Kuyakhula mosaopa Chakwera wamupha Chilima. Chifukwa cha udindo
Жүктеу.....
Пікірлер: 185
@user-fm8ed7eo3i7 күн бұрын
Akulu eeee apa pa kanakhala kuti Pali anthu 10 ngati inu ayi dziko bwenzi likuyenda bwino. I like your style brother ❤
@NgomaRaheem15 күн бұрын
Manganya ndi mfiti yotheratu ndagwilizana nazo
@user-do2cs8nf4b7 күн бұрын
Mizimu ya wonse omwe adawapha pa ngozi ya ndege ija iwanzunzedi anthu amenewa
@Trancy-xt4py15 күн бұрын
Posatengera CHIPANI chilima adachita kuphedwa kumene achakwerawo akudziwa Koma pot CHOIPA chimakanidwa sangamvomere Koma MULUNGU akudziwa
@DorrahBanda
7 күн бұрын
Zoona
@VeronicaChirwa-ct4os15 күн бұрын
Mwandiyankhulira bwino kwambiri. Ama radio onse sakuthandiza a Malawi. Kulephera kunena chilungamo zoona??? Amalawi muzichangamuka please!!! Ku Church ko mumapemphera chani? Ama Wailesi simunathandize or pang'ono, ndipo tataya nanu chikhulupiliro ma Radio 📻 oyipa panokha.
@manfredzalirabetha2440
6 күн бұрын
Ma radio osathandiza a mmalawi muno bola limpopo basi iyaa
@user-be5fc3ed1i
2 күн бұрын
Bora Limpopo FM yoha basi komanso ndi imene inasegula maso amalawi kuti ndege yagwera kuchikanga komaso anthu amwalira shame mawayiesi oyima panokha Lero ndimasiya kalekae kunvera hot current.yanga ndi Limpopo FM, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo
@MercyKachenje15 күн бұрын
Mau amphavu awa vuto anthufe nsanje too Mulungu apitilize kitiululira zinsisi
@LamieTiger15 күн бұрын
Vuto ndilot athu ena akuikira kumbuyo athu afitiwa athu ot akudalira mitsokho yathu Kut antchedwe olemera mipando akupheranayo nditimisokho tathu toja deleri kuzolowela Moyo osagwira ntchito Moyo opatsidwa zaulele chakwera wayetsa Kuno Ku church Kut udzilandila chakhumi mabatile ako
@GiftKananji15 күн бұрын
But how manganya did this? he looks like a sheep but he is a bad person, here Boni Kalindo is being punished because of this man eish that's very sorry
@ThomasKaphwiti12 күн бұрын
Ndipo manganya siwakuno mayi ake ndi aku Zimbabwe muzikaona kuchenjera ngt akuba nkhuku😅😅
@samueljuma4452
6 күн бұрын
Kkkkkkk ngati akuba nkhuku???koma ndaseka
@ChimwemweBottomani-hc5ju5 күн бұрын
I was wondering how mr michael usi allow to bi a vice president as he was a vice president to late chilima😢😢 we was all.shocked to bi honest usi sanaganize bwino ...indeed they need to comfess ngati amakhulupiliradi Mulungu ....i salute you my brother n may u always bi protected
@PaulMinofu15 күн бұрын
On point❤❤❤❤
@OsmanBakali-s5x7 күн бұрын
💔💔💔💔mpaka pano ineyo ndmangoona ngati a CHILIMA alipo sanamwalire ai.. I will still missing him in my heart ❤️ forever 😭😭😭
@InnocentMlowoka-ew4lo15 күн бұрын
Chilungamo kuwawa
@FrynessMoyo-to2du7 күн бұрын
Amene anapha chilima panya pake 😢😢😢
@cacksygustarf626014 күн бұрын
Voice ya nzeru❤
@user-yo9rw8tr4s15 күн бұрын
Dosanama munthu Uyo walankhula mau wogwilika kwambile
@BensonChilundu7 күн бұрын
Micheal Usi ndi munthu ozikonda kwambiri.zoona zake zaoneka zokha chifukwa iyeyu sakadalolera kukhala Vice President.Koma abale ndalama zovuta ndithu
@YusufuKaifa-fr4wt7 күн бұрын
❤❤❤❤❤❤my point president chakwera out
@user-dp7bc7yy6s14 күн бұрын
Muli speech yamphavu ndipo boma ili Mulungu achite nanu
@mollymasangano4733 күн бұрын
Well spoken my brother we can't keep Quite on what happened in our National, we are still mourning all who died on that day ,it SAD.
