Ali mu njira by Great Angels may his soul rest in peace .Pepani akubanja
Okhala akumtundu malomopanga zoti ayikoke khaki kuti tikafike paradise akuziwapodi kathu
You are doing a good job, koma muzitsitsako background song. #Phokoso kwambiri#
Ambuye muwapatse anthu akufa chiusiro chosatha ndipo kuwala kosatha kuwalitse maso wano ause ndi ntendere...amem
Pepani wofedwa pepani mzimu wa malemu uwuse mutendere AMEN
Ndangoyiona kumene nkhani yomvetsa chisoniyi.Mzimu wa mnyamata ameneyu upitilile kuusa ndi mtendere. Pepani akubanja.
Si matsenga ayi ingakhale kuti yamupititsa ku Malo ake amene imakhala
Bamboyu ndi mfiti. Akudziwapo kanthu.
Zosakhara buinoi Mzimu wake uwuse muntendere .zinazo musiireni mulungu muini zonse
Palibe zamuwanthu apa. Aliyese amadziwa kut ng'ona ndichilombo. Ine SI wakumeneko koma nkhaniyi ikudzinena yokha palibepo ufiti apa. Ifa yowawa ndithu ndipo zandikhudza .Mulungu amuyang'anire
Abambowa awa andiyankhira mwa mzeru kwambil. Everything osamangoti zamuwanthu kod bwanji sitifuna kuvomereza
Ambuye akufungatileni nonse anamfedwa
Sizawathu nthawi basi inakwana munthu aliyense Mulungu adamulembera zithu zitatu 3 .chayamba kubadwa, 2 kukhala ndimoyo,chachitatu 3imfa
😭😭😭😭 pepani abale imfa iyi simayiwalika ,nafe zinationekera 2022 yi mpaka lero ,
Sadness 😢
Pepani pepani imfa zotelezi zimakhumudwisa kwa anthu osala komaso chiopsezo chifukwa anthu amaopa kuchita zinthu zikafika potere
Komano osathamangisa kuti zamasenga chifukwa ndavamo kuti ming'ona irimo menemo
Da guy in water he know what is going on?
Next time low the volume of background song
Thanks for information
Zachisoni kwambili
A Govate ulemu wanu ntchito mumaigwira tikuonera nao kuno ku malawi 🇲🇼
Sizoona khani yachisoni kumasekelera ngati ya ukwati bambo inuyo mwandikwisa mwachita chimo😭😭😭
bambo awa akuti sizamuwathuwa akuziwapo kathu
Zosakhala bwino koma pepani anafedwa mwana muzimu wake owuusa mtendere
Bambo awa akuti sizamwawathuwa akuziwapo kanthu za ifa ya mwana ameneyu ndithu
Sory anamfedwa nonse. Zosayenda ndithu nzimu wake uwuse mumtendele
Bambo uyu akuziwapo kanthu ndinthu mwinaso ndi yemwe wapeleka mwana ndinthu mulungu odziwa kulanga walange onse agwira ntchito pa mwana
aaa zosakhala zandivetsa chisoni
Pepani anamalira nonse😭😭😭
bambowa akuti sizamuwathuwa akutanthauza kuti Chan akuziwapo kathu chifukwa khani yachisoni kumasekelera ngati ya ukwati koma kulakwa 😭😭😭😭😭💔💔
Inesotu ndikudabwa nawo ndy paja poti amati khondo nd anasi
Zovuta mmm
😢
Zosakhala bwino pepani akubanja komanso a BS channel potidziwitsa
Zosakhala bwino
Pepani pepani
Pepani
Koma abale zovutatu izi
Mudzi uliwonse umakhala ndimunthu ofunika panthawi yake
Pepani kwambiri chonde nyimbo muzisisako ndithu kuti mau azimveka
OK , zanveka , zikomo kwambiri
Zomvetsa chisoni ndithu 😭😭😭😭😭😭😭
Mwini mbumbayo wandikaikisa
Ifaikutenga ana an,gono pepan kwambiri mzimu wake uunse muthendere😭😭
Abale bambowa anena mwazelu tisamagoti zamasenga ai mulungu ifa anaivomeleza bwanji timakaika tonse tizafa ndithu
Пікірлер: 47
Ali mu njira by Great Angels may his soul rest in peace .Pepani akubanja
Okhala akumtundu malomopanga zoti ayikoke khaki kuti tikafike paradise akuziwapodi kathu
You are doing a good job, koma muzitsitsako background song. #Phokoso kwambiri#
Ambuye muwapatse anthu akufa chiusiro chosatha ndipo kuwala kosatha kuwalitse maso wano ause ndi ntendere...amem
Pepani wofedwa pepani mzimu wa malemu uwuse mutendere AMEN
Ndangoyiona kumene nkhani yomvetsa chisoniyi.Mzimu wa mnyamata ameneyu upitilile kuusa ndi mtendere. Pepani akubanja.
