BON KALINDO KUYANKHULA PAMBUYO PA CHIGAMULO CHAKU COURT 10 July 2024

Пікірлер: 65

  • @MuhajirinaSaid
    @MuhajirinaSaid16 күн бұрын

    Keep it up mr Dc

  • @ForsterThawan
    @ForsterThawan16 күн бұрын

    Aaaaaaaaa koma kalindo ndi munthu wankulu kwambili ndipo amayankhula saopa kanthu

  • @user-lz5yv4vj6h

    @user-lz5yv4vj6h

    16 күн бұрын

    Kkkkk koma Born aaaa ndi president wanthudi ,l salute you sir

  • @josephinemisomali6840
    @josephinemisomali684016 күн бұрын

    Ndimadikira Dc kuti lero atichani apa nditha kukagona 😂😂😂 Boni kalindooooooooo!!!

  • @NelsonbastonMandela
    @NelsonbastonMandela16 күн бұрын

    Kkkkl mpaka police 200 koma bon kalindo ndimunthu okwiya kwambiri 😂😂😂😂😂

  • @robertchitsulo8006
    @robertchitsulo800616 күн бұрын

    Bon kkkkkkkkk akuti aputa milandu yambiri iwe ndi 1 basi kkkkkk

  • @SamfrayGvng
    @SamfrayGvng14 күн бұрын

    Eeeee ai ndagonja nanu big up a 🙋DC

  • @user-mk7fh5ml8s
    @user-mk7fh5ml8s15 күн бұрын

    Mr kalindo ife tidalira inu basi❤❤❤

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d16 күн бұрын

    Wakumuzi kwenikwenni za pa social media -zi saziziwa kuti inu muma -aimilira

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x16 күн бұрын

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂Nyau kumva pain 😂😂😂

  • @AufiThera
    @AufiThera15 күн бұрын

    Kod Aku Germany aja bas angotithera ndalama mosemuja lipot osabwerensa aaaa ndiye angopita kwawo wapas amenewo iyaaa

  • @TougiedaAjam
    @TougiedaAjam15 күн бұрын

    It's the Dc keep it

  • @PeterKathewera
    @PeterKathewera15 күн бұрын

    Kodi kwanu sanakuvoteren bwanji😢😢

  • @AlickMakunganya-o4w
    @AlickMakunganya-o4w15 күн бұрын

    Ichichi sichamasewera Adaaa😂😂

  • @PetroMatias
    @PetroMatias16 күн бұрын

    🤝🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🤝🤝🤝🤝

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e15 күн бұрын

    DC 🥰

  • @EvsonNgurube
    @EvsonNgurube15 күн бұрын

    Bon kalindooooooo

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace32116 күн бұрын

    Za Imfa Ya Chilima Tisaopsezane, Ngati Simunamuphe Tiuzeni Kuti Chinachitika Ndichani? Ku MCP musabise zinthu zoti munapanga nokha, Chakwela Ukhale ndimanyazi Ubusa wake Uti Unkapanga iwe Okupha Nzako Chifukwa Chautsogoleli?

  • @AufiThera
    @AufiThera15 күн бұрын

    Wanthu wanthu DC 💪

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e15 күн бұрын

    DC ❤

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali16 күн бұрын

    Ndodo ija ituluke DC tatopa ndi chakwera ife kkkkkkkkkkk the DC ❤❤❤❤

  • @sir-wanton-2001
    @sir-wanton-200114 күн бұрын

    Kkkkk chikumvesa kukoma a Malawi ambili

  • @user-fz3gu2ez1o
    @user-fz3gu2ez1o14 күн бұрын

    Kkkkkkkk Mwana ovuta kulera Hehehehe

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo16 күн бұрын

    Amafuna kukuipisirani Mr DC koma akunama 💪

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x16 күн бұрын

    Bon Kalindo the DC (The most dangerous child)❤❤❤❤❤❤

  • @GracePhirie
    @GracePhirie15 күн бұрын

    Mwana woipa kwambiri😂😂😂

  • @allansili-rc9gc
    @allansili-rc9gc16 күн бұрын

    🤣🤣🤣🤣 mpaka a police 200 kkkkk

  • @williamchatha6139
    @williamchatha613915 күн бұрын

    The DC salute

  • @ShaibKudzinja
    @ShaibKudzinja16 күн бұрын

    The DC, ndipo anthu tizamulilira kwambri mkului nd ntchto yakei akazasamira mkono

  • @ZexNkhoma-p8t
    @ZexNkhoma-p8t16 күн бұрын

    The braval child of Malawi, Speak out without fear and favor! Bon kalindo, The DC...

