MCP Kumangochi Yayaka Moto

MCP Kumangochi Yayaka Moto

Пікірлер: 71

  • @KateRose-sh8zl
    @KateRose-sh8zlАй бұрын

    Azimai saganiza zamavuto alipo ndife opusa kwabasi

  • @unarinematshomo2841
    @unarinematshomo2841Ай бұрын

    Ko ma njala imeneyi kumakhala busy ndichakweraso😂😂😂😂😂 Amalswi si muli serious 😂😂😂

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4vАй бұрын

    Mahule. Osowa amuna awa mwina awonedwe usilu watundu wanji uwu

  • @ChiyembekezoPhiri-sv8nw
    @ChiyembekezoPhiri-sv8nwАй бұрын

    Ndi ufulu wawo basi asiyeni tikumana 2025

  • @edmorswalley6663
    @edmorswalley6663Ай бұрын

    Mabadzi Apita apa 😅😅😅

  • @JoshuaNyirongo
    @JoshuaNyirongoАй бұрын

    Asamangodya zomba bwanji.

  • @FaisonLukiyo
    @FaisonLukiyoАй бұрын

    Wadya omweu chakwera 😊

  • @BiasElliot
    @BiasElliotАй бұрын

    Chuma chomadya ena, osauka busy ku vina. aaaaa zomvetsa chisoni kwambili

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873Ай бұрын

    Umbuli kumalawi sudzatha anthu ngati akuyimbira kuvinira mutsogoleri wopanda tsogolo mukuganiza ziko lingasinthe mbuli ndizambiri kumalawi

  • @user-dv7ht6vn9s
    @user-dv7ht6vn9sАй бұрын

    Dyera.... Ma K2000 basi😂😂😂

  • @BerlindaJetel
    @BerlindaJetelАй бұрын

    Moto wake mukunenao ndiuti wayakao

  • @user-oq5rg5mz7q
    @user-oq5rg5mz7qАй бұрын

    Nkazi wayine never kupita kusongano wa MCP

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomoleАй бұрын

    Kukhala mkaziwanga ndimve kuti analikomweko kukamuchapa makofi kunyumba uku mkupusa zedi .

  • @user-sv2vc7ie2m
    @user-sv2vc7ie2mАй бұрын

    Zaziiii chimenechiso ndi chipani kusasa Mai mukatero mukagone ndinjala

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6dАй бұрын

    Azimai ovetsa chisoni kwambili mmm koma

  • @user-jn7bt1uy5s
    @user-jn7bt1uy5sАй бұрын

    Nambo kwereko

  • @victorauwana7258
    @victorauwana7258Ай бұрын

    Anakawatenga kulilongwe kukawavinisa ku mangochi... Amangochi sangapange manyi ngati awa

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2dАй бұрын

    Zisilu agalu chosecho mwagona ndi njala mulibe sugar kufela 2 pin mahule

  • @GodsonLindan-hn4kp
    @GodsonLindan-hn4kpАй бұрын

    Koma umphawi siwabwino , anthu akuvutika ndikukwera mitengo yazinthu ,ndikumamchemelera.ana awo sukulu ikulepheleka kulipila ,ayi awa popeza anawo amakhala kowenza mnsomba.

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711Ай бұрын

    Aaaaa mangichi

  • @charlesnanthambwe1832
    @charlesnanthambwe1832Ай бұрын

    Mbuzi za dzimayi

  • @owenskabazanechiumia3543
    @owenskabazanechiumia3543Ай бұрын

    Koma ndiye Umphawi ndivuto lalikulu, Komanso Kamuzu anatipusitsa Azimayi achimalawi ndiotengeka ndi zaziii Anthu akuwawona awawika mumavuto ndiiwowo, koma nkuapasa so sapoti kuti apitilize kugwetsa Malawi mpaka tione K20000 note zomvetsa chisoni pa Mangochi apo.

