KUCHIPANI CHA UTM CHADABWITSA ANTHU🤔🤔

Пікірлер: 153

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt6 күн бұрын

    SKC was a general fitter analibe kuyankhula za munthu koma maso ake anali ku dziko la malawi kuti lizakhare pabwino, now Usi amayenera kuwafikira a U TM amnzake powawuza za kusankhidwa kwake

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb6 күн бұрын

    Chitsiru manganya ndiwa MCp anampha chilima ameneyo anakambapo Chan Za lfa yachilima galu uyo ndi chakwera

  • @princedetbozsmallboy1749

    @princedetbozsmallboy1749

    6 күн бұрын

    Tikudabwa nawo anthu ena usiyu anaphanawo Chilima shame on him galu

  • @jelsonmlowoka8611

    @jelsonmlowoka8611

    5 күн бұрын

    Usova iwe ndiwe ndani kumuletsa usi kusakhala vp wa dziko, why did the utm owner appoint him as his runningmate at first, leaving you with no any position in the party?

  • @GibsonBanda-ey2gc

    @GibsonBanda-ey2gc

    5 күн бұрын

    umbuli

  • @user-ui7wv1mb4g
    @user-ui7wv1mb4g6 күн бұрын

    No need for imposing Usi on UTM. Usi has been so slippery in UTM. Let him go and we shall see if he is going to survive in MCP. UTM Executive may opt to accomodate him but as for ordinary members its a big NO! Why this time? Where was he all that time when our dear president was alive? Zachibwana a ayi. Usi safunika. Apite akachite zake aone ngati angadzatione.

  • @StewartMustafa

    @StewartMustafa

    5 күн бұрын

    Yes Usi can't survive in MCP if he doesn't know. But let's give him chance to proof him self whether he z an UTM member or not?

  • @AckimMhango-v1x
    @AckimMhango-v1x6 күн бұрын

    Vuto lalikulu ndi boma chifukwa linayamba kukhala ndi Usi before Chilima asanamwalile

  • @leonardzchavula3139
    @leonardzchavula31396 күн бұрын

    Its unfortunate that UTM has not shown any excitement on the appointment of Dr M B Usi,however constitutionally he was the appropriate choice.Had Chilima won the presidency in 2019 Usi was to be State Vice President. UTM has just to accept the situation.

  • @actuarialscience2283

    @actuarialscience2283

    6 күн бұрын

    I am on one of MCP whatsapp groups. I know that Usi is MCP. I am also an MCP member but I don't like Chakwera

  • @MirriamKambale

    @MirriamKambale

    6 күн бұрын

    He deserve deserve the appointment coz he was utm vp but it doesn't mean utm could have been overjoyed coz they're still in mourning time

  • @Betty-fe9ql

    @Betty-fe9ql

    6 күн бұрын

    His conduct from the 10th leaves a lot to be desired, your senior dies and you don't say a single word what's that

  • @chimwemwedulla6760

    @chimwemwedulla6760

    6 күн бұрын

    Inu zomwe usi anayalkhula komulunbiritsa kuja amaoneka ngati anali namalira amene uja?

  • @ancientnkhata1137

    @ancientnkhata1137

    5 күн бұрын

    Anamalira munali inuyo​@@chimwemwedulla6760

  • @yohaneben5452
    @yohaneben54525 күн бұрын

    I think most of the people don't know more about usi,although he is vp of UTM but originally he is a member of MCP.

  • @DysonKamama-yh7hq
    @DysonKamama-yh7hq6 күн бұрын

    Zitheka bwanji munthu anzako akulila koma osakakumana ndiakuchipani chanu before kulumbilisidwa, iye nkumakasangalala chilipo

  • @CharityChikomo-hl1gz

    @CharityChikomo-hl1gz

    6 күн бұрын

    My question exactly was he never suppose to ask his fellow utm members before making his mind???anywy zoona zidzaziwika mu nthawi yamulungu

  • @PociahMack

    @PociahMack

    6 күн бұрын

    ​@@CharityChikomo-hl1gz zimene a mayakhula a UTM munthu amene anali ndi umunthu kunali kovuta kumakhala nawo, even akubanja paja anatulusa chikalata chowadzudzula.

