HOT CURRENT 14 JULY 2024 |

Пікірлер: 97

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632Ай бұрын

    Go on Guy's we wait to see the changes in Malawi eeeee from Bakili muluzi up to know am in RSA because of politics of Malawi throwing as away not thinking of coming back to home eeeeeeeeesh

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786Ай бұрын

    Chilima was assassinated that's the truth what more do u want to hear?

  • @user-lj8ug5lq8c
    @user-lj8ug5lq8cАй бұрын

    Guys keep it like this ,this is Hot current we know from those days congratulations

  • @JamesIngeni-ku3qj
    @JamesIngeni-ku3qjАй бұрын

    Manganya ndi mcp anapha chilima.

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6eАй бұрын

    Usi si wa UTM. Munamuwona muja amarandira udindo muja? UTM yachita bwino kuwaturuka.

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769Ай бұрын

    Ngozi ija singozi ngozi ,,komanso yonse taona ndimafinso

  • @BambordKabambe
    @BambordKabambeАй бұрын

    😂😂😂😂😂 chaka chino ndi CHONG'ALURA

  • @JohnNjerenga
    @JohnNjerengaАй бұрын

    Kkkkk akut ipondeni fadha

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310Ай бұрын

    Apa ndiye mwabwelatu chilungamo chimenecho

  • @EstherChimombo
    @EstherChimomboАй бұрын

    🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥💯💯

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pkАй бұрын

    Times muziwe kuti chilima agwila bwanji ntchito ndi chakwela mu 4years

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100Ай бұрын

    Masapota a UTM tonse tatuluka ku mgwirizano Chifukwa tinkasapota Chilima.Usi alibe masapota.

  • @user-oh9bh1cl3b
    @user-oh9bh1cl3bАй бұрын

    Well spoken guy's adzimva akawalalawa

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830Ай бұрын

    Walephera Chakwera kulamulira kuchedwa 4yrs ndipo akhala akungodandaula DPP mmalo mopanga ziganizo msanga

  • @OrtonKabbichi
    @OrtonKabbichiАй бұрын

    Sizachilendo olo pa ngozi ya ndege ija anachedwanso kukafufuza ayambe kuchotsa ameneo onwe amaenera kukafufuza za ngozi ya ndege

  • @patricksinyala1345
    @patricksinyala1345Ай бұрын

    Mtsukuluzi ukulankhula mopusa, kufooka kwa Ussi kunayamba Chilima alimoyo. Ndipo. Chilimma anali atamuzindikila Kale Ussi ukathyali wake.

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3hАй бұрын

    Inu ussi siwa UTM 😂😂😂😂ameneuja ngawa MCP

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109Ай бұрын

    Chakwera so asamale zomwe wawona Nzake wa kwa merica zija zichitikanso kuno.

  • @symonmakata938
    @symonmakata938Ай бұрын

    Changucho chiyambile pa kafukufuku wa ndege inapha chilima kenako the public ikhala ndi changu

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4vАй бұрын

    Dziko ndilathu osaonesa kutopa azibambo ipondeni thawi ino palibe kuopa ng,alulani basi ng,ambani

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2dАй бұрын

    Usi atha ngati nankhumwa sure, olo kuthesako akufuna kukhaulisa manganya coz anamuziwa kuti uyu sitili limozi ndi wa mcp.

  • @JohnmarkNazombe-hi9xd
    @JohnmarkNazombe-hi9xdАй бұрын

    Dziko nkumasawukaaaaah!!!!!!!

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100Ай бұрын

    Masapota ake ati omwe atsatire Usi ku MCP. Musanamizane palibe yemwe angavotere MCP true member wa UTM

  • @EfeloYovita
    @EfeloYovitaАй бұрын

    ngati bola Allience latha ndibwino kukhala opanda president cs chakwela polowa m boma unali mgwilizano maka utm inali ndimavoti ambiri kuposa mcp we must have emergency presidental election

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tgАй бұрын

    MCP yayambitsa nkhondo yoopsa yokha amalawi sangasangalale nazo izi Zotsatila results zangozi kuli ziiiii mpaka pano what do you do

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazumaАй бұрын

    Keep it up Guy's ife ndalama tidya koma sitidzawavotela talira kokwana sife opusaso pano

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uyАй бұрын

    Akuchedwa Nd pule yomweyo😂😂😂😂😂

  • @imaculadaAndre-ns1py
    @imaculadaAndre-ns1pyАй бұрын

    Fiti ndifiti basi awa sangaulule chilingamo kwao ndikunama basi koma ife chilingamo tinachipeza kale

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784Ай бұрын

    Akuti mbwexe😅😅😅😅😅😂😂😂

  • @catherineKalinga-m4c
    @catherineKalinga-m4cАй бұрын

    🤩

  • @AishaChipande
    @AishaChipandeАй бұрын

    Chakwela azuzula bwanji pomwe iyeyo anaphaso muzake

  • @EsnartMbalale
    @EsnartMbalaleАй бұрын

    Ipitilile ndiyabwino coz ikulakhula mosatenga bali

  • @imaculadaAndre-ns1py
    @imaculadaAndre-ns1pyАй бұрын

    Tamusiyani maganya abakhala komweko adzatiuza zenizeni abawatola zifukwa adzapange sewelo mutu wake chakwera anapha zake chifukwa chaudindo

  • @OfwaMwambila
    @OfwaMwambilaАй бұрын

    Alot of people re in marriages that ended a long time ago but due to kids u re forced to still living together that's what I think was the case of SKC&usi.

