CRUISE 5 WITH GEORGE THINDWA
George Thindwa is a curious man. He is the Executive Director of the Association for Secular Humanism in Malawi and a confessed atheist. He says he has not set his foot in church, and doesn't see any need to. He does not believe in the existence of God or even the Devil. He is a well-accomplished Economist and once headed the Economics Association of Malawi - ECAMA.
Follow this program and hear more about his background, family and his arguments on how he thinks the world came into being.
Пікірлер: 76
Ndiyambe ndikuthokoza aChakhaza pocheza ndi mkuluyu, poyamba background yake ( childhood development ) Ku mbali ya chipempedzo sinali bwino .Chinanso nchakut sakufunika kumuweruza koma kumupemphelera kuti apulumutsidwe ndi Ambuye Yesu khristu pot malemba akut mu nthawi yakusadziwa Mulungu analekelera ,nkhan siyongopita Ku mpingo koma kumdziwa womtumikira monga zinachitikira pa machitidwe atumwi9 ( nkhan ya mayitanidwe amtumwi Paulo).Kuonjezera apo Mr Thindwa choti mudziwenso nchakuti maphunziro ngakhale Ali ofunika simayankho amavuto onse amoyo uno ndikupatsani chitsanzo cha nkhani ya m' bible mu buku LA machitdwe atumwi chapter16:16-40 pa nkhani yomwe anamangitsa Paulo ndi Sila.Mutha kuona kut chayambi cha matenda awobwebwetuka uja monga luka ( wolemba bukuli) akufotokozera sichimene adotolo amatenda amisala angafotokoze .Akatswiri azachuma sangafotokozenso out chinsinsi cha kuchita bwino kwa omwe amapindula ndi zimezi ndi chiyan? Komanso gwero lakuvutika kwa wodwala uja? Palinso nkhani zawomenyera ufulu anthu kuyambira wodwalayo,Atumwi aja ngakhale amene anabesa chuma chawo kudzera mzomwe zimachitikazi palibe chomwe angachite munyengo ngati izi.Akupatsan funso mwadwala chipatala chalephera wina atakupempheleran nkuchira mu dzina LA Yesu Khristu mwayankha mododomatu? Mwinanso titakamba za Vuto la uhule anthu alangizidwa kuyipa kwa vutoli kupasidwa ndalama out apeze zochita koma osasintha enanso ndalamazo nkukhala Nazi koma osasintha Alonso ophunzira taonani pano Dziko likupereka ufulu kwa achinyamata kutenga njira zolera chikhalirecho zambiri sizawateteza kumatenda opatsirananapogonan KO'd akuchuluka otenga matendawa mdzina LA ufulu tinene kut zikuyenda ?mutha kuona kut Chifukwa chakuti chiwanda chili mkat mwa munthu uja sichinachotsedwe vuto lizingozungulira Muli ndi maphunziro abwino pezan zochita zabwino moyo wanu uli mdzanja la Yehova yang'aniran mathero ake Hebrews9:27 komanso Ku Genesis 3 akut unapangidwa Ku nthaka komwekonso udzabwelera bwanji maphunziro alibe yankho Ku vuto la imfa? Ndibwelenso Ku machitidwe 16 chimene chinapangitsa Paulo kuzindikira gwero la vuto lija ndiye mphamvu ya mzimu woyera( Mzimu wa chidziwitso ) Yemwe mungampeze mutalapa ndikuvomereza Khristu Yesu ngat mpulumutsi wa moyo wanu ( machitidwe2:38) nkhoswe imene Ambuye Yesu anawauza ophunzira akekudzawatumizira ndikuwatsogolera mu choonadi komanso kuvumbulutsa zinsinsi zochekera kwa Mulungu kudzera mwa mwana wake Yesu Khristu.Chiuta wawe namwe zuwa liweme.
Well educated man koma omvetsa chison eeeeeee ayi, anthu anga akuonongeka chifukwa cha kusadziwa.
Nthidwa ndi Genious, His brain is superpower.....! You're not alone Mr.
Powerful God always with him that's why he like Rabecca Malope songs because in doing that he is praying
@andreamillar9896
5 жыл бұрын
Kuyipa kwa Makolo athu potsatengera Ana athu ku Church ndizimenezo a Bambo awu Satanic. Teach a child to know God while he is still young.
Uphawi umapangitsa uchimo.izi akupanga pofuna ndalama.the songs he likes are highly spiritual. God loves you mumbuli wanuwo
@mwaibanda5877
Ай бұрын
Unfortunately he is not as poor as you think.
@AngungaThatcherNgoma
Ай бұрын
Yes
These are nothing but the facts
And chimene chidakusangalatsani kuti muzikonda nyimbo za Rabecca ndi umulunguwo please musabisale bambo
Akufunika kumupemphemphelela
Koma zikomo🙌🙌 eeee
Long live George
A Thindwa Rabecca amaimba gospel nde mumapempheranso.
