Always your the best all the time mr president Bonie Kalindo
@anicakandiado23 күн бұрын
Kulankhula mwachilungamo. UTM tsegulani maso. Tulukani mu tonse alliance monga akunenela Bon Kalindo please. A MCP asakupusitseni ife tili mbali yanu ndi SKC osaopa, osatopa, osafooka 💪
@KondwaniMwasinga-rs6kv23 күн бұрын
Born kalindo🔥🔥🔥🎷🎷
@AlbertEngelbercht23 күн бұрын
Kalindo is trying his best,chikufunika osusa agwirane manja!,ku UTM apereke mpata kapena position imene Mary chilima angatenge icho chiperekeranso mphanvu ina yapadera muchipani.
Bon kalindo akunena zowona lelo muchoke ku mcp mukapitiliza ndiye kuti mukusangalala ndi ife ya chilima chipani chimene chingawine ndi UTM kampeni wake zikolose lapasi lipanga saport
@user-oq8uv9xi5s23 күн бұрын
🎉🎉🎉 following
@ListonFrancis23 күн бұрын
Mbambande Bon Kalindo
@WestonGawaza23 күн бұрын
Mayi chilima to be president, braund banda,mwana wachilima awa kaliyati, awa musankhemo mumozi ankhale president mwana wa chilima anyamata ose ankhala ndi chidwi
@KudaKaira23 күн бұрын
The DC
@TaongaChibuwu22 күн бұрын
Zikomo bwana DC UTM yitulukedi kumeneko iyime pa yokha basi
@PempheroAlufandika23 күн бұрын
Mumatiimilira a bon
@MaxwellMakoka23 күн бұрын
Mr DC 2025 woyyeee.
@Lazarus-qo1sl23 күн бұрын
Chilungamo ndimwano❤ The DC pick up man
@user-dp7bc7yy6s23 күн бұрын
A UTM uthenga ndiumeneo zili ndiinu kunyalanyaza kapena kutengapo kanthu km mawa pangatalike muzawakumbukira mau a Bon sadutsa pachabe
@AlinafeSolomoni23 күн бұрын
True
@AhmadShariff-bk3rr23 күн бұрын
Tiyeni tiyeni tiyeni Mr DC
@valenceemmanuel7423 күн бұрын
Like this guy or not , but he is very sharp
@fahadmilanzi23 күн бұрын
Kalindo amalankhula zoona uyu ndi mpulutsi.
@MerryWayson23 күн бұрын
Na pa Bone Kalindo palibeso same same Mtanyiwa anthu awa amanena chilungamo chokhachokha
@Peter-vc6ll23 күн бұрын
Nice
@TalazanGamah23 күн бұрын
Powerful spetch
@InnocentMatemba-y1k23 күн бұрын
Big up de DC our pool p
@LenoMvula23 күн бұрын
My vote kalindo umatha umatiimirila
@AndreaSignala-hk2yg23 күн бұрын
It's true bwana president woyamba wa anthu osauka muno Malawi
@priscillamangata402323 күн бұрын
President wathu Mr DC
@willardkajalika-m8g23 күн бұрын
😹😹😹 iwe umakwana aaa nilinje mau
@user-nf3ik3ff6y23 күн бұрын
The Dc bon kalindo ❤
@user-je8jm5uy1q23 күн бұрын
Koma Mai kaliyati ndi kagulu kanu choonde nvelani kulira kwa anthu ngati ku UTM kuli anthu olimba nde ndinuyo mumakhala chifupi ndi Chilima musakomedwe ndi ndalama mukwiitsa anthu ochuluka nthawi yatha kale iyi musanvere MCP kukunyengeleleni ndi ndalama misozi ili manso ndithu mutenga tsoka
@MathewsChitambe
23 күн бұрын
Zoona mb'ale
@khuzenigunya23 күн бұрын
Kalindo good advice
@MathewsChilenje23 күн бұрын
Umaitha bon
@FrankAndsen23 күн бұрын
Khan nd yoona
@LottiAffati23 күн бұрын
kalindo umakwana ase
@MussaAmadu-o9f23 күн бұрын
Very true
@MuhammadSamson-yz1kl23 күн бұрын
A UTM mukapanda unvera za bon kalindo muzalira moyo wanu onse
@Moses5123 күн бұрын
The Dc bon kalindo 🎉🎉🎉
@OwamiSimeon23 күн бұрын
Kalindo more 🔥 ❤
@AgnessMzengo23 күн бұрын
Wise man
@ArnoldKamanga-r6k23 күн бұрын
Tikumupemphani a Born kalindo bwelelani ku UTM please
@LuundoJohnkabage
23 күн бұрын
Ndipo president akakhale iyeyu ndimunthu wamaso mphenya❤❤we love him❤
@jeladiaustain23 күн бұрын
❤❤❤❤❤❤❤
@user-bf1sz6pu1n23 күн бұрын
What if mrs Chilima is not a politician? Komanso akuti anthu azilowa kuchipinda ndi candle nkumakatchula dzina la Chilima kodi Chilimayo wasandukano mulungu?