  • @user-ko2yv4gi5y
    @user-ko2yv4gi5y6 күн бұрын

    Chilungamo ndi amanganya anatengapo gawo lakuphedwa kwa saulosi chilima ndingakhale pakwanu pa inu mukuyakhula pali munthu amene anatenga nawo chigawo kuwapasa udindo iwowo kulibe kathu koma chilungamo anthu aku utm akudziwa kuti panali ngwilizano pakati pa manganya ndi chilima

  • @RonicSouza-sk5ux
    @RonicSouza-sk5ux6 күн бұрын

    Usi didn't consult the party when he was told about the news of his presidency

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon6 күн бұрын

    Nonse munakonza program iyi ndinu anthu opanda nzeru mukuonesakuti muli mbali ya mcp mumafuna kuti a utm akapeze ku parliament chosecho president wao wangoikidwa kumene m'manda, athaphedwa ndi mcp agalu kwabasi zikanakhala kuti zachitika mnyumba mwanu sibwezi mukukamba uchisiru mukukamba apau anthu opusa opanda chisoni

  • @user-un6qv6sj3h

    @user-un6qv6sj3h

    6 күн бұрын

    True bro

  • @rodgerskatengeza1903

    @rodgerskatengeza1903

    5 күн бұрын

    Constitution imapeleka masiku ochepa president or vice president akamwalira kuti asankhe wina

  • @user-xz7mo8zy8f
    @user-xz7mo8zy8f6 күн бұрын

    Cheap propaganda. UTM mukuganiza bwino kwabasi

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani56976 күн бұрын

    Nonse ndinu wanzeru zochepa mulankhuranu a UTM atiuzeso chani poyera zaku lephera kwao kosapezeka kolumbilitsa, pomwe anjawala adanena kale tikadalira nde mufuna atiuzeso chani za milandu basi

  • @hagayichiluwe
    @hagayichiluwe6 күн бұрын

    It's just reminding me that sanje kapena nkhwidzi exist

  • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg

    @CHIFUNDOCHINA-lp9lg

    5 күн бұрын

    Vuto la USI anazionetsera KUTI Sali ku UTM,ATANGOMWALIRA CHILIMA,Nde chipani chisangalala bwanji

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l6 күн бұрын

    This is talking reality... Kodi ndani sakuziwa ngozi vuto ndilakuti ndi ndege yoyamba kugwa ku Malawi. Komaso DPP yokusonkheza moto kwambiri kuti utm isokonekere

  • @princekandulu4542

    @princekandulu4542

    6 күн бұрын

    Mmenenso MCP n imakokomeza mikangano ku Dpp

  • @chimwemwedulla6760

    @chimwemwedulla6760

    6 күн бұрын

    Ndiwe mbuzi

  • @spargomw

    @spargomw

    6 күн бұрын

    Mwana wa Ng'ona iwe, khakhakha. Za DPP zikukukhudxa chaaa, zipangan zanu. Ife tili ku ma stand

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma6 күн бұрын

    Koma anthu Inu muli ndi nzeru?a utm apita bwanji kukaombela mmanja ali pa maliro?Kodi malamulo ake amtundu wanji week sinathe ena ayamba ukuvina kulumbilitsana a Malawi?which means it was planned this b4 imfa ya chilima khalani ndi nzimu waumunthu eeti

  • @mathewssimbi3052
    @mathewssimbi30526 күн бұрын

    Koma ngakhale palibe umboni okwanira mafedwe a chilima ndiwonkhumudwitsa kwambiri ndipo ndiwokayikitsa kotero mkovuta Kuti lero ndi lero akulu akulu a UTM adzikapezeka akuyimba nthungululu pamwambo wosankhidwa Kwa Ausi kotero kusapita kwao kumwamboku mkovetsetseka zongofunika tsopano kuwona kutsogolo

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f6 күн бұрын

    Anthu amene aludandaula zanthawi sakudziwa zamalamulo amdziko

  • @IdrisYousuf

    @IdrisYousuf

    6 күн бұрын

    Àluthu aluamenewo aludandaulawo alukuti taludziwe😅😅😅😅😅😅

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb6 күн бұрын

    Inuso mphokoso kusowa zakamba position ndikuluza munthu malamuro ndichani zachamba et manganya amafuna Kare uvp Kare that way anamupereka chilima kwa mikangoyo mukusokosa kusowa zakamba

  • @user-ez4ru5sk2l

    @user-ez4ru5sk2l

    6 күн бұрын

    The truth is that SKC shoes are unfittable in all the alliance...and entire country leadership currently....but the country has to move forward.....ndale sizinthu zamuyaya ... it's about servanthood ... service to the people

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f6 күн бұрын

    Kusankhidwa kwa Michael usi wasatila ndondomeko yake chifukwa iye anali osatila wa the late SKC.komano tingodziwa kuti usi ali ku UTM kapena ali ku mcp?