  • @FaisonLukiyo
    @FaisonLukiyoАй бұрын

    Auawo sagwira ntchito

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3iАй бұрын

    Mmmmmmmm moto wake uti poti akufuna kuti awadyere ndalama zomwe akubanzo, ndi wa kumangochinso

  • @user-ti2ct8ts8d
    @user-ti2ct8ts8dАй бұрын

    Zitsiru kuvinila chitsilu chinzawo

  • @user-ww9rj2wx8d
    @user-ww9rj2wx8dАй бұрын

    Zakutumbo basi kusowa zochitatu uku hiyaaaa

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6rАй бұрын

    Mcp mito kuti buuuu❤❤❤

  • @usumanidaudi
    @usumanidaudiАй бұрын

    Inuso a hanifa mwayamba kujama ya mcp anthu atatuwo paka kwawonesa apa muzawona apm pa 12 pano

  • @BonganiCharles-ju4ty
    @BonganiCharles-ju4tyАй бұрын

    Azimayi angododoloka zili zonse maka achiyao eeeee mavuto kufika kunyumba kungo ona poto wauma

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cnАй бұрын

    Mmmh shame on you mangochi women😢

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pwАй бұрын

    Ayao a 2 sim awa not a 1 sim .muyao wa original angamasapote idzi

  • @user-dh8ml4bv4w
    @user-dh8ml4bv4wАй бұрын

    Azimayi Ali ndiivuto kutengeka zaziiii

  • @APOSTLEBJ-tc5fp
    @APOSTLEBJ-tc5fpАй бұрын

    Ayao alibe nzeru alibe kaya chifukwa cha umbuli wosapita ku school kaya.mcp idapha ndi kuwocha nyumba za anthu aku mangochi ku malindi kwa amoto pofuna kumupha chipembere koma lero ayao ndikumasapota mcp zoona?

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8oАй бұрын

    Mzakhumudwa even mavoti a 2025 a chakwera azawinanso kwambilinso

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8oАй бұрын

    Pa Malawi mpovuta ena akulila ena avotela yemweyo chakwera

  • @BerlindaJetel

    @BerlindaJetel

    Ай бұрын

    Kkkk etietii zomvesa chisoni

  • @LovelyBlini-cu3iu
    @LovelyBlini-cu3iuАй бұрын

    Ena ndi obwela MCP ndiyochenjera apasidwa ma 5pin adyeleni

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823Ай бұрын

    Azimayi amenewa Ali ndi ma banja ndithu koma, zitsilu za wanthu

  • @isaaczuze
    @isaaczuzeАй бұрын

    Zisilu za anthu ndipo ndakhumudwa kwambili😊

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214Ай бұрын

    Komatu azimayi polani moto kwanuko zikuyenda anzanthu ayi zikomo 💔💔💔

  • @innocentissah2636
    @innocentissah2636Ай бұрын

    Zitsiru kuvinira mbava ngati akudya mmakwawo

  • @user-ql7ik4mw6p
    @user-ql7ik4mw6pАй бұрын

    Umbuli.kudzapita.kusukulu.ndizimene.zikufuta

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711Ай бұрын

    Mangochi nsimungawine MCP loko patamvuta bwanji mungodzita anthuwo akuyimba chimene akamvotele akuchidziwa siyaguletu awa adzingokudyelani k5000 pin chitsango akudziwa mamvuto akomana nawo zaka 4 ulamulilo wa MCP ndi UTM mwadxudza dzedi iiiiiii

  • @AdamAPhiri
    @AdamAPhiriАй бұрын

    Ndiye yayaka moto di. Mangochi ndi Mangochi yo anthu ake amenewo kkkkkkkkkkkk Zomvetsa chisoni.

  • @usumanidaudi
    @usumanidaudiАй бұрын

    Inu mangochi sipanga zachibwana akungofuna ndaramayo basi osati angavotere mcp asa chakwera ndi fiti

  • @violetmahachi7673
    @violetmahachi7673Ай бұрын

    Abeleni abwera okha oskana ndalama

  • @edenngoma8214
    @edenngoma8214Ай бұрын

    Who is here with me

  • @goodvisionmedia2023
    @goodvisionmedia2023Ай бұрын

    30 people only

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2dАй бұрын

    Anthu ovesa chisoni kuvinila mbava chosecho akugona ndi njala koma umphawi ndi wa chabe 2 pini basi anga gule chani sugar yemwe sikwanaso echeee

  • @BerlindaJetel

    @BerlindaJetel

    Ай бұрын

    zitsiru zaanthu

  • @APOSTLEBJ-tc5fp
    @APOSTLEBJ-tc5fpАй бұрын

    Koma zakuti sugar akugulitsa K6000 akuziziwa koma ayaowa?

