BON KALINDO KUYANKHULA PAMBUYO PA CHIGAMULO CHAKU COURT 10 July 2024
Жүктеу.....
Пікірлер: 65
@MuhajirinaSaid16 күн бұрын
Keep it up mr Dc
@ForsterThawan16 күн бұрын
Aaaaaaaaa koma kalindo ndi munthu wankulu kwambili ndipo amayankhula saopa kanthu
@user-lz5yv4vj6h
16 күн бұрын
Kkkkk koma Born aaaa ndi president wanthudi ,l salute you sir
@josephinemisomali684016 күн бұрын
Ndimadikira Dc kuti lero atichani apa nditha kukagona 😂😂😂 Boni kalindooooooooo!!!
@NelsonbastonMandela16 күн бұрын
Kkkkl mpaka police 200 koma bon kalindo ndimunthu okwiya kwambiri 😂😂😂😂😂
@robertchitsulo800616 күн бұрын
Bon kkkkkkkkk akuti aputa milandu yambiri iwe ndi 1 basi kkkkkk
@SamfrayGvng14 күн бұрын
Eeeee ai ndagonja nanu big up a 🙋DC
@user-mk7fh5ml8s15 күн бұрын
Mr kalindo ife tidalira inu basi❤❤❤
@user-jk8sh7fh2d16 күн бұрын
Wakumuzi kwenikwenni za pa social media -zi saziziwa kuti inu muma -aimilira
@user-uc1pd1tc2x16 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂Nyau kumva pain 😂😂😂
@AufiThera15 күн бұрын
Kod Aku Germany aja bas angotithera ndalama mosemuja lipot osabwerensa aaaa ndiye angopita kwawo wapas amenewo iyaaa
@TougiedaAjam15 күн бұрын
It's the Dc keep it
@PeterKathewera15 күн бұрын
Kodi kwanu sanakuvoteren bwanji😢😢
@AlickMakunganya-o4w15 күн бұрын
Ichichi sichamasewera Adaaa😂😂
@PetroMatias16 күн бұрын
🤝🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🤝🤝🤝🤝
@user-hh4wn4vf9e15 күн бұрын
DC 🥰
@EvsonNgurube15 күн бұрын
Bon kalindooooooo
@Homeofpeace32116 күн бұрын
Za Imfa Ya Chilima Tisaopsezane, Ngati Simunamuphe Tiuzeni Kuti Chinachitika Ndichani? Ku MCP musabise zinthu zoti munapanga nokha, Chakwela Ukhale ndimanyazi Ubusa wake Uti Unkapanga iwe Okupha Nzako Chifukwa Chautsogoleli?
@AufiThera15 күн бұрын
Wanthu wanthu DC 💪
@user-hh4wn4vf9e15 күн бұрын
DC ❤
@MariamJaffali16 күн бұрын
Ndodo ija ituluke DC tatopa ndi chakwera ife kkkkkkkkkkk the DC ❤❤❤❤
@sir-wanton-200114 күн бұрын
Kkkkk chikumvesa kukoma a Malawi ambili
@user-fz3gu2ez1o14 күн бұрын
Kkkkkkkk Mwana ovuta kulera Hehehehe
@MisheckAselo16 күн бұрын
Amafuna kukuipisirani Mr DC koma akunama 💪
@user-uc1pd1tc2x16 күн бұрын
Bon Kalindo the DC (The most dangerous child)❤❤❤❤❤❤
Пікірлер: 65
Keep it up mr Dc
Aaaaaaaaa koma kalindo ndi munthu wankulu kwambili ndipo amayankhula saopa kanthu
@user-lz5yv4vj6h
16 күн бұрын
Kkkkk koma Born aaaa ndi president wanthudi ,l salute you sir
Ndimadikira Dc kuti lero atichani apa nditha kukagona 😂😂😂 Boni kalindooooooooo!!!