@WestonGawaza23 күн бұрын
Brayani Banda ndimunthu wa chikondi ndi ziko Lake mayi cilima tiwona ngati chilimayo alipo anthu tivota ambiri mwana wachilima anakonda achinyamata ndiye achinyamata ose ali ndi ife
@BlessingsMaheya23 күн бұрын
Sanena boza uyu
@chifundobuledi23 күн бұрын
🎉More fire!!!!!!!!!!!
@user-fz3gu2ez1o23 күн бұрын
Tidziwe basi. Ma traitor tiwadziwa lero
@Shelifibraheem23 күн бұрын
Our freedom fighter ndiwe kawawa ndithu
@MaxwellumbiriLumbiri23 күн бұрын
Bon kalindo umakamba zoona
@Zamwano23 күн бұрын
Kd zimenez zitithandiza osapita pa galaundi kukapanga ma demo ngati tikuona kuti zithu sizilibwino,, Timakunyadilan mr DC,Km please dziko ndilathu tiyeni tipange zaku Kenya 🇰🇪 basi
@FrancisNyayi
23 күн бұрын
Mmm
@OsumaniJaffali23 күн бұрын
Amakwana koma ❤
@BensonChakalamba-db7uf23 күн бұрын
The problem is anthu akumudz unthengawu suwapeza cz of social media
@amfanamane23 күн бұрын
My vote umakwana
@user-fi7ko7bl6f23 күн бұрын
The DC mwana oopsa kwambiri satekeseka ndi Uniform ya a police,ingankhale Unyolo. Tell them 😅😅😅😅
@BlessingsMikeyasi23 күн бұрын
The DC ,lankhula chilungamo bas
@IssaMmadi-zh8un23 күн бұрын
Bhooooooooo nikalindo😂❤
@SolomonNjolomole23 күн бұрын
Gwilizano a mcp adayedzeka amamukana chilima dzuwa likuswa mtengo achakwera kumayankhula zonyazitsa chilima Ali pompo chilima sanapuse sanayambane ndi munthu ndie lero zatani RIP chilima.
Пікірлер: 148
Bon kalindo amalankhula zoona zokhazokha koma anthufe timangoti ndi wama comedy let's support him as malawians
Kuyankhula mopanda mantha ngati wakhalira mfuti Bon kalindo 😮😮
@OscarChizula-qr4bi
23 күн бұрын
Ndpo inu
Uyu ndiye activits yemwe timamudziwa, Bon kalindooooooo!! Mwana owopsa kwambiri.
Wamisala anaona nkhondo,,lero Bon kalindo mukumuyamikila koma mmene munkamunyozela siizi😂😂😂😂
Thanks sir for ur update
Ati amakutengan ngat manyi😂😂😂😂 chi booooniiiiii kalindoooo
Kalindo amatha kwambili❤
Your the best the DC bon kalindo❤
Good advice sir.
God bless you Kalindo
@BlessingsPhiri-fv5gs
23 күн бұрын
Umakwana
Good advice
Komatu bon kalindo amayakhula ngati wamisa koma ndizoonadi zimene amayakhula anhtu inu muzichenjera
Good advise Mr born kalindo thank you 😅
Utm siingatuluke mugwilizano ngakhaleso atatuluka palibe chazelu chomwe angapeze
Uyu ndiye ❤
Always your the best all the time mr president Bonie Kalindo
Kulankhula mwachilungamo. UTM tsegulani maso. Tulukani mu tonse alliance monga akunenela Bon Kalindo please. A MCP asakupusitseni ife tili mbali yanu ndi SKC osaopa, osatopa, osafooka 💪
Born kalindo🔥🔥🔥🎷🎷
Kalindo is trying his best,chikufunika osusa agwirane manja!,ku UTM apereke mpata kapena position imene Mary chilima angatenge icho chiperekeranso mphanvu ina yapadera muchipani.
Yomweyo fadaa🎉
Mr Kalindo mukutitsegula mmaso kwabasi keep it up
President wathu wathu,Mr Kalindo lero ndilomwe tidziwedi kuti UTM ipitilira ndipo SKC waphera chilungamo.
I love you so much
U always stand in true mr Bon l love u more than
Salute
Chilungamo chimamasula go ahead the DC
The DC🔥🔥🔥
The DC mwana ohopya kwambili
Big up to you 🎉🎉🎉🎉🎉 umatha kung'alura
DC Huma kwana
Mumaitha bwana d c ndi more pachilungamo😊
Bwana DC mumatiimilira
Bon kalindo akunena zowona lelo muchoke ku mcp mukapitiliza ndiye kuti mukusangalala ndi ife ya chilima chipani chimene chingawine ndi UTM kampeni wake zikolose lapasi lipanga saport
🎉🎉🎉 following
Mbambande Bon Kalindo
Mayi chilima to be president, braund banda,mwana wachilima awa kaliyati, awa musankhemo mumozi ankhale president mwana wa chilima anyamata ose ankhala ndi chidwi
The DC
Zikomo bwana DC UTM yitulukedi kumeneko iyime pa yokha basi
Mumatiimilira a bon
Mr DC 2025 woyyeee.
