Ndipo ineyo mmmm nayenda wapansi kukafika ku city center koz of this man nditsiku losaiwalika pamoyo wanga😊sleep well mr king man we shall forever remember you
@isaacbwanali4699Ай бұрын
Ine aChilima ndidzawakumbikila chifukwa chakudzipereka kwao potumikila dziko- komanso potumikira Yehova pamoyo wao. Mzimu wao ndi ena onse omwe adatayika, pangozi iyi yandege iwuse mumtendere waYesu ❤🎉
@user-ql1fy2rc4tАй бұрын
Chitsime chija chinali chakuya now ic mmene madzi mulibemo chilima King of national unity
@user-bq5eu7xb8hАй бұрын
Anali munthu okonda kupephere koma anthu❤❤
@dysonfysonchifundo2284Ай бұрын
Tidzakumbukila potipangitsa kukhulupilila Munthu olakwika nkango uli pa mpando, koma mzimu wawo uwuse mu ntendele, kungodandaula Moyo wake wapita ngati mwanapiye eish
@samuelmanda6588Ай бұрын
Ndidzamukumbukira chifukwa cholimba mtima kuti dziko lino ndila wina aliyense, tikhale ndi chiyembekezo kuti zinthu zisintha ndipo tsogolo lathu ndi lowala tikakhala ndi masomphenya. Kudzichepetsa kunalu mwa akulu aja mmmmmmm ayi enafe titengeteko phunziro. Experience yawo pogwira ntchito ndi ma private sector he had results oriented mindset.
@dinganinedsontchongwe610Ай бұрын
Saulosi Chilima sitizamuiwala anali munthu amene anabwadwa munthu was mwayi munthu wokondweka country wide munthu wolimba mtima simple man no one like him
@ernestphiri5507Ай бұрын
Its a great loss to the nation he was a great man no wonder he was a threat to the leaders of Malawi RIP beloved leader
@LeendaDeborah2005Ай бұрын
Kwa ine he looked so brave nthawi ya campaign but I don’t know what happened to him when he got in power. Adangoyamba kukhala zii all of the sudden. I may have never liked him that much once he got in power koma ineyo ndikudana kwambiri ndi mtundu wa imfa yomwe yamutenga. Wafa imfa yosayembekezeleka ndipo yowawilatu. Ambuye mukatamandike
@user-ln4de7ke4jАй бұрын
Chilima was a good man than the one who is in power
@glorynkhata1185Ай бұрын
Kungot wamwarira imfa yosakhala bwino koma kudziko ayi amaba kwambili chitukuko amapanga ku family kwake ndi ku ma party ndi amene amamudziwa za ubwino wake ine kulibe kungot mariro sitimasekerera RIP TO ALL CRASHED IN THAT BAD ACCIDENT
Mr Chilima was Genius man.The youth of Africa has lost the great leader.He had good visions for the country of Malawi.
@usumanidaudiАй бұрын
Chirima anari munthu wabwino kwambiri ine ndikudandawura kwambiri 😢😢
@DavieMakwechaАй бұрын
Ndidzawakumbukira chifukwa sanadwale ena apanga naye njiru ndi nzeru zomwe anali nazo osati zambuli zili ku mcp ko akuuzeni tanthauzo ya democracy mchiwewa sizophana ngati nthawi ya kamuzu ayi sithani a mco ino ndi nthawi ina zosiilana za dziko izi
Пікірлер: 50
Kungotchula mawu okhao oti malemu,,ndagwesa misonzi 😢😢😢R.I .P
Ndipo ineyo mmmm nayenda wapansi kukafika ku city center koz of this man nditsiku losaiwalika pamoyo wanga😊sleep well mr king man we shall forever remember you
Ine aChilima ndidzawakumbikila chifukwa chakudzipereka kwao potumikila dziko- komanso potumikira Yehova pamoyo wao. Mzimu wao ndi ena onse omwe adatayika, pangozi iyi yandege iwuse mumtendere waYesu ❤🎉
Chitsime chija chinali chakuya now ic mmene madzi mulibemo chilima King of national unity
Anali munthu okonda kupephere koma anthu❤❤
Tidzakumbukila potipangitsa kukhulupilila Munthu olakwika nkango uli pa mpando, koma mzimu wawo uwuse mu ntendele, kungodandaula Moyo wake wapita ngati mwanapiye eish
Ndidzamukumbukira chifukwa cholimba mtima kuti dziko lino ndila wina aliyense, tikhale ndi chiyembekezo kuti zinthu zisintha ndipo tsogolo lathu ndi lowala tikakhala ndi masomphenya. Kudzichepetsa kunalu mwa akulu aja mmmmmmm ayi enafe titengeteko phunziro. Experience yawo pogwira ntchito ndi ma private sector he had results oriented mindset.