@HameedahMasambuka15 күн бұрын
Ndipo kukumangan inuyo. Ndizakhala numbar one kusonkha ndalama yokuombolelan mmmmmmm
@user-jn2oc3cn3q
7 күн бұрын
Kkkk km support iyi
@user-be5fc3ed1i
2 күн бұрын
@@user-jn2oc3cn3qkkkkkkk kwachema
@user-be5fc3ed1i
2 күн бұрын
Chilungamo chiyende ngati madzi 😂😂😂
@ThomasKaphwiti12 күн бұрын
Ndipo zoona tatiyeni a Malawi tionetse mkwiyo wathu Maliro ndiye tinayika kwa tsalano tithane ndizigawengazi😢😢😢😢
@FrynessMoyo-to2du7 күн бұрын
Manganya ndi fiti panya pamake plus chakwera 😢😢
@MtokomaYohane7 күн бұрын
And is true chakwera akukhunzidwadi and i have more questions
@paulinekayuni16217 күн бұрын
As for radio and tv extension I can agree I was expecting too for them kupangitsa conference yofusa mafuso representing people mafuso amene akufusa. Koma zinazo kaya
Manganya mpando kumeneko sanjoya akachita chibwana mkwiyo wa Mulungu umukantha koopsa tikupempheratu magazi a Chilima aja ayankhula usazione ngati wachenjera
@FelisterNgwira-op7rr14 күн бұрын
Deotoronomy 29 ; 29 verse the secret things belong unto the Lord our God: but those things which are revealed belong unto Us and to our children ever, that we we may do all the words of this law
Kkkkk mimba zilikhutchu Ngati ogulitsa tomato oola kkk Koma big man
@InnocentnMbale-zq8pk15 күн бұрын
Ndipo Inu eee ziko ili likupita kuti ndipo ine zundiwawa ndisaname ngati ndikufa ndife koma kumalawi anthu tili ndi mantha kwambiri
@FrynessMoyo-to2du7 күн бұрын
Amalawi ndi amantha size😢😢😢
@YasinMusa-ym8lp7 күн бұрын
Chichakwera chakupa galu wacha be chabe kupa andu osa lakwa chaka chamawa ndipa fup mtikumana mbusi simenesi achakwera 😢😢
@harrisbanda589111 күн бұрын
Kulankhula chilungamo mopanda kuopa
@user-be5fc3ed1i2 күн бұрын
Tiyeni tisiye kumvera ma wayilesi akumalawi chifukwa wonse anaguidwa kale Bora Limpopo FM radio, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo
@user-do2cs8nf4b7 күн бұрын
Koma nde zoonadi ndithu watsala iyeo akuwona ngt sadzafa
@user-oc9vl9xz8e5 күн бұрын
Zimenezi amalawi onse akuziwa zimenezi koma akuopa kuyankhula chilungamo monga chimenecho Mulungu akuteteze kuti upitilize kutiya khulila ku Mtundu wathu..