Si matsenga ayi ingakhale kuti yamupititsa ku Malo ake amene imakhala
Bamboyu ndi mfiti. Akudziwapo kanthu.
Zosakhara buinoi Mzimu wake uwuse muntendere .zinazo musiireni mulungu muini zonse
Palibe zamuwanthu apa. Aliyese amadziwa kut ng'ona ndichilombo. Ine SI wakumeneko koma nkhaniyi ikudzinena yokha palibepo ufiti apa. Ifa yowawa ndithu ndipo zandikhudza .Mulungu amuyang'anire
Abambowa awa andiyankhira mwa mzeru kwambil. Everything osamangoti zamuwanthu kod bwanji sitifuna kuvomereza
Ambuye akufungatileni nonse anamfedwa
Sizawathu nthawi basi inakwana munthu aliyense Mulungu adamulembera zithu zitatu 3 .chayamba kubadwa, 2 kukhala ndimoyo,chachitatu 3imfa
😭😭😭😭 pepani abale imfa iyi simayiwalika ,nafe zinationekera 2022 yi mpaka lero ,
Sadness 😢
Pepani pepani imfa zotelezi zimakhumudwisa kwa anthu osala komaso chiopsezo chifukwa anthu amaopa kuchita zinthu zikafika potere
Komano osathamangisa kuti zamasenga chifukwa ndavamo kuti ming'ona irimo menemo
Da guy in water he know what is going on?
Next time low the volume of background song
@balancosemanalckgovate8464
7 ай бұрын
Thanks for information
Zachisoni kwambili
A Govate ulemu wanu ntchito mumaigwira tikuonera nao kuno ku malawi 🇲🇼
Sizoona khani yachisoni kumasekelera ngati ya ukwati bambo inuyo mwandikwisa mwachita chimo😭😭😭
bambo awa akuti sizamuwathuwa akuziwapo kathu
Zosakhala bwino koma pepani anafedwa mwana muzimu wake owuusa mtendere
Bambo awa akuti sizamwawathuwa akuziwapo kanthu za ifa ya mwana ameneyu ndithu
Sory anamfedwa nonse. Zosayenda ndithu nzimu wake uwuse mumtendele
Bambo uyu akuziwapo kanthu ndinthu mwinaso ndi yemwe wapeleka mwana ndinthu mulungu odziwa kulanga walange onse agwira ntchito pa mwana
aaa zosakhala zandivetsa chisoni
Pepani anamalira nonse😭😭😭
bambowa akuti sizamuwathuwa akutanthauza kuti Chan akuziwapo kathu chifukwa khani yachisoni kumasekelera ngati ya ukwati koma kulakwa 😭😭😭😭😭💔💔
@Joy-zx3lv
7 ай бұрын
Inesotu ndikudabwa nawo ndy paja poti amati khondo nd anasi
Zovuta mmm
😢
Zosakhala bwino pepani akubanja komanso a BS channel potidziwitsa
Zosakhala bwino
Pepani pepani
Pepani
Koma abale zovutatu izi
Mudzi uliwonse umakhala ndimunthu ofunika panthawi yake
Pepani kwambiri chonde nyimbo muzisisako ndithu kuti mau azimveka
@balancosemanalckgovate8464
7 ай бұрын
OK , zanveka , zikomo kwambiri
Zomvetsa chisoni ndithu 😭😭😭😭😭😭😭
@chifunirogoliat4630
7 ай бұрын
Mwini mbumbayo wandikaikisa
Ifaikutenga ana an,gono pepan kwambiri mzimu wake uunse muthendere😭😭
Zosakhara buinoi Mzimu wake uwuse muntendere .zinazo musiireni mulungu muini zonse
@ChrissyKazinga-jd8dx
7 ай бұрын
Abale bambowa anena mwazelu tisamagoti zamasenga ai mulungu ifa anaivomeleza bwanji timakaika tonse tizafa ndithu