njira yomweyo Mose analandira mwatsatanetsatane zimene zinachitika pa kalengedwe, iwenso, walandira mawu a moyo wosatha patsiku lino la Epulo 24, 1993 ndipo ichi chaikidwa ndi Mulungu. Pa nthawi yoikidwiratu, udzamvetsa ndikuphunzitsa zimene siwunaphunzire kotero kuti yense wokhulupirira ali nawo Moyo wosatha ". 7. KODI TSOPANO UTHENGAWU UKUTI CHIANI? Uthengawu ukunena kuti sitilinso mu nthawi ya madzulo koma pakati pausiku. Komabe uwu ndi m’mbadwo womwewo ndi Mzimu womwewo wa Eliya, koma Uthenga wa “ TSOPANO” umene uli wapamwamba kuposa uthenga wa nthawi ya madzulo [ Mkonzi: uthenga wa William Branham] Choncho Zekariya 14:7 ali kusiyana ndi Mateyu 25:6. 8. Uthenga uwu ukunena kuti bungwe la mipingo ya dziko lapansi, mabungwe a mipingo, mayanjano, migwirizano, zitaganya ndi migwirizano ya mipingo ... Chikatolika, mipingo ya chilamulo chakale, mipingo ya Chimethodisti, Eckankar, timagulu ta Horus, mipingo ya Chiluthera, mipingo ya Chianglica , Mahikari, mipingo ya Chibapiti , chi Rosicrucian, chiNazarene, chi Scientology, chi esotericism, mipingo ya chi Anabapiti, chivuduu, mipingo ya Chiadventi , makampani a yesu, mamishoni a chi Emmau, chi Inner Life, mboni za Yehova, mboni za Yesu, mipingo ya chi Foursquare. 9. Chipembedzo chotchedwa Freemasons, mipingo ya Chipentekositi, kulambira milungu ya Inca , mipingo ya Chipurotesitanti, chi Krishna, mpingo wa chiKhristu, kusinkhasinkha kwa chi transcendental, za chi Grail, aza mizimu, mipingo ya chiEvanjeriko, chiMormon, chiGuru Maharaja, Chisilamu ndi Chiyuda ndinso yonse mipingo yotchedwa yobvumbulutsidwa ndi yobwezeretsedwa ...misasa yopemphera, nyumba zokumanirana amuna, zokumanirana azimayi, mamishoni ndi mautumiki kuphatikizapo a Achibranham, uku ndiko kunena kuti, anthu amene adakali akutsatira Uthenga wa William Branham, ngakhale mu chiyero chake chonse, ndi puligatorio ndiwo makoka a Satana, otumizira anthu ku gehena ndipo mizimu yomwe imatumikira mumipingo imeneyi si Mzimu Woyera, koma ziwanda zodolola. Mizimu imeneyi ndi ziwanda zimene zinali mu mitsinje, zinkapezeka m'madzi, zigoba, vuduu, nkhalango ndi mitengo yopembedzedwa, zikhalidwe ndi miyambo ndiponso ndi imene inaukitsa ansembe a nsupa achikhalidwe. 10. Uthenga uwu ukunena kuti Chisilamu, Chikhristu ndi Chiyuda ndizo mizimu itatu ya chule mu Chivumbulutso 16:13. Zipembedzo zitatu izi zimati ndi za Abrahamu. Zipembedzo zitatu izi zimakhulupirira mwa Mose. Zipembedzo zitatu izi sizimakhulupirira mwa aneneri amoyo koma aliyense amadzinenera kuti ndi wa mneneri yemwe iyo sikumudziwa. Aliyense wa iwo ali ndi buku lake-lake loyera. Ndipo onse atatu akuyembekezera Mesiya. Iwo ali mizimu itatu ya chule mu Chivumbulutso 16:13. Uthenga ukukunena kuti zimenezi ndi ziwanda zimene zinaukitsa Elvis Presley, Bob Marley, James Brown, Madonna, Papa Wemba zimene lero zaukitsa magulu ndi oyimba a chikhirisitu monga Tabitha Lemaire, Don Moen, Exo Eclats, Yolanda Adams ndi Celine Dion …