Kodi National Anthem ija amayimba nawo kapena amaiwona kuti ndiyolakwika?
Ati Mulungu kulibe, kuyankhula kwa zitsiru.😏
Akuluwa a Eliya aposatu😆😆
Thanks for the enlightenment, this is absolutely awesome
Joab ndi #1 kkkkk wampanikizatu munthuyu
Titha kuphunzira kwambiri koma nkukhalabe opanda nzeru ngati akuluwa, ndi Mulungu Amene amapereka mphepoyo kutidziwitsa kuti mmadzi simuli bwino ndiye wina kupanga ignore that plain warning.
this guy
Eiiiish ambuye akukhululukireni
Dzimene mukuyankhula madala ndizopanda nzelu
Bible limati, “ Chisilu chimati kulibe Mulungu “ I guess the man so just so ……Let me save my word.
Humble man friendly person, I'm very sorry for that papa about being arrested for the mcp government by Dr Banda
God is calling him, that is why he loves Rabecca malope. God Himself will make way to bring this man to Himself. He is God of mercy.
Adzakumane ndi wa njoka ujaface to face adzakambilane bwino
Chamba
That is according to him, (he doesn't believe in God) not you and me, so leave him alone. It's not up to us to judge him.
@ralphhenderson5312
5 жыл бұрын
sizoona ngati munthu akutayika akonzedwe akusokoneza life is too short usakhale mbuli
@truthtellerlastonk.m.p4985
3 жыл бұрын
@@ralphhenderson5312 who told you kuti akutaika????
Nanu munyanya mwakumana ndi wen wen Satanists
komadi madala awa sangangokhalakhala,akuyenela amadya chamba
Poor soul, just being intelligent as he is explaining it's God's blessing.
Bola a Eliya aja amadziwa kuti Mulungu aliko osati phwephwa izi
God forgive him!
Inde mdala
But Rebecca Malope is a Gospel artist
@ralphhenderson5312
5 жыл бұрын
Nchifukwa chake tikuti ndimbuli sakudziwa chomwe akupanga Mulungu amukhudze
Mulungu adzikukhululukilani madala
@truthtellerlastonk.m.p4985
3 жыл бұрын
Apanga tchimo lanji???
Satana uja ndamuona ndi maso lero😮
Akuluwa mutu ukugwila koma
All am seeing is confusion from this guy. He was contradicting himself during the chat
Drange kwambir kapen fodya Wa chamba😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Looking at the comments it clearly shows how ignorant the so called christians are: Calling the non believer osazindikira. you guys need enlightment for sure dont just believe for the sake of believing
@georgesiwale8127
Ай бұрын
Yes, I am wondering too. We need to wise up
@simonabraham7241
Ай бұрын
For sure, these so-called christians are something else 😂😂😂
Ndi omvetsa chisoni, infact he is worse than the devil himself. The devil doesn't dispute the existence of God, according to the book of Isaiah and Ezekiel, the devil wants to be like God the most high. This old man is totally out of his mind.
Bible linanenakale kuti the fool say there is no God, ndiye mukamawona anthu atelewa wosamadwabwayi p
Ngati chili chamba chikugwira ntchito
Kkkkkkkkkkkkkk
The holy spirit gives one the ability to sense the presence of God. If the spirit is not in you then there is no sense.
@youmad9087
3 жыл бұрын
What spirit is that?
@aminbwanali3954
2 жыл бұрын
This man is the brother of falawo he deserved to be panished
Mkuluyu wangokura koma nzeru mulibemo. Google mwini wache ndi muthu osati mulungu ndipo nthawi zina siigwira network
Muziwerenga Bible Mr thindwa
@apatsamuula4676
2 жыл бұрын
Alibe thawi yowerenga bake akuyakhula xoduka mutu
Kkkkkkkk koma Joab umakumana nazo inetu abambo awo komwe akulowa sindikudziwako.
Bambowa ndi chiwanda, akufunika mapephero.
@truthtellerlastonk.m.p4985
3 жыл бұрын
Zaziiii zenizeni 🚮🚮🚮 mapemphero achani??
koma abale mmmmm zodabwisa kwabasi munthu wankulu ngati ameneyu?? 😯😯😯
This atheist akungofunika maumboni amachilitso. Funso lakuchipatala lamuyimitsa mutu mpaka wavomera kuti akhoza kukhulupilira kkkkkkkkkkkkkk
aaaah kumvets chisoni you dont believe in God- you missing out on a lot hey.
@youmad9087
3 жыл бұрын
Omvetsa chisoni ndi iweyo
According to the Bible Mr. George Thindwa ndi achitsiru, that's it and i can prove it and he has proven it himself kuti, he is a fool.
Anangokula nzeru alibe🚮
@simonabraham7241
Ай бұрын
Ndiye mumlalikira bwanji ndi mau onyozawo?