  • @user-un6qv6sj3h

    @user-un6qv6sj3h

    6 күн бұрын

    Adalowa kalekle MCP

  • @user-ik5sz8hc6f

    @user-ik5sz8hc6f

    6 күн бұрын

    @@user-un6qv6sj3h vuto ndilimenelo.Anayenela kukhalabe wa UTM kuti alemekeze ukuru former president of UTM

  • @NefassiNefitarZaqueioZaqueio
    @NefassiNefitarZaqueioZaqueio6 күн бұрын

    Ngati palakwika kulumbilitsa a Usi nsanga ,tilolerane inuyo mukudzidzulanu sindinu angwiro muli ndi zofooka zanu choncho ngati late Chilima adasankha a Usi adaona kuthekera komwe kuli mmenemo. Kaya wina afune kaya asafune zili choncho basi olo mutukwana olo mutakhala chete ,zichitika zomwe mulungu wavomereza

  • @user-ux3ed3ni1p
    @user-ux3ed3ni1p6 күн бұрын

    What is Dr. Usi bringing to the leadership of VP and UTM. will be the question.

  • @tamalangoma2765
    @tamalangoma27656 күн бұрын

    May be you should blame late VP for choosing Usi ngati VP wake. Please stop making too much noise.

  • @chimwemwedulla6760

    @chimwemwedulla6760

    6 күн бұрын

    What noise achitsiru inu

  • @user-mz8nw6nx6p
    @user-mz8nw6nx6p6 күн бұрын

    Malamulo amanena kuti for 7days pasankhidwe munthu wina,,komaso sakanankhidwa wina koma Usi chifukwa anali vp wa chipani cha UTM,,so guys I don't know why we don't understand for this issues,,,we suppose to understanding because it's a rule,, it's not opinion for someone

  • @ishmaelsiffah9900
    @ishmaelsiffah99006 күн бұрын

    Ussi samapanga za UTM n the sad point ndizomwe timaziona munthawi yomwe anthu amapanga zamaliro a SKC ndi ena,iwo aja being munthu wamkulu wachipani pambuyo pakumwalira kwa achilima iwowo ndamene timayembekezera kuti ndiomwe azititonthoza ndikumatipatsa ma update amomwe tiyendere koma mmalo mwake anamusiira mzimai kumapanga zazimenezo n zinatengera kulimba mtima kwamai Kaliyati osatopa,osafooka kumatiyankhula amalawi nthawi ndinthawi,mukumbukirenso kuti ndi a Ussi omweo akuwafunsa zakuimila kwao kwaku Blantyre anakanitsitsa kutchula kuti akaimila chipani chanji yet munthuyo mukuti ndiwa UTM pamabvuta pati kunena zokuti akaimila UTM izo ndizachidziwikile kuti akulu amenewa UTM anaituluka kumangotsala kuti officially alengedze kuti atuluka

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande61082 күн бұрын

    Onse Ali apa ndi zitsilu , how Catherine be sitting and talking while the responders they say ,they are still mourning and it's true Malawian are mourning ndale zophana basi achewa opanda Pache inu

  • @chrispinechirwa2655
    @chrispinechirwa26553 күн бұрын

    Choyamba tidziwe kuti mu zipanimu utsogoleri umasankhidwa through convention nde kusankhidwa kwa usi sikutanthauza kuti ndi mtsogoleri wa utm. By the way the government could write aletter to utm based on their agreement to prove that the alliance is still valid. Koma kungotenga munthu personally uuùuuu it's clear usi si wa utm

  • @yasitafuphiri-nw2he
    @yasitafuphiri-nw2he5 күн бұрын

    If Usi was never a UTM member, y Chilima appointed him as party VP?