  • @StiveKantiki
    @StiveKantikiАй бұрын

    Akuyambisa kuchedwa ndi achakwela ndipo ife tinalakwisa kumuika munthu onamizila ubusa Ngati uyu pa mpando

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109Ай бұрын

    Mbwelera zokha zokha za mcp kkkkkkk koma pankuku!!!!!!

  • @BestonStima
    @BestonStimaАй бұрын

    Mcp ivutika chifukwa isanalowe m'boma amalawi ankaopa nkhanza za mbiri yawo Lero in their 4yrs rule patuluka nkhanza. Do you think they can reign???????????

  • @robertnambazo9936
    @robertnambazo9936Ай бұрын

    President osaziwachomwe akuchita he is so relaxing President President uyu ndi bubu shatapu zake

  • @SteveKanongwa
    @SteveKanongwaАй бұрын

    Koma ma guys inuo hahaha munatopa nalo dzikoli simufunaso zachikape

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9hАй бұрын

    Manganya ndi wa mcp not utm

  • @johnmhango9405
    @johnmhango9405Ай бұрын

    Briefcase parties end just like that.

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109Ай бұрын

    Uyakhura za chidodoyo ndiye ili mbudzi yoyambisa chakwera samasata zinthu that’s y anyamata ake angomisewera basi.

  • @SteveChapola
    @SteveChapolaАй бұрын

    A mcp chipani chokupha

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769Ай бұрын

    Sitizalola report. Wonder you are very Intelligent than pankukuyo

  • @GodfryMalishe
    @GodfryMalisheАй бұрын

    Salute u guys 😂

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uyАй бұрын

    How many meetings manganya has been attending?? Can he allow to apart from the alliance coz it's obvious manganya it's won't allow

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476Ай бұрын

    Eeeeeee yankhulani guys ❤

  • @lukedumbula2724
    @lukedumbula2724Ай бұрын

    Very true wonder and jona, a PULE akuchedwaa

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3wАй бұрын

    Pa nkhani yochedwetsa chitukuko, tingomuchotsa next year basi, sali fit Chakwera to be a President.

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769Ай бұрын

    A Usi si president wanthu,,munthu mkazi wake tamuziwa polumbilitsa mkumazitama kuti ine sindinayendepo ndi mkazi wanga,,muthuyu angayendese chipani

  • @RafiqueChibwana
    @RafiqueChibwanaАй бұрын

    You guys u don't share kamba here really keep it up guys kkkkkkkkk

  • @JaphetSakala-pq4fl
    @JaphetSakala-pq4flАй бұрын

    Kuchokela pa ifa ya VP chilima kufikila pasiku la mavoti UTM ILI PA TOP ONE. or Dpp ndi mcp ita phatikizana. UTM IKUTENGA BOMA TIZAIPEPESA NDI VOTE.

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3prАй бұрын

    Lero munabweratu a jonah kkk wonder akuti back to sender eee Chakwera dzimvere mumtolo

  • @JuuuKomba
    @JuuuKombaАй бұрын

    Eni ake a UTM ndifeyo ovotafe Tatupu ndife awowo dyela Paolo asaleko tilibe nawo film

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuziАй бұрын

    Osawopa ayi a malawi ambiri tikuyang'anira inu kut muziyakhura mosawopa apa

  • @CosimassShyman
    @CosimassShymanАй бұрын

    Wakulu andevu zamwayi amayankhura Chichewa cha boo

  • @YamikanChirwa
    @YamikanChirwaАй бұрын

    Ng'alula iwe

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tgАй бұрын

    😂😂😂😂😂 anyamata inu mwandisangalatsatu chikufunika ndichimenechi osanyangerera kulankhula chilungamo kubandaluka basi sizoopaso ayi

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6pАй бұрын

    Kaya DPP kaya ilibe ndalama iwinabe 2025

  • @user-rd9pd9hr2l
    @user-rd9pd9hr2lАй бұрын

    Inuyo munabwera ngati coming 🔥

  • @MisheckAselo
    @MisheckAseloАй бұрын

    A pule ayamba kupemphera ku CCAP kamutu kataya

  • @joneskalitsilo6556
    @joneskalitsilo6556Ай бұрын

    Exactly Wonder bambo wanzelu amakonza mavuto amu nyumba mwake not kutuluka nkumakadandaula panja or kubwalo kuti mnyumba mwanga sitikudya ana anga sakuvala bwino, sitikudya bwino! Nde ana Inu muzivala bwino, muzidya bwino, ukuganiza kuti anawo azitenga kuti?