Saulosi Chilima sitizamuiwala anali munthu amene anabwadwa munthu was mwayi munthu wokondweka country wide munthu wolimba mtima simple man no one like him
Its a great loss to the nation he was a great man no wonder he was a threat to the leaders of Malawi RIP beloved leader
Kwa ine he looked so brave nthawi ya campaign but I don’t know what happened to him when he got in power. Adangoyamba kukhala zii all of the sudden. I may have never liked him that much once he got in power koma ineyo ndikudana kwambiri ndi mtundu wa imfa yomwe yamutenga. Wafa imfa yosayembekezeleka ndipo yowawilatu. Ambuye mukatamandike
Chilima was a good man than the one who is in power
Kungot wamwarira imfa yosakhala bwino koma kudziko ayi amaba kwambili chitukuko amapanga ku family kwake ndi ku ma party ndi amene amamudziwa za ubwino wake ine kulibe kungot mariro sitimasekerera RIP TO ALL CRASHED IN THAT BAD ACCIDENT
Tizamukumbukila chilima chifukwa chakudekha kwake komaso kuopa Mulungu zachisoni wafa imfa yowawa imene dziko la Malawi silizayiwala
Mr Chilima was Genius man.The youth of Africa has lost the great leader.He had good visions for the country of Malawi.
Chirima anari munthu wabwino kwambiri ine ndikudandawura kwambiri 😢😢
Ndidzawakumbukira chifukwa sanadwale ena apanga naye njiru ndi nzeru zomwe anali nazo osati zambuli zili ku mcp ko akuuzeni tanthauzo ya democracy mchiwewa sizophana ngati nthawi ya kamuzu ayi sithani a mco ino ndi nthawi ina zosiilana za dziko izi
We'll rimaid Mr chilima for everything
Nkhani yosakhala bwino ndiyamoyo wachokawo,koma pa nkhani yachitukuko sanachite chilichose mmalawi muno . RIP SKC.
@user-xg2ks9nw5q
Ай бұрын
Palibe ku malawi angafane ndi chilima
Mmmh kulila ndikulila ine ndikulila chifukwa chot nd moyo wachokawo,zinazo akudziwa mulungu koma rest in peace
Ndimaonamo future bingu mwa saulosi
Taluza anthu anzeru awili saulosi and bingu
Ndizamukumbukila anali muthu olimba mtima wachikondi odekha mwa chilima munali chiyembekezo chaamalawife 😢😢
Wayifeladi mbendela ya Malawi koma Chakwela ambuye amuwone
Mkulu ameneyi tidandaula kwambiri ngati munthu koma pa chitukuko anaika Malawi pa ma vuto polowetsa mcp mboma
Ine siwandale ndipo kumalawi ndinachoka ndili wachichepele komano nkhani ya Chilima yandikhunza ndipo ndalira ndikulirabe kuona mmene afela atagwila colona manja Mulungu wa moyo tichitileni chifundo nkhondo iyiyi ndinu nokha mungaikwanitse palibe chinsisi panziko
@user-ol1hf7ru1v
Ай бұрын
Amen 🙌
Zosayenda koma kunena mwachilungamo chilima ndamene anapeleka dziko lino mwadani kut anthu aziwona nyekhwe achinyamata akungokhala pano kusowa zochita zitchito kulibe
Masiku omaliza ana amulungu adzakhala akuphedwa
Ause mumtendele adatisinthitsa kaganizidwe
Chitsime chimaera chakuya chikaphwa😢😢
Tizawakumbukira chifukwa anali munthu ozichepatse mzimu wawo uuse mutendela
Ndidzamukumbukila ndimiyambi R.I.P
😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢
Ndizawakumbukila Achilima chifucha msso phenya aeo apita nawo
Rip my big man palibeso
Ndidzamukumbukila chifukwa chamiyambi chamudimadima mwana wambuzi anayamwa tonde
@user-yl3lg5fk8f
Ай бұрын
Harry suliyani my classmate at nayizi primary bangwe good job bro
Malawi 😅😅
Miyambi yake monga njoka saweta
Will meet other side of the life 😢😢😢
RIP BIG
Watichotsa Mantha moti even gun point mmalawi sazanjenjemera
Malawi talusa munthu ofunikira kwambiri palibe wina ofana ndi chilima
Amatilimbikisa kuti tizikhala ogwirizana komaso kitilimbikisa achinyamatafe pakhani yachitukuko
😅
Zikomo kwambiri
Ntchito zabwino monga kuyimira dziko
Koma chakwera kumutenga zako kukamuphera kumupoto komwe iweyo umadako kumupoto chakwera iwe sataniki wakulu chakwera