Kkkkl mpaka police 200 koma bon kalindo ndimunthu okwiya kwambiri 😂😂😂😂😂
Bon kkkkkkkkk akuti aputa milandu yambiri iwe ndi 1 basi kkkkkk
Eeeee ai ndagonja nanu big up a 🙋DC
Mr kalindo ife tidalira inu basi❤❤❤
Wakumuzi kwenikwenni za pa social media -zi saziziwa kuti inu muma -aimilira
😂😂😂😂😂😂😂😂😂Nyau kumva pain 😂😂😂
Kod Aku Germany aja bas angotithera ndalama mosemuja lipot osabwerensa aaaa ndiye angopita kwawo wapas amenewo iyaaa
It's the Dc keep it
Kodi kwanu sanakuvoteren bwanji😢😢
Ichichi sichamasewera Adaaa😂😂
🤝🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🤝🤝🤝🤝
DC 🥰
Bon kalindooooooo
Za Imfa Ya Chilima Tisaopsezane, Ngati Simunamuphe Tiuzeni Kuti Chinachitika Ndichani? Ku MCP musabise zinthu zoti munapanga nokha, Chakwela Ukhale ndimanyazi Ubusa wake Uti Unkapanga iwe Okupha Nzako Chifukwa Chautsogoleli?
Wanthu wanthu DC 💪
DC ❤
Ndodo ija ituluke DC tatopa ndi chakwera ife kkkkkkkkkkk the DC ❤❤❤❤
Kkkkk chikumvesa kukoma a Malawi ambili
Kkkkkkkk Mwana ovuta kulera Hehehehe
Amafuna kukuipisirani Mr DC koma akunama 💪
Bon Kalindo the DC (The most dangerous child)❤❤❤❤❤❤
Mwana woipa kwambiri😂😂😂
🤣🤣🤣🤣 mpaka a police 200 kkkkk
The DC salute
The DC, ndipo anthu tizamulilira kwambri mkului nd ntchto yakei akazasamira mkono
The braval child of Malawi, Speak out without fear and favor! Bon kalindo, The DC...
😂😂😂😂😂the DC machine
Winiko the DC pachilungamo sumawopa iweyo umatha
❤❤❤❤❤ more fire 🔥
boni kalindo malawi 😂😂😂😂
Bon Kalindo
Mr Dc mumakwana inuyo tilinanu ife amalawi
The DC
zopanda ntchito zomwe ukulu inu mumalankhula
Chizagwira zipolopolo😅😅 iwe ndi machine, wait to destroy them with you
Umakwana DC
The DC🔥
It's plezident of poor people
The DC!
Uyu yekha timuteteza I swear
The DC 😂😂😂
Kulankhula wina aliyese atha kulankhula koma kuchita zakupsa...Bwana Bon kalindo akumalankhula koma ndi action yanji yomwe ikuchitika? We need kulankhula ndikuchita namaona progress..Mukatiuza zomwe mwapezazo kenako muzinenanso kuti tipanga izi pothana ndizimenezi...tisamangokhalira kumva mwana oopsa mmalankhulidwe, action nothing
@myheartforkids2876
15 күн бұрын
Inu mene mwayankhulamu mwapanga action yanji? Kkkkkkkkkk
@sir-wanton-2001
14 күн бұрын
Kkkk mbuli ife timakonda DC
@OnexAliMwale
14 күн бұрын
@@myheartforkids2876 Amene amawatsata omenyera ufulawa atha kudziwa kuti nthawi ya Bingu kunali Mavuto Bamusi ndipo amati akanena amapanga action ndipo Mpaka Bingu anasintha machitidwe azinthu zina, nthawi ya Peter kunali Timothy Mtambo, za amenewu mukudziwa zomwe amachita, Koma Bwana Bon mmmm tiyeni tizingomva Mwana oopsa komanso kung'alura kenako tiseke osaona chisintha...I always appreciate for actions not talking that's why tonse Government tikudana nalo coz nawoso kulankhula amatha koma kukwanilitsa kukuwavuta
DC mewafika
The DC umakwana
Chipangoline😂😂
Zamanyi basi kape ndiweyo akanadakhala Ofuna kupha akanampha iweyo umatisokoneka mutu amakutuma ndindani? Umango uwanamizila anthu wosawuka ndidziko lanji lomwe kungapezeke wolemera wose?
@musaphiri317
15 күн бұрын
Iwe akupasa zingati koma inu ndi onvesachifundo kupusa uchisru
@SamKaposa-i5c
15 күн бұрын
Nyau imeneyi itayeni
@EvsonNgurube
15 күн бұрын
Matako ako nyau iwe
@sir-wanton-2001
14 күн бұрын
Kape uyu
Even ur voice doesn't sound like a leader
😂😂😂😂😂
😂😂
Ati amangidwe ndamako
@user-uc1pd1tc2x
16 күн бұрын
😂😂😂😂😂Amangidwadi ndi amake a Chakwera 😂😂
@chifukanyo9447
16 күн бұрын
😂😂😂
@sir-wanton-2001
14 күн бұрын
Kkkk