  • @jelsonmlowoka8611

    @jelsonmlowoka8611

    5 күн бұрын

    Your question is very straight and correct

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l6 күн бұрын

    UTM this is your good time and best Future be united guys chipani chizalowa muboma pachokha don't expect kuzalamulira Malawi

  • @StewartMustafa
    @StewartMustafa5 күн бұрын

    Gentlemen plzzz lets take this issue very seriously. Dr Usi z not wrong kulandila udindo kapena kuti VP. Ndizoona kuti Dr Usi anayamba kukhala ndi boma more especially president of the republic kalekale komano chomwe tingadziwe ndichakuti even The laye Dr Saulos Chilima adali pafupi ndi boma more especially to the President of the Republic. Now gents if u digest all of these it means these pple r wel organised coz they both take one step at a time. Now lets not talk a lot of things when its not time to do so. Time will tell whereby will will proof Dr Usi that is a member of MCP or He z still with us in Almighty UTM.

  • @user-ux3ed3ni1p
    @user-ux3ed3ni1p6 күн бұрын

    Malamulo are there but we pick and choose what to enforce in Malawi" s constitution.

  • @Moffat-oi4yx
    @Moffat-oi4yx4 күн бұрын

    Akanganya inu mwalandila banzi chakwelayo akalemekeze malamulo osankha vp bwanji sanalemekeze malamulo Osaka ndegeija kumawalozela anthu kolakwika akudziwa chilungamo

  • @wellosmbewe6820
    @wellosmbewe68205 күн бұрын

    Who is the president of UTM now and what is his speach

  • @RoseLameck-ub7sq
    @RoseLameck-ub7sq5 күн бұрын

    Ine dakalila malilo achilima singakambe kathu ndingodikila chaka chamawa ka vote bas chiweluzo nkaweluzila komweko ndichala changa😢

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v6 күн бұрын

    Koma tu anthu mcp mukamapanga zithu mudziziwa kuti mawa ndi tsiku Lina

  • @user-sh6gi5uq3l
    @user-sh6gi5uq3l5 күн бұрын

    Akapusa a UTM a muluza manganyawo atuluka

  • @EsnartMartin
    @EsnartMartin5 күн бұрын

    Ineso Manganya simnamulandire ku UTM

  • @user-eb2yo9bc9k
    @user-eb2yo9bc9k6 күн бұрын

    I doubt of all this, am confused but what I know is that utm is not happy with that

  • @RaphaelMaunde
    @RaphaelMaunde6 күн бұрын

    The appointment is right decisions but there is some issues between Dr Usi and UTM party Dr Usi was not royal to the party

  • @laurentbutao4084

    @laurentbutao4084

    5 күн бұрын

    Exactly

  • @Happy-e8d
    @Happy-e8d5 күн бұрын

    Ndinakakhala ine ndikanaka kukhala VP

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo95025 күн бұрын

    Dziko La malawa amipingo ndamene anasokoneza ndi athila kuwili amasokoneza athu iwo ananena sakhani tsogoleri asakha akubweraso mwasakha thawi yolakwika kkkk koma guys mavuto Eni Eni and manganya anali wachiwili kwa wachiwili anayenera akhala iye kaya😢

  • @user-sh6gi5uq3l
    @user-sh6gi5uq3l5 күн бұрын

    Amalawi let's move on zinazi tichedwa nazo mulungu salakwisa kodi amalawi mpaka liti tijusungabe mangawa look at APM for not accepting the fact someone is ruling now aaaa moti a UTM amafuna kufunsidwa maganizo pomwe thawi yochita appoint veep itakwana and azichedwa ndizosangala munthu mmmmmm. Malawi my country learn to accept God's plan

  • @KhonzoBlose-wq7zm
    @KhonzoBlose-wq7zm5 күн бұрын

    Move yonse yakuphedwa kwa Chilma amayiziwa asapuse fans.

