Bon Kalindo lero pa 11 July kufotokoza mopanda kuopa aliyense - “MUNDIMVA NDIPO SINATI”

Пікірлер: 81

  • @user-ix2ux5ss1b
    @user-ix2ux5ss1b19 күн бұрын

    More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika

  • @EversDman
    @EversDman18 күн бұрын

    Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯

  • @PeterKasiya
    @PeterKasiya18 күн бұрын

    Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji19 күн бұрын

    Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏

  • @LuyoloTlhapane
    @LuyoloTlhapane12 күн бұрын

    A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila

  • @MomeryPhiri
    @MomeryPhiri18 күн бұрын

    ❤❤❤❤❤❤❤ love it

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k19 күн бұрын

    bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo

  • @user-xm5cq1fb8g
    @user-xm5cq1fb8g18 күн бұрын

    Ulemu wanu big❤❤❤❤❤

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp18 күн бұрын

    😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi

  • @neemahkapatamoyo9563
    @neemahkapatamoyo956319 күн бұрын

    Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌

  • @user-dj6rc3lc4t
    @user-dj6rc3lc4t19 күн бұрын

    Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana

  • @FarookRaphael
    @FarookRaphael19 күн бұрын

    More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem19 күн бұрын

    Big up bro

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i19 күн бұрын

    Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂

  • @FlorryVugy
    @FlorryVugy19 күн бұрын

    A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂

  • @UthmanKapungu
    @UthmanKapungu19 күн бұрын

    Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife

  • @AffickChaona
    @AffickChaona16 күн бұрын

    ❤❤❤❤❤

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j19 күн бұрын

    Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima. Agalu a anthu ndithu

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w20 күн бұрын

    Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto19 күн бұрын

    Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @NdawaPhillipfortunePhakatie
    @NdawaPhillipfortunePhakatie19 күн бұрын

    Motor 💥 kalindoooo

  • @user-wm4rs4kd7d
    @user-wm4rs4kd7d19 күн бұрын

  • @user-zt3gv7md6x
    @user-zt3gv7md6x18 күн бұрын

    Zoona amwene

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs19 күн бұрын

    😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i19 күн бұрын

    Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂

  • @nicholasmutano6017
    @nicholasmutano601719 күн бұрын

    Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?

  • @PeterMaulana-qk5uq
    @PeterMaulana-qk5uq19 күн бұрын

    Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!

  • @FwasanMwenefumbo-zq7sg
    @FwasanMwenefumbo-zq7sg19 күн бұрын

    The DC 🔥

  • @BernadettaTengula
    @BernadettaTengula18 күн бұрын

    Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂

  • @ericlarks8165
    @ericlarks816519 күн бұрын

    ,🔥🔥🔥🔥

  • @JoyceChitsulo-mw7wg
    @JoyceChitsulo-mw7wg19 күн бұрын

    Makosana apa nde mwapita

  • @FrankMilias-og3js
    @FrankMilias-og3js19 күн бұрын

    Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko

  • @user-hq8fw5hz2l
    @user-hq8fw5hz2l19 күн бұрын

    Awa ndie mawu

  • @user-dm6xq6cp1m
    @user-dm6xq6cp1m19 күн бұрын

    Ai zikomo 🥱

  • @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa
    @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa19 күн бұрын

    Ambuye akudalitsen

  • @benjulius6070
    @benjulius607019 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂

  • @gerrardgladstone2473
    @gerrardgladstone247319 күн бұрын

    Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi19 күн бұрын

    Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi

  • @ChisomoamitoniSauzandeamiton
    @ChisomoamitoniSauzandeamiton19 күн бұрын

    bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu

  • @SmartMoles
    @SmartMoles19 күн бұрын

    Zofunikila kulangura mwayangure kumene

  • @VincentMalika-w7x
    @VincentMalika-w7x19 күн бұрын

    Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath

  • @directorkfuture118
    @directorkfuture11819 күн бұрын

    Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂

  • @user-tw5iw7gf2v
    @user-tw5iw7gf2v19 күн бұрын

    😂😂😂😂 mpaka muchenga license

  • @RamseyWasi
    @RamseyWasi19 күн бұрын

    Blasa, Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC) My opinion: Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga19 күн бұрын

    Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga19 күн бұрын

    Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha

  • @user-kx4cj7iu9q
    @user-kx4cj7iu9q19 күн бұрын

    Dc

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda589119 күн бұрын

    Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk

  • @HendersonDziwa
    @HendersonDziwa19 күн бұрын

    Dzelu zachepa kkkk

  • @DaudiAbdullah-o5l
    @DaudiAbdullah-o5l19 күн бұрын

    Mumatiyimilila

  • @TshepoModise-xs4qu
    @TshepoModise-xs4qu19 күн бұрын

    Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee

  • @maxwellcaptain3937
    @maxwellcaptain393719 күн бұрын

    Kalindo samaopa😂😂

  • @PeterGrant-ih1sr
    @PeterGrant-ih1sr19 күн бұрын

    Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga19 күн бұрын

    😂😂😂😂😂 koma DC

  • @D.RJALLI-qo6yd
    @D.RJALLI-qo6yd19 күн бұрын

    Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns19 күн бұрын

    Ati kutitola kapena chani

  • @JuliusMunthali-z7j
    @JuliusMunthali-z7j19 күн бұрын

    Awuzeni

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward19 күн бұрын

    Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto

  • @user-ls5zj8qn6k
    @user-ls5zj8qn6k19 күн бұрын

    Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo

  • @AnthoniohMazengera
    @AnthoniohMazengera18 күн бұрын

    Hahahahahahahahahaha😂😂😂

  • @Aluwenkareem-ev3ro
    @Aluwenkareem-ev3ro19 күн бұрын

    😂🤣😂🤣

  • @lytonmaseko4534
    @lytonmaseko453419 күн бұрын

    😂😂 kung'alulatu

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi871316 күн бұрын

    😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp

  • @GiftKulture
    @GiftKulture19 күн бұрын

    🤣🤣🤣🤣 mipunga

  • @AaronLitete
    @AaronLitete19 күн бұрын

    Kkkkk boma lopusa

  • @YonaMartin-kb3do
    @YonaMartin-kb3do19 күн бұрын

    😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe

  • @user-yl3lg5fk8f
    @user-yl3lg5fk8f19 күн бұрын

    Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious

  • @sir-wanton-2001
    @sir-wanton-200119 күн бұрын

    Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo

  • @ikmusic-s9f
    @ikmusic-s9f19 күн бұрын

    koma nde eeee mpaka licence mchenga

  • @YohaneMbewe-u4k
    @YohaneMbewe-u4k19 күн бұрын

    😂😂😂😂

  • @user-ky8us1ff5b
    @user-ky8us1ff5b19 күн бұрын

    😅😅😅😅

  • @wangachindeya8577
    @wangachindeya857719 күн бұрын

    Bigiliman naweni

  • @user-vn1wq6wg6i
    @user-vn1wq6wg6i19 күн бұрын

    K.K😂

  • @PhillipMtonga-g7o
    @PhillipMtonga-g7o19 күн бұрын

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance

  • @BenjaminKayembe-j7j
    @BenjaminKayembe-j7j19 күн бұрын

    km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km

  • @Kachelephiri
    @Kachelephiri19 күн бұрын

    Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.

  • @ChristopherKawilam

    @ChristopherKawilam

    19 күн бұрын

    Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe

  • @ChristopherKawilam

    @ChristopherKawilam

    19 күн бұрын

    Yamba wapita Kaye Ku school ya mkaka uziwe kulemba...... galu iwe

  • @user-wz6jy3re8n
    @user-wz6jy3re8n19 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂

  • @MadalitsoManyozo

    @MadalitsoManyozo

    19 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @myheartforkids2876
    @myheartforkids287619 күн бұрын

    😂😂😂😂😂

Келесі