Chilungamo ndimwano❤ The DC pick up man
A UTM uthenga ndiumeneo zili ndiinu kunyalanyaza kapena kutengapo kanthu km mawa pangatalike muzawakumbukira mau a Bon sadutsa pachabe
True
Tiyeni tiyeni tiyeni Mr DC
Like this guy or not , but he is very sharp
Kalindo amalankhula zoona uyu ndi mpulutsi.
Na pa Bone Kalindo palibeso same same Mtanyiwa anthu awa amanena chilungamo chokhachokha
Nice
Powerful spetch
Big up de DC our pool p
My vote kalindo umatha umatiimirila
It's true bwana president woyamba wa anthu osauka muno Malawi
President wathu Mr DC
😹😹😹 iwe umakwana aaa nilinje mau
The Dc bon kalindo ❤
Koma Mai kaliyati ndi kagulu kanu choonde nvelani kulira kwa anthu ngati ku UTM kuli anthu olimba nde ndinuyo mumakhala chifupi ndi Chilima musakomedwe ndi ndalama mukwiitsa anthu ochuluka nthawi yatha kale iyi musanvere MCP kukunyengeleleni ndi ndalama misozi ili manso ndithu mutenga tsoka
@MathewsChitambe
23 күн бұрын
Zoona mb'ale
Kalindo good advice
Umaitha bon
Khan nd yoona
kalindo umakwana ase
Very true
A UTM mukapanda unvera za bon kalindo muzalira moyo wanu onse
The Dc bon kalindo 🎉🎉🎉
Kalindo more 🔥 ❤
Wise man
Tikumupemphani a Born kalindo bwelelani ku UTM please
@LuundoJohnkabage
23 күн бұрын
Ndipo president akakhale iyeyu ndimunthu wamaso mphenya❤❤we love him❤
❤❤❤❤❤❤❤
What if mrs Chilima is not a politician? Komanso akuti anthu azilowa kuchipinda ndi candle nkumakatchula dzina la Chilima kodi Chilimayo wasandukano mulungu?
Brayani Banda ndimunthu wa chikondi ndi ziko Lake mayi cilima tiwona ngati chilimayo alipo anthu tivota ambiri mwana wachilima anakonda achinyamata ndiye achinyamata ose ali ndi ife
Sanena boza uyu
🎉More fire!!!!!!!!!!!
Tidziwe basi. Ma traitor tiwadziwa lero
Our freedom fighter ndiwe kawawa ndithu
Bon kalindo umakamba zoona
Kd zimenez zitithandiza osapita pa galaundi kukapanga ma demo ngati tikuona kuti zithu sizilibwino,, Timakunyadilan mr DC,Km please dziko ndilathu tiyeni tipange zaku Kenya 🇰🇪 basi
@FrancisNyayi
23 күн бұрын
Mmm
Amakwana koma ❤
The problem is anthu akumudz unthengawu suwapeza cz of social media
My vote umakwana
The DC mwana oopsa kwambiri satekeseka ndi Uniform ya a police,ingankhale Unyolo. Tell them 😅😅😅😅
The DC ,lankhula chilungamo bas
Bhooooooooo nikalindo😂❤
Gwilizano a mcp adayedzeka amamukana chilima dzuwa likuswa mtengo achakwera kumayankhula zonyazitsa chilima Ali pompo chilima sanapuse sanayambane ndi munthu ndie lero zatani RIP chilima.
@user-eh1mg3ww6d
23 күн бұрын
Ndipo ndizoonadi amamukanadi chilungamo ndiye lelo ayanja otsalao
Usazafe kalindo uzangotsowa ngati eliya
the dc
Kmat uyu tiyen Tzimuvela zimene amayankhulaz
Makwana mr keep it up
The DC mulomwe wathuwathu odziwa zinsinsi
The DC kkkk konda u ife
Umakwana winiko
The DC agogo anga akufuna azakuoneni
Boss
In short Utm ibwerere ku DDP....tigwetse vinyau tikinze dziko
Good Good news
Dc 🎉🎉🎉🎉
The Dc mawu ako a koma akagonela
Mzimu wa bwana Chilima uwavuta.mukaone maruwa ngati akukanika kufa .musamale kwambilitu.
Dc mwana oooopsa kwambili
Mumakwana bwana born kalindo
THE DC PANGOLINI 💪💪💪💪💪
boooooon kalindo!