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire87696 күн бұрын

    It can stay kufika pa 2 July ndipo panakhala popanda vice Kwa chaka bwa a Chilima atamangidwa

  • @ChisomoPound
    @ChisomoPound5 күн бұрын

    Khaniyi mutati muyione ndiyovutirapo vuto Lili APA anthu ambiri andale amafuna maudindo ngat awa ndiye pamakhala kuyang'anizana ndi diso lofila ngat iweyo sunasakhidwe,choti muziwe Pali zina zimachitika mwamalamulo tiyeni tibwelere mbuyo 2012 bingu wa muthalika atamwalira Ku dpp kunali ambiri amafuna udindo koma anayiwala kut Kuli lamulo lot ngat president watisiya vice ndi yemwe akuyenera kukhala mlowa mmalo ndiye izizi zomwe zikuchitikazi khani siyina ayi maudindo amenewa Kuli kapezedwe Ka ndalama mwaulesi

  • @williamsjonazie5764
    @williamsjonazie57646 күн бұрын

    Choyamba tiwunikile Kaye kuti Kodi chakwera poziwa kuti usi ndi vice president wa UTM anawawuza za appointment ya usi? Ngati adatelo ndiye a UTM analakwisa kusapita koma ngati sadawauze za kusakhidwa Kwa usi adachita bwino kusapita chifukwa usi wangokhala vice president wa UTM koma ndi member wa UTM,executive ikanaziwisidwa mwa dongosolo and then invited kukalumbilitsa vice president. Nde anthu musamangofutsa mafutso mwina mufutse chakwera yo. Ndamene angalongosole momwe adayendesela ndondomeko yake.

  • @KhonzoBlose-wq7zm
    @KhonzoBlose-wq7zm5 күн бұрын

    Manganya he is a snake ndiwa Mcp .every knows about that, chitsilu cha munthu

  • @humphreysidie4747
    @humphreysidie47475 күн бұрын

    Guys ineso ndufuna kumangidwa, this Usi guy knew everything, he sold Chilima

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q5 күн бұрын

    Manganya sanali wa UTM analowa MCP kale kale mosadziwa anthu mumtima mwake anali wa MCP

  • @AllaniWilesi
    @AllaniWilesi4 күн бұрын

    Ausi achita bwino inde koma asamanyengane nda azimayi ayeni pakuti Ali ndimbili yonyasa kwambili

  • @OmexPoisonkaombe-cf7bz
    @OmexPoisonkaombe-cf7bz5 күн бұрын

    Kusapanda nseru anapha bwanji vice president wathu ameneyo bas

  • @HellenKanyemba
    @HellenKanyemba5 күн бұрын

    Atolankhani thawing zina ndinu anthira kuwili achakwera sanamusankhe usi koma achilima ndio anasankha a usi koma achakwera angitsatira lamulo basi

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande61082 күн бұрын

    It not alaw, kut you must choose the vice president wachipani, that is a trap iwe manganya akupasa zingati why you didn't have time to settle and see it with your utm people

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r6 күн бұрын

    Awusi anarephera kutengapo gawo, kufa kwa skc relo palibe sngakondwe nazo asiyen azipanga zomwe amatha ndi kongweresi yakeyo

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani56976 күн бұрын

    A UTM ku sapita kolumbilitsa a Usi nkutheka sadalakwise mwina sadayitanidwe patha kukhara padalibe consultations,

  • @mzeewandembonyirongo2972
    @mzeewandembonyirongo29726 күн бұрын

    Don't just say this...who do you think kuti akanamusakha? Mention her or him....

  • @chifundomaduka6242
    @chifundomaduka62425 күн бұрын

    Usi was never UTM

  • @Stewartchikoja
    @Stewartchikoja6 күн бұрын

    Kodi ngat wina adakhala Dzaka 4 osapenza mpumulo pa office yake how about 1 Yr chingasithe ndi chani ?

  • @JackMvura-ik2td
    @JackMvura-ik2td6 күн бұрын

    Munena angati mutukwana angati anzathu patsogolo Ife basi zaziii nthawi ikupita tichedwa zinenani bola chakwera sadandaula anaona kale Kuti sanje zilipo kuteloku Wena mtima uwawa Kuti basi manganya wapita basi ayi zosiyilana mawa ndinu pepani mulungu akusungeni

  • @user-ql8sj4jj3y
    @user-ql8sj4jj3y5 күн бұрын

    Manganya ndi mcp,, if he was vice wa chilima, atamwalira dr chilima was just qite why

  • @RonaldGama-gz9ug
    @RonaldGama-gz9ug6 күн бұрын

    Kodi a UTM wo mukuwafuna kuti atanipo Pa nkhaniyi coz they can't reserve the time anayankha zomwe iwo Ali ndiye chinanso ndi chani

  • @stevenbanda-zp7ie
    @stevenbanda-zp7ie6 күн бұрын

    Is Michael USI Acting president of UTM??