Пікірлер: 185
Akulu eeee apa pa kanakhala kuti Pali anthu 10 ngati inu ayi dziko bwenzi likuyenda bwino. I like your style brother ❤
Manganya ndi mfiti yotheratu ndagwilizana nazo
Mizimu ya wonse omwe adawapha pa ngozi ya ndege ija iwanzunzedi anthu amenewa
Posatengera CHIPANI chilima adachita kuphedwa kumene achakwerawo akudziwa Koma pot CHOIPA chimakanidwa sangamvomere Koma MULUNGU akudziwa
@DorrahBanda
7 күн бұрын
Zoona
Mwandiyankhulira bwino kwambiri. Ama radio onse sakuthandiza a Malawi. Kulephera kunena chilungamo zoona??? Amalawi muzichangamuka please!!! Ku Church ko mumapemphera chani? Ama Wailesi simunathandize or pang'ono, ndipo tataya nanu chikhulupiliro ma Radio 📻 oyipa panokha.
@manfredzalirabetha2440
6 күн бұрын
Ma radio osathandiza a mmalawi muno bola limpopo basi iyaa
@user-be5fc3ed1i
2 күн бұрын
Bora Limpopo FM yoha basi komanso ndi imene inasegula maso amalawi kuti ndege yagwera kuchikanga komaso anthu amwalira shame mawayiesi oyima panokha Lero ndimasiya kalekae kunvera hot current.yanga ndi Limpopo FM, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo
Mau amphavu awa vuto anthufe nsanje too Mulungu apitilize kitiululira zinsisi
Vuto ndilot athu ena akuikira kumbuyo athu afitiwa athu ot akudalira mitsokho yathu Kut antchedwe olemera mipando akupheranayo nditimisokho tathu toja deleri kuzolowela Moyo osagwira ntchito Moyo opatsidwa zaulele chakwera wayetsa Kuno Ku church Kut udzilandila chakhumi mabatile ako
But how manganya did this? he looks like a sheep but he is a bad person, here Boni Kalindo is being punished because of this man eish that's very sorry
Ndipo manganya siwakuno mayi ake ndi aku Zimbabwe muzikaona kuchenjera ngt akuba nkhuku😅😅
@samueljuma4452
6 күн бұрын
Kkkkkkk ngati akuba nkhuku???koma ndaseka
I was wondering how mr michael usi allow to bi a vice president as he was a vice president to late chilima😢😢 we was all.shocked to bi honest usi sanaganize bwino ...indeed they need to comfess ngati amakhulupiliradi Mulungu ....i salute you my brother n may u always bi protected
On point❤❤❤❤
💔💔💔💔mpaka pano ineyo ndmangoona ngati a CHILIMA alipo sanamwalire ai.. I will still missing him in my heart ❤️ forever 😭😭😭
Chilungamo kuwawa
Amene anapha chilima panya pake 😢😢😢
Voice ya nzeru❤
Dosanama munthu Uyo walankhula mau wogwilika kwambile
Micheal Usi ndi munthu ozikonda kwambiri.zoona zake zaoneka zokha chifukwa iyeyu sakadalolera kukhala Vice President.Koma abale ndalama zovuta ndithu
❤❤❤❤❤❤my point president chakwera out
Muli speech yamphavu ndipo boma ili Mulungu achite nanu
Well spoken my brother we can't keep Quite on what happened in our National, we are still mourning all who died on that day ,it SAD.