  • @yaodjakacou4456
    @yaodjakacou44565 жыл бұрын

    Kc.2:11 Pamene mtumiki wam’thenga akutumizidwa kudziko lapansi, ndichifukwa chakuti palibe choonadi padziko lapansi ndipo uthenga wake ndiwo wokhawo woona wa nthawi yake. Iye ndiye choyimira cha choonadi. Iye ndi woweruza wa Mawu a Mulungu mu nthawi yake. Inu mukuwona? Pamene Nowa ankalalikira, palibe amene akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Nowa. Pamene Yeremiya ankalalikira, palibe amene akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Yeremiya. Pamene Eliya ankalalikira, palibe amene akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Eliya. Pamene Ambuye Yesu Khristu ankalalikira kumeneko m'misewu ya Yerusalemu, palibe amene akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Ambuye Yesu. Iye anati, "Palibe amene amabwera kwa Atate koma kupyolera mwa Ine." Inu mukuwona? Pamene Martin Luther anali kulalikira mu Germany, palibe yemwe akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Martin Luther. Pamene John Wesley ankalalikira, palibe yemwe akanakhoza kupulumutsidwa pa nkhope yonse ya dziko kupatula mwa Uthenga wa John Wesley. Pamene William Branham ankalalikira mu Amerika, palibe yemwe akanakhoza kupulumutsidwa pa nkhope yonse ya dziko kupatula mwa Uthenga wa William Branham. Ndipo lero inu simungathe kupulumutsidwa koma kupyolera mu uthenga wa m’neneri Kacou Philippe. Ngati inu munali mwana wa Mulungu m'nthawi yawo, inu mukanakhulupirira mwa iwo ndipo ndi zofanana lero.[mkonzi: wosonkhana anena, “Ameni! "].

  • @luisdomingosjosesinaportar6452

    @luisdomingosjosesinaportar6452

    Жыл бұрын

    Mentira....

  • @kouakoucynthia2827
    @kouakoucynthia28275 жыл бұрын

    14. Tsoka lalikulu la umunthu uko kunali kumasuka kolengezedwa kwa Hava, ndipo ngakhalenso lero ndi kumasuka kolengezedwa kwa mkazi ndipo icho tsopano achitengera ku kachisi.

  • @giftkamanga4646

    @giftkamanga4646

    4 жыл бұрын

    Amen

  • @user-ro6jj2sk2d
    @user-ro6jj2sk2d5 ай бұрын

    Amen

  • @johnchirwa4289
    @johnchirwa42899 ай бұрын

    Amen 🙏🙏

  • @owenbanda
    @owenbanda Жыл бұрын

    Nyimbo ya tanthauzo

  • @achillebehi1754
    @achillebehi17545 жыл бұрын

    #PKPCHANNELTV.1. Kinde ma jabila ma jakwenda nuti iwi ng’om, tie mesa mir ambadha man Ker mi Polo re ma gidwogo iwi ng’om. Man icopo ngo nibedo dhu mesa mir ambadha i Polo ndhu tek ilar ibedo dhu mesa mir ambadha m’ular ubedo iwi ng’om i ng’et jabila ma jakwenda mi thek dhanu m’utuk peri. Man icopo ngo nimondo ku yor i dhugola mi Polo, man nibedo i dhu mesa mir ambadha, ndhu ku nimondo ku yor i dhugola ma jabila ma jakwenda tie ku kifungula ne iwi ng’om.

  • @tonemuyaya6284
    @tonemuyaya62846 ай бұрын

    ❤❤❤❤ amen

  • @LovenessSakala-kx6zy
    @LovenessSakala-kx6zy5 ай бұрын

    ❤❤❤❤❤

  • @mdtiyad2844
    @mdtiyad2844 Жыл бұрын

    Amen and amen

  • @yaobleestelle2513
    @yaobleestelle25135 жыл бұрын

    40. Abale a ku Africa, Asia, Europe ndi America! Inu mwina munali kuyembekezera Uthenga wa Mateyu 25:6 mwinamwake mu dziko lanu koma Mulungu anachita izo mosiyana. Kumbukirani Ambuye wathu Yesu Khristu! Pokhala mkulu wa ansembe Melkizedeki, achirabi ndi alembi anaona kuti Iye adzachokera ku fuko la Levi. Koma Iye adachokera ku fuko la Yuda. Ndiye, Uthenga Wake ndi ntchito Zake zinatsimikizira kuti Iye anali Mesiya. Ndipo lero pa nkhope yonse ya dziko lapansi, ngati iwe uli mwana wa Mulungu, malo ako awa ali pano ndi m’neneri wa nthawi yako, M’neneri Kacou Philipe. Ndipo amene ali ndi makutu akumva amve.

  • @JorgeMarqueschathobwa-sn1we
    @JorgeMarqueschathobwa-sn1we10 ай бұрын

    Pitilizani kuipatsa moto

  • @BrandnerSakala
    @BrandnerSakala2 ай бұрын

    0

  • @thandijuma9503
    @thandijuma95037 ай бұрын

    Amen