  • @MCAnthonyNdau
    @MCAnthonyNdau6 күн бұрын

    Kodi akankhala kuti anali apulezident kuti ndiomwe atisiya Chilima automatically akanakhala pulezident Kodi kolumbilitsa sakanapita

  • @user-ql8sj4jj3y
    @user-ql8sj4jj3y5 күн бұрын

    Total lay dpp sizikuwakhuza

  • @FrancisStima-sc7zs
    @FrancisStima-sc7zs6 күн бұрын

    A UTM ananyanyaladi ndizona Koma anakakhala kt asakha aliyese akanavomelabe chifukwa andalewa amafuna ndalama osati kutisogolelai ndichifukwachake zipani zikungobadwabe aliyese akufuna kukhala pamwamba

  • @TaniaMphalumo
    @TaniaMphalumo5 күн бұрын

    Zauchisilu basi wasangalalanazo ndani utm muyisiye agaru inu

  • @MCAnthonyNdau
    @MCAnthonyNdau6 күн бұрын

    Ndichimodzi modzi bingu atamwalila sitinakhale ndi pulezident wanyowani

  • @user-oe1lg4xo7w
    @user-oe1lg4xo7w6 күн бұрын

    Mamembala a UTM akuziwa kuti Razalo wasankha nkhwali kuti ikhale pampando wa vp

  • @MikeKatola
    @MikeKatola6 күн бұрын

    Inenso sindikuona vuto bcz olo ufumu amalonga wina mfumu asanaike.so why utm akuonesa kukwiya.akukwiya ndi anthu oti sakuziwa kuti chilima ndi usi amagwirizana chani.

  • @VictoriaWilliam-ms2ft
    @VictoriaWilliam-ms2ft5 күн бұрын

    Usi siwa utm ndiwa mcp uja musatinamizepo apa

  • @ChisomoPound
    @ChisomoPound5 күн бұрын

    Komaso kod tikumuyamikila chilimba kut anali Muthu wabwino ndipo oganiza boo funso langa Lili APA kod chilima anaona chani Kwa usi ?

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili6 күн бұрын

    Bt u vice wanu mmmm

  • @Shire9627
    @Shire96276 күн бұрын

    Malawians timadana ndi chilungamo🤣🤣🤣

  • @MarkGonda-qr4vm
    @MarkGonda-qr4vm4 күн бұрын

    Koma ndiye azingopanga zamasewerotu amanganyawa

  • @AmusedDimSum-hd5yp
    @AmusedDimSum-hd5yp6 күн бұрын

    how did you know that those who were not happy were utm members of the pary banzi mwadyayo musasokoneze zinthu

  • @RonaldGama-gz9ug
    @RonaldGama-gz9ug6 күн бұрын

    Ndiye pano galu zanuwo akulemekeza malamulo ngati momwe mukuneneramo

  • @HanifiYaumu
    @HanifiYaumu6 күн бұрын

    Kape manganya akudziwapo kathu pa infa skc

  • @saidimwanyali8969
    @saidimwanyali89696 күн бұрын

    Kodi pofuna kusanga ausi achakwera adayitana ausi oka kapena adayitana chipani chonse ndikumasanga kapena anawasanga kuseri

  • @user-mm9ox2pz7p
    @user-mm9ox2pz7p6 күн бұрын

    Zaziiiii mwasowa zokambirana

  • @PreciousKARINGANIZA
    @PreciousKARINGANIZA4 күн бұрын

    Anampereka zake chifukwa chofuna mpando

  • @PempheroAlufandika
    @PempheroAlufandika6 күн бұрын

    Anachita bwino a UTM munangagulitsa chipani mwaganiza bho

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w6 күн бұрын

    Palibe chimene angachite Usi, and Malemu ndiamene adatsogolera kubweretsa mavuto ali ku Malawi lero.