  • @user-mi3fw1zg8b
    @user-mi3fw1zg8b15 күн бұрын

    😂😂😂😂😂the DC machine

  • @kondwanimandala4575
    @kondwanimandala457515 күн бұрын

    Winiko the DC pachilungamo sumawopa iweyo umatha

  • @KhalideNerve-mu1eq
    @KhalideNerve-mu1eq15 күн бұрын

    ❤❤❤❤❤ more fire 🔥

  • @lazarousnamakhwa6549
    @lazarousnamakhwa654915 күн бұрын

    boni kalindo malawi 😂😂😂😂

  • @IbrahimYusufu-z9d
    @IbrahimYusufu-z9d15 күн бұрын

    Bon Kalindo

  • @NorahMangasanja
    @NorahMangasanja16 күн бұрын

    Mr Dc mumakwana inuyo tilinanu ife amalawi

  • @HaruunWalusa
    @HaruunWalusa15 күн бұрын

    The DC

  • @moseskalande9853
    @moseskalande985315 күн бұрын

    zopanda ntchito zomwe ukulu inu mumalankhula

  • @nafejonga972
    @nafejonga97216 күн бұрын

    Chizagwira zipolopolo😅😅 iwe ndi machine, wait to destroy them with you

  • @EmmanuelNgambi-y6h
    @EmmanuelNgambi-y6h15 күн бұрын

    Umakwana DC

  • @user-zs6qc9dx8s
    @user-zs6qc9dx8s16 күн бұрын

    The DC🔥

  • @user-ql8nf2vb8s
    @user-ql8nf2vb8s16 күн бұрын

    It's plezident of poor people

  • @AustinBornface
    @AustinBornface16 күн бұрын

    The DC!

  • @ArnoldKamanga-r6k
    @ArnoldKamanga-r6k16 күн бұрын

    Uyu yekha timuteteza I swear

  • @PoxisNation-fe1kr
    @PoxisNation-fe1kr15 күн бұрын

    The DC 😂😂😂

  • @OnexAliMwale
    @OnexAliMwale15 күн бұрын

    Kulankhula wina aliyese atha kulankhula koma kuchita zakupsa...Bwana Bon kalindo akumalankhula koma ndi action yanji yomwe ikuchitika? We need kulankhula ndikuchita namaona progress..Mukatiuza zomwe mwapezazo kenako muzinenanso kuti tipanga izi pothana ndizimenezi...tisamangokhalira kumva mwana oopsa mmalankhulidwe, action nothing

  • @myheartforkids2876

    @myheartforkids2876

    15 күн бұрын

    Inu mene mwayankhulamu mwapanga action yanji? Kkkkkkkkkk

  • @sir-wanton-2001

    @sir-wanton-2001

    14 күн бұрын

    Kkkk mbuli ife timakonda DC

  • @OnexAliMwale

    @OnexAliMwale

    14 күн бұрын

    @@myheartforkids2876 Amene amawatsata omenyera ufulawa atha kudziwa kuti nthawi ya Bingu kunali Mavuto Bamusi ndipo amati akanena amapanga action ndipo Mpaka Bingu anasintha machitidwe azinthu zina, nthawi ya Peter kunali Timothy Mtambo, za amenewu mukudziwa zomwe amachita, Koma Bwana Bon mmmm tiyeni tizingomva Mwana oopsa komanso kung'alura kenako tiseke osaona chisintha...I always appreciate for actions not talking that's why tonse Government tikudana nalo coz nawoso kulankhula amatha koma kukwanilitsa kukuwavuta

  • @RedrawLittleMushutula
    @RedrawLittleMushutula15 күн бұрын

    DC mewafika

  • @williamalvis6028
    @williamalvis602816 күн бұрын

    The DC umakwana

  • @phindiswatshibo7101
    @phindiswatshibo710116 күн бұрын

    Chipangoline😂😂

  • @chipanganofackison5185
    @chipanganofackison518516 күн бұрын

    Zamanyi basi kape ndiweyo akanadakhala Ofuna kupha akanampha iweyo umatisokoneka mutu amakutuma ndindani? Umango uwanamizila anthu wosawuka ndidziko lanji lomwe kungapezeke wolemera wose?

  • @musaphiri317

    @musaphiri317

    15 күн бұрын

    Iwe akupasa zingati koma inu ndi onvesachifundo kupusa uchisru

  • @SamKaposa-i5c

    @SamKaposa-i5c

    15 күн бұрын

    Nyau imeneyi itayeni

  • @EvsonNgurube

    @EvsonNgurube

    15 күн бұрын

    Matako ako nyau iwe

  • @sir-wanton-2001

    @sir-wanton-2001

    14 күн бұрын

    Kape uyu

  • @moseskalande9853
    @moseskalande985315 күн бұрын

    Even ur voice doesn't sound like a leader

  • @FrankMulola
    @FrankMulola16 күн бұрын

    😂😂😂😂😂

  • @samhussen708
    @samhussen70816 күн бұрын

    😂😂

  • @brightkaunda920
    @brightkaunda92016 күн бұрын

    Ati amangidwe ndamako

  • @user-uc1pd1tc2x

    @user-uc1pd1tc2x

    16 күн бұрын

    😂😂😂😂😂Amangidwadi ndi amake a Chakwera 😂😂

  • @chifukanyo9447

    @chifukanyo9447

    16 күн бұрын

    😂😂😂

  • @sir-wanton-2001

    @sir-wanton-2001

    14 күн бұрын

    Kkkk