  • @peternashyo9850
    @peternashyo9850Ай бұрын

    Nkhaniyo ndiyoona, a President akugona kwambiri pachiongolero, dziko silingatukuke ai

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100Ай бұрын

    Anaphedwa ku Mwanza aja ndiochepa.pano ayesetsetsa kupha ambiri.athakati sadzasintha.Malawi Congress of Perishers

  • @DarlingtonMaya
    @DarlingtonMayaАй бұрын

    Gyz mmmatha

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6yАй бұрын

    MCP ndi Yakupha

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuziАй бұрын

    Iwe pankuku osamayakhura mowopa apa

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANIАй бұрын

    Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach

  • @MuhamadYassin-ye4hn
    @MuhamadYassin-ye4hnАй бұрын

    Mumakwana mabigi

  • @Amos-tr6ro
    @Amos-tr6roАй бұрын

    Koma makosana inu MMM mwanditha keen on on our behalf

  • @jackmambo2638
    @jackmambo2638Ай бұрын

    Kod amaphang’ombe ali kut😂😂

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5oАй бұрын

    Did. Mcp ask Afford

  • @StiveKantiki
    @StiveKantikiАй бұрын

    Aganizq bwanji mwakuya kuposa anthu zosatheka ubongo unatha chifukwa ankadya zopasidwa Za chaulele

  • @user-tg7ni7wh2c
    @user-tg7ni7wh2cАй бұрын

    Eeh 😂

  • @johnmhango9405
    @johnmhango9405Ай бұрын

    A kaliati ndi a njawala nzokonza izi, akufuna apange handpick Kabambe, can't you read between the lines? Typical of atsogoleri a dyela.

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1rАй бұрын

    Emusipi ofunika isale yokha. Anthu woipa awa

  • @frankdomingo1109
    @frankdomingo1109Ай бұрын

    Decisiveness palibepo

  • @yusufjab786
    @yusufjab786Ай бұрын

    Ndipo inuyo kumeneko mumaitha 😂😂😂 akuchedwesa ndi chakwera

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5oАй бұрын

    You. are. wrong. it. Is. People. at. the. grassroots. who matters not individuals

  • @PartsonMdeza
    @PartsonMdezaАй бұрын

    🤣🤣🤣 iponden fadah kkk

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hnАй бұрын

    Ofufuza ngozi akuti, khoswe akakhala pakhate sapheka

  • @SteveChapola
    @SteveChapolaАй бұрын

    Asiyeni atuiuka chifukwa chake achakwera apha chirima ndipo ndizoona

  • @lastonmasoatenganji-bs5gf
    @lastonmasoatenganji-bs5gfАй бұрын

    Osamayiwala ku mudzi kaamba kokomedwa ndi maidyaidya chifukwa tsiku Lina amadzakusandutsa mtsamiro wa mfumu ikadzamwalira.

  • @michealchaomba9761
    @michealchaomba9761Ай бұрын

    😂😂😂 President wake utiyo mukudikira kuti azuzuleyo

  • @MarthaBanda-ye4pt
    @MarthaBanda-ye4ptАй бұрын

    Koma Wonder Ati kukura mtima 😂😂😂😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥uyatseni basi ng'alulani basi

  • @user-ru4px8os2v
    @user-ru4px8os2vАй бұрын

    Anthu ake ndi chimwendo banda,howeh mkaka,zikhaleng'oma ndiomwe akuyenela kuchoka

  • @ThandiMbewe
    @ThandiMbeweАй бұрын

    Musamamuzile zochita president, yekha samawona???

  • @Extratremendouszeus

    @Extratremendouszeus

    Ай бұрын

    President wake uti Ma comments 100 wa MCP yekha .chita manyazi😅😅

  • @SteveChapola
    @SteveChapolaАй бұрын

    Chakwera ndiwofoka koma kumagaanthu chimenecho ndiye chitukuko.chake

  • @NdazionaKumcheza
    @NdazionaKumchezaАй бұрын

    Ine dakalira malemu za chipani tizitaye uko aaa

  • @YusufuUsumani
    @YusufuUsumaniАй бұрын

    agaluwa alilimosi ndi chachera

  • @JudithMaida-ug4oi

    @JudithMaida-ug4oi

    Ай бұрын

    Mumatiimilira big hands for you

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuziАй бұрын

    Osamayakhura ngat akupatsani za lent kung'alura basi ukuva iwe ndevuzamwayi !!

  • @user-ql8nf2vb8s
    @user-ql8nf2vb8sАй бұрын

    Inu a times muyang'ane mgwirizanou kuchokela mmbuyo inunomwe mumaunikira mgwirizanou mmene umayendela chilima asanamwalile asiyeni ausi ali ndigululawo odya zake alibe mulandu

  • @MuhamadYassin-ye4hn
    @MuhamadYassin-ye4hnАй бұрын

    Mumakwana mabigi