Ndipo kukumangan inuyo. Ndizakhala numbar one kusonkha ndalama yokuombolelan mmmmmmm
@user-jn2oc3cn3q
7 күн бұрын
Kkkk km support iyi
@user-be5fc3ed1i
2 күн бұрын
@@user-jn2oc3cn3qkkkkkkk kwachema
@user-be5fc3ed1i
2 күн бұрын
Chilungamo chiyende ngati madzi 😂😂😂
Ndipo zoona tatiyeni a Malawi tionetse mkwiyo wathu Maliro ndiye tinayika kwa tsalano tithane ndizigawengazi😢😢😢😢
Manganya ndi fiti panya pamake plus chakwera 😢😢
And is true chakwera akukhunzidwadi and i have more questions
As for radio and tv extension I can agree I was expecting too for them kupangitsa conference yofusa mafuso representing people mafuso amene akufusa. Koma zinazo kaya
Iponden fadah 🎉
Inu mwayakhula mawu ife tikuwopa kuyakhulapo mwatilakhulira mulungu awakanthe kopotsa
The power of massage and the power of prayer indeed
Sanayankhuleponso amangophwisa mkhutu wa udindo usi
Mulungu akuona zonse,,, ndipo samagona tulo. 😭😭😭😭😭
Manganya mpando kumeneko sanjoya akachita chibwana mkwiyo wa Mulungu umukantha koopsa tikupempheratu magazi a Chilima aja ayankhula usazione ngati wachenjera
Deotoronomy 29 ; 29 verse the secret things belong unto the Lord our God: but those things which are revealed belong unto Us and to our children ever, that we we may do all the words of this law
Mau amphamvu
Inu ndiye mwanena zoona brother mmmmmh ulemu wanu Inuyo shaaaa Ndamva nanu kukoma zedi❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Not all days are Sundays God is watching and may there souls rest in peace 🙏
Powerful message Duuu may their souls rest in peace ✌️
U are talking sense
Koma izizi tu we are praying kuti Mulungu alange aliyense amene anatenga gao lokupha chilima pompano asadikile chiweluzo
So heartly broken dear
Yesu anapelekedwa chifukwa cha ndalama yochepa,God have mercy
Nawoso mayiko usi mbusi yamunthu kukonda ndalama kumeneko mpaka kulolela Kuti munthu ampedwe ndalama abale God bless you mukutidzegula mithu
Chi Michael usi manganya that why amuika pa mpando iyeyo kuthamanga kukakwera pa mpando pakamaso gwaaaaa manganya
It's true my brother that's sad
Zoona ❤❤❤❤❤❤❤
Yes may God perform wonders that the truth must prevail
Osaopa osafooka tizafera mbendera yathu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Bakili muluzi tv yekha akalowa kumwamba bro kuyankhula mowonatu
You will pay for it, what's wrong did our SKC do to you😭😭😭😭😭 the day will come 😢😢😢
manganiso anu ameneyo okay alibwino
Basi poti kulibe mulandu okupha ndimphezi ...mudiyeni chakwelayo azasowa omusumila
Osaopa osafooka tiime pa chilungmo dziko lino nditose ndopo mbendera yake ndiii🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼situkukuopami😢😢😢😢
Chilima anaphedwa chifukwa cha jealousy eishiii Malawi will never change for better.
Enanu mudakangosiya kucommenter Ngati sizikukumvekelani bwino Ife nde tikumva kusekemela chipepeso chathu timachipeza kuzela kwaanthu amenewa chilima wathuuuu tizamfela
Zoonadi manganya ndi munthu oipa sanayakhulapo za imfa ya chilima
Ndi Ana omwe akudziwa
Zoona awa ndiye mau bro end I love you so much brother ❤🎉🎉
Ambuye tipheleni Chakwera 😂😂😂😅😅😅
@Hellenistic109
7 күн бұрын
AMEN 🙏
Ndpo mabala akutiwaw
Ameni amen misonzi ya wanthu osalakwa simapita pachabe
Zoonadi brother ife tikulira ndithu esh infa ya chilima mmmm😢😢😢😢 mulungu 😢😢😢😢
Zoonadi inenso ndikusiwa cho cho
Komad manganya anatidabwitsatu palibe chimene anayankhula pa za imfa ya Chilima an angokhala pheeee ngt sizikunkhudza zombvetsa chisoni kwabasi Mulungu yekha ndamene akudziwa zonse
That’s true brother if it was khozi ya ndeka suit no trousers no shoes my
Ndipo inu ka pangolin kamakhala chikwama mpaka kumugwira ndege ikulu ikulu osayipeza😂😂😂
Ndipoh zoonadi mwalakhula bwino ndithu broz man
Ndava chisoni
Unali bho koyamba kuja koma zalowa nsanje kwinako
Atola khani afikapodi apasidwat ndalama kut akhale chete ndipo mulungu agwesere mulili mkabudura mwawo Kuti zokozera zawo zinyenyeke kuti AZIWE phamvu ndiukulu WANU mulungu wanga chilimat sadakwake ,osalakwq kwambili ndiuyu chakwerayi
Manganya umuziwe yesu ndiukachenjede wakoyo kupusa kwako Michael usi Mzimu wa chilima ukusate ndikukantha kwambiri
Mudziwa bwanji chilungamoa Malawi ambili ndi osaphuzila ndipovuta
Eyadi ndemweyooooo
Bambo inuo ambuye akutetezeni mwayankhura mau amphamvu kwambili ndipo mizimu yanthu amene anamwalira pangozi imeneija iwazuze achakwera komaso onse amene anatenga po gawo ambuye muchite nawo
Pokhapo pokakamila u president next term, munawonesa kuti chilima simumamufunila zabwino.mukayakha kwa jahjah.