  • @buttbutt6690

    @buttbutt6690

    Ай бұрын

    Iweyo opuza😅😅

  • @edenngoma8214
    @edenngoma8214Ай бұрын

    Waiting

  • @phirimacdonald8638
    @phirimacdonald8638Ай бұрын

    Wakupasani ma k2000 wakulakwilani mudya matsiku angat? Paja azimayi mmatipwetekesa kwambiri

  • @marryphili5419
    @marryphili5419Ай бұрын

    Zisiru za azimayi izi shame on you mukhawura ndi njara Chaka chake ndi chino

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4pyАй бұрын

    Awawo sakumvutika Sali Malawi momomwemo amzimai opanda zochita taweremukani muchangamuke kusaphuzira sikwabwino ndithu

  • @isaaczuze
    @isaaczuzeАй бұрын

    Koma ndichifukwa chiyani abale ....anthu tikuvutika koma kumachemelela chakwera ....Kaya ndi umbuli koma mavuto alipo .....ma 5000 akupasaniwo akubweleselani mavuto osati masewela ......

  • @user-lf6qf2tw5o

    @user-lf6qf2tw5o

    Ай бұрын

    Uchisiru

  • @LukaAron-el5qh
    @LukaAron-el5qhАй бұрын

    Koma azima ndichani mukuchita zoonadi kusowa kwanu chochita pochoka pompo mimbamo njala yokhayokha

  • @JackMvura-ik2td
    @JackMvura-ik2tdАй бұрын

    Palibe ogwetsa MCP maka chilima akaima payekha nankhumwa payekha basi DPP yathapo azimai alindi mphamvu awuza azimuna awo kuti bambo sapoteni tambala wakuda

  • @Chiso2019
    @Chiso2019Ай бұрын

    Azimai okhaokha bwa?

  • @Pangolinimw

    @Pangolinimw

    Ай бұрын

    anyamata safuna sauzilu

  • @user-hd6xc5ud2b
    @user-hd6xc5ud2bАй бұрын

    Zisilu ndithu

  • @beinhardkausiwa7107
    @beinhardkausiwa7107Ай бұрын

    Kunali mnsonkhano?

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4scАй бұрын

    Anthu ache atatuwa.asogoleli,alipowa akuchiononga,chipani cha kamuzuchi.bolatso, mwini wache chifukwa iyeyo,safuna amalawi azigona ndi njala olo adzigula sugar K5000

  • @eliffagondewe8214

    @eliffagondewe8214

    Ай бұрын

    Shame on you azimayi kwanuko zikuyenda eeti💔💔

  • @user-nn9bg3ve3g

    @user-nn9bg3ve3g

    Ай бұрын

    A Malawi anthu womvetsa chisoni kwambiri amagulidwa ndi 2000

  • @HarrisonMwanga-xy4sc

    @HarrisonMwanga-xy4sc

    Ай бұрын

    @@eliffagondewe8214 azimai kwathu kuno anasiya,anachangamuka,bola anganati azibvina ili UDF olo afford.

  • @HarrisonMwanga-xy4sc

    @HarrisonMwanga-xy4sc

    Ай бұрын

    @@user-nn9bg3ve3g kkkkkkkkk malawi ziko lolemela kwambili,koma olemela ache ndi azitsogoleli.ku kalonga sugar K6000 pomwe ena akuthamangila andale omweo akuononga malawiwo'kumaomba manja.malawi,poyamba anali the home❤️of Africa lero shame

  • @IdaCMwale

    @IdaCMwale

    Ай бұрын

    Ndi ufulu wawo azimai asiyeni