Ku Boma Penapake Mulankhula Mwachibwana Kwambili - Bon Kalindo
Bon Kalindo responds to a statement made by the Ministry of Information following the burial of the Late Vice President Right Honourable Dr. Saulos Klaus Chilima and eight other Malawians. He also calls on the Malawi Broadcasting Corporation to cease acting as a propaganda machine and instead urges them to strive for impartiality in their reporting.
A Bon Kalindo ayankha zomwe unduna wa zofalitsa nkhani unanena potsatira kuikidwa kwa wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr. Saulos Klaus Chilima ndi a Malawi ena asanu ndi atatu. Iye wapemphanso bungwe la Malawi Broadcasting Corporation kuti lisiye kupanga Propanga m’malo mwake akuwapempha kuti aziyesetsa kusakondera mbali imodzi.popereka malipoti.
#malawi
Пікірлер: 42
NG'ALULA BON AGALU AMENEWA AZOLOWERA KWABASI, NJOKA NDINJOKA
Osafooka , osatopa kms Osachita mantha Dziko ndi lathu ( Thanks Mr Kalindo posachita mantha 🔥)
I will be following you my freedom fighter Mr Bon Kalindo God bless you all of time
bon kalindo 🔥🔥🔥
Kenako tipita ku ma station tikamatche aseke tidzasegula akachoka pampando moto kuti buuuu ❤
Well done big boss the DC
Freedom fighter 💪 🙌 president wa ife wosowa makwacha
Bless you 🙏
Ulemu wanu mr kalindo
Ndipo auzeni zoona
Sure
Big up boss
Zoona DC
Malawi on 🔥🔥
Nde akuti amumangilanji amenewa? Pachilungamo ngati ichii😅😅😅
❤
Amene amaona za nyengo tsiku limenelo akuyenera kumangidwa, Chilima Uja munachita Kupha A MCP, tengani dzikoli muzilamula
🔥🔥🔥🔥
Anakachoka asapitirizesso
Anthu okupopani akupwetekesani a bon mukanangopempha unduna akupwetekesani ameneyi alangidwe nsanje yakula akalindo😅😅
Go kalindo
Fact
Ng'alura Bon...
Kungolankhula chilungamo basi akuyetsa amalawi tikugona
Koma 😂😂😂 ati mwayamba kuikana ndege
Bwana ndegeyo musayikane 😂😂
Akuti Namandege...😂😂😂😂
Ang'alule mbale
Yah zoonadi the DC vuto ndiloti kumalawiko kulibeko president dziko lonvesa chisoni ng'alulani basi
The DC
😂😂 koma DCCC ndiakatundu
Amalawi tilowe pansewu, kodi ma demo akuvuta bwanji ndi boma ili? Nthawi ya DPP ma demo samachewatu.
Ndipo asatinyaseso athu amenewa
Dee See
Kkkkkk namandege
Tiyeni tonse timutsapote kalindo malawi yu wafika pa nyansi anthu oyipa awa a mcp ndipo mbiri imadzibweledza yonkha lero ndi izi achera nsapha patetete
DC unabwadwa bwanji 😂😂 ndikufuna ndizakuone
kkkk kwayaka
Mbuzi ya DPP kalindo uchedwa nazo
Chirungamo chiyende
Dc mwana wachabe
DC kkkkk