  • @user-ui7wv1mb4g

    @user-ui7wv1mb4g

    6 күн бұрын

    What mavuto are you talking about . Was he on the driving seat? Kufooka kwa wina osaloza chala ena

  • @KenDuweh
    @KenDuweh6 күн бұрын

    Muwawudze a Micheal usi kuti watikumbutsa za mbala ziwiri pa mtanda ifeo timukumbutse za Yudas isikaliyot uja unapeleka Yesu khristu kuti kodzi zinankhla bwanji? Zandale tiyen tizingoona😅

  • @user-vr5jn8sz5r
    @user-vr5jn8sz5r6 күн бұрын

    Manganya ndi wa MCP ngati inunomwe a ZBS musamati pepelese.

  • @kamphunguluhanga5716
    @kamphunguluhanga57166 күн бұрын

    Osagwirizana nazozo akulakwa. Chifukwa or vhikqnkhala kuti running mate akanakhala Rasta Chikomeni zikanakhala momwemo basi. Munthu uyu wotchedwa Chakwera ndi Munthu woyenera usogoleri. Chifukwa watsata ndondomeko yamugwirizano wawo komnso kutsatira constitution ya Presidencey

  • @NefassiNefitarZaqueioZaqueio
    @NefassiNefitarZaqueioZaqueio6 күн бұрын

    Kutukwana kwanu kwanveka dziko lonse mulungu walola kuti mutukwane koma mudzayankha mwapadera .Dziyanganileni nokha onyoza inu.

  • @peterkinsLekera
    @peterkinsLekera6 күн бұрын

    Malamulowo anaphwanya kake akadangopitiriza panafutsa kale masiku 10 asadasakhe

  • @janemsiska3345
    @janemsiska33455 күн бұрын

    Mukwonago video yatsiku amalengeza maliro manganese amasekelera

  • @BRIGHTONALASON
    @BRIGHTONALASON5 күн бұрын

    Malamulo anthu salibwino komanso mmmmmm ena ifayi yawakomera nde chaona nzako chapita mawa towards you

  • @YohanePatrick-lc2lq
    @YohanePatrick-lc2lq6 күн бұрын

    Unuyo mwapanga program imeneyiso ndinu dzitsilu kwabasi manganyaso nindani

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp5 күн бұрын

    Sachamba

  • @MayiSwale
    @MayiSwale6 күн бұрын

    Chanzeru ndi chani??? Zaziiii

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy17496 күн бұрын

    Inuyoso nanu aaàa manganyayu anapha nawo Chilima galu wamunthu uyu kakuwoneka mumask ka manganyaka kanachenjela udyo

  • @RonaldGama-gz9ug
    @RonaldGama-gz9ug6 күн бұрын

    Eya akuyenera kutenga komweko ndi chifukwa chofuna kuwapusitsa

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h6 күн бұрын

    A p k musati 100,% koz anthu sakuteloyi tikuti manganya adali mthila kuwiri

  • @EstherAmadu-md3et
    @EstherAmadu-md3et6 күн бұрын

    Koma abale manganya angakhale wachiwiri wa ntsogoleri wa dziko mmmm dziko limafuna kutsogoleledwa ndi anthu a serious uyu anthu sangamunvele akapitilize ma drama

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e6 күн бұрын

    Utsi nd wa mcp inu a utm mukapusa mugulitsa chipan😮

  • @Maliet-nh6kf
    @Maliet-nh6kf5 күн бұрын

    But why you killing others skc he made mcp to be on position later on decide 😈 chakwera pathako pako malo mobweza ulem ndikupha munthu😢😢😢

  • @TsholofeloTong
    @TsholofeloTong5 күн бұрын

    Usi please just go to your MCP because we already know that you're mcp member

  • @Maliet-nh6kf

    @Maliet-nh6kf

    5 күн бұрын

    Uyanya mcp kupha

  • @user-qo5sw2os4j
    @user-qo5sw2os4j5 күн бұрын

    Vuto ndi MCP and usiyo iyaa

  • @marryphili5419
    @marryphili54196 күн бұрын

    Ine Si wachipani Koma kunena zoona a usi akuziwapo chinachake pa imfa ya achilima chifukwa khope yake achilima atamwalira kumene iwo samawoneka wokhuzidwa ndi imfa imeneyi

  • @omarlux3434

    @omarlux3434

    6 күн бұрын

    Kod akanasakhivwa kaliyati mukanaso kut amaziwapo kathu mumafuna asakhe inu

Келесі