Inu ndiye mwandilizaaaaa ineeeeeeeeee maliro awa ,A chilimaaaaaa inuuuuuuu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Kkkkk mimba zilikhutchu Ngati ogulitsa tomato oola kkk Koma big man
Ndipo Inu eee ziko ili likupita kuti ndipo ine zundiwawa ndisaname ngati ndikufa ndife koma kumalawi anthu tili ndi mantha kwambiri
Amalawi ndi amantha size😢😢😢
Chichakwera chakupa galu wacha be chabe kupa andu osa lakwa chaka chamawa ndipa fup mtikumana mbusi simenesi achakwera 😢😢
Kulankhula chilungamo mopanda kuopa
Tiyeni tisiye kumvera ma wayilesi akumalawi chifukwa wonse anaguidwa kale Bora Limpopo FM radio, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo
Koma nde zoonadi ndithu watsala iyeo akuwona ngt sadzafa
Zimenezi amalawi onse akuziwa zimenezi koma akuopa kuyankhula chilungamo monga chimenecho Mulungu akuteteze kuti upitilize kutiya khulila ku Mtundu wathu..
❤❤
Iwe ndiye munthu, Malawi tulo anthu kutipusitsa chonchi,tingoyang'anila ngat nkhuku mkhola ikaphedwa imodzi zina zimangoyang'ana. Mmmmm
Yes ambuye atithandize abale eesh💔💔so sad
Zoona anthu oyipa kwambiri magazi alimanji mwawo 😅😅😅
Nkhani ya Straight 200%
Iwe ndiye walasa!
❤
Bambo ndithu mwapeleka mitu akanakhala kuti amawelenga kapena kumvela ma media mwina akanaphuzira zina
Ufulu umeneu wa anthu a misala
Ili ndi pemphero la Ana a Mulungu,, ndipo akuona ndi kumva msozi wa aliyense... Mudzalira nonse munatenga gawo pa imfa Ya anthu amenewa 😭😭😭😭
Ndifiti Manganya mwana oyipa kwambiri chisilu chamunthu ichi galu kwabasi nkhankhankha uyuuuuuuuuuuu ndimapulani awo opusawo abvutika okha mitima mwawomo
Akuti pangolini imakhala chikwama koma mumayigwila kukanika kuyipeza ndege koma yayikulu ngati imeme ija eshiii malawi walila ndithu
Mwatilankhulila father 😢😢😢
Akuopa kumangidwa
Osawopa osatopa osafooka 💪🔥🔥🔥
🔥🔥🔥
Nkhaniyo ndiyonaaa kapena 😂
Mpakana kumupha mzunu kamba ka mpando wa u president ngati kuti malawiyu ngwa amanu mukuona ngati mupitilizabe kulamulako?? Anyani agalu inu anthu oipa