I am a musician,producer and professional sound engineer This woman has changed music in Malawi
@daniellomoliwa7394Ай бұрын
She's not artist accept that fact.. there's someone behind her but that can't be fact to hate her..we must love what she's doing
@PeterNakhutu-tp1ns
Ай бұрын
Uku nde kulankhula..
@AndrewBanda-gk7voАй бұрын
Respect what the old woman is doing guys , paka sindingapite ku show kwa jetu Malawi tusungira anthu opondera love each other , pake zinthu zimativuta kuti zizitiyendera
@EvanceGift-zr1wyАй бұрын
Jetu amatha kungoti kumalawi umbuli umatipweka sitimaziwa kupangana support km kunyoza. I love you Grandma jetu i'm watching you from south Africa capetown
@ajleonard265Ай бұрын
Kuli ambiri kuimba saata koma antu amawakondera moraro basi, ena angomukondera chisoni ndikufuna kumunyoza Joy Nathu, but the fact will remain the same and can not change the song, saatha
@GeofreyCassim-ip1tkАй бұрын
Mayi wapeza chochita, let's congratulate her , mumafuna kt azikupemphani . Muziwalambila omwewo omwe amakupatsani ndalamawo kt muziwachemerela. At that age but she managed to come up with a song , that's great achievement. This is very sad to hear that people who have many followers discouraging someone coz of the age.What a roll model .Mwakhumudwitsa dziko
@user-kr1kg5hy9l2 ай бұрын
Amatha Jetu,am one of her top fan❤️❤️❤️🔥🔥🔥
@user-ie8ed5zm3g
Ай бұрын
Amatha kuyimba kwambiri ndipo ndidolo wa azimai kuposaso makape Inu mukumunyozanu nyimbo zanu sitimazira
@user-zl1xz9kt5s2 ай бұрын
Adani okuda nd mitima yomwe a Malawi podcast akumva pain nd Chakwaza Akakhala oyera kungu lokhayu nde amangofuna achina ujeni aja ampatse chibanzi chikankwana azibudikulisa mma social media mu zaziiii Akhalitse Jetu 💪🔥
@yungdrashmw40512 ай бұрын
Amatha kuyimba kwambili ndipo ndichitsazo chabwino kwa anthu wonse wokalamba kuti wokalambaso alindikuthekela kuzitha zinthu chifukwa tonse ndi anthu wolengedwa kuchokela kwa Mlengi wamakolo anthu Over !!!!!🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
@innocentmausa66432 ай бұрын
Pass my humbly respect to her Manager for doing good example potiwonetsa ndikutiphuzitsa kuti Agogo ndim'dalitso komanso tinayenera tiwasamale ndikuwathokona pantchito yobeleka makolo athu
@innocentmausa66432 ай бұрын
aMalawi timakondwa tikamawona anthu achikulire akutonzedwa kuti ndi mfiti that's Y now tikunyasibwa ndi Jetu but to my side am very grateful to see Jetu being happy,healthy and enjoying lifestyle if U could listen to her when she was saying ine pamoyo Wanga sindiname ndadyapo KFC or Ku Nando's Pano ndikutokoza kubeleka ndikwabwino ,I hope munavapo
@georgechimaliro9908Ай бұрын
She is doing well, let's support her.
@MeclinaKamanga-jp7rmАй бұрын
Amatha Jetu ....asiyeni.asanje a podcast
@MadalitsoBaulenАй бұрын
We are bangweans and being proud of our talented grand ma Jetu
@johnchicotiАй бұрын
Jesus akuyimba bwino moti apitilize luso lake kuti ngati pali Ena okalamba Aliso ndi luso Lina abwele poyela I love ❤ Jetu anthu awo ndi afiti kwawo usawavele
@ChrisChokaniАй бұрын
Amene akuti samatha ameneyu chitsilu kwabasi 😂😂
@user-tt9qz8jd8cАй бұрын
She is the best in what she does no need to compare with others she is being Jetu..... she is being her...
@patriciap.bandah33852 ай бұрын
Anthu inu ndiwomvuta kwabasi, mwini wake anayankhula momveka bwino kuti amasangalala nazo chifukwa sakhalanso akuganiza kuti ndi gogo wamasiye inu ndiye muzichuluka nzeru, kuli oyimba ambirimbiri kunjaku wosatha kuimba koma timakhala tikumvelabe nyimbo zawo ndiye inu yambisani nkhani ina
@GanizaniTime
Ай бұрын
Mmmm mzovuta kwaine saimbadi
@HappyBirchForest-zy8nq2 ай бұрын
Amalawi munazolowera jealousy panya panu pangani zanu zukukanikani zikanakhala kuti ama jealousy mumalandila ndalama mukanalemera koma mulemera mapwala anu
@PrincehrnNgombayela-rq3giАй бұрын
Amalawi tinazolowera kuona agogo mtown mu akupemphetsa ndie jetu pa level yake akuitha let's support her , tikumudikira pa 26 apa kuno ku island kuti azaipatse moto
@user-jk8sh7fh2dАй бұрын
Iiiiiiiii! Amatha jetu ndi gogo wathu ameneyu wa chi malawi, enawo alibe ntima wa chikondi that's why samankonda to me si-kuti ndimazikonda kwenkwen koma zimangondipasa moti ndithakhala kuti kuthekela kwa chuma ndili nako nditha kungonthandiza bsi , posatengela kuti ndimazikonda olo ai why ndi olimbikila kusiyana ndi kumangokhala anapeza zochita jetu bsi let's support her kunyoza si sikungathandize kwa gogoz ngati imenei
@wangat2005Ай бұрын
Jetu emweyo kuti waaaaaaaaaaaaa
@GharmonizeCondeboyАй бұрын
Salute agogo jetu🎉🎉
@pettersen2717Ай бұрын
Akulu inu a man u.nsanje izakuphani ndithu. Kodi inu ndi agogo anu munachitapo zoterezi kupatula pa ufiti agogo anu aja?
@MaureenMugala-yh5pjАй бұрын
Yes Jetu nice woman ad she can sing
@user-ir2yz5zz5xАй бұрын
Jetu kusaizi yake amatha kuimba ndpo nyimbo zake timazifira kwambili
@RachelPhiri-lm6evАй бұрын
vuto amalawi kuphempha salufuna kuvutisa anthu akuchita bwino aliyese akunena za jetu mutu wake kkkkkk mpaseni ulenu
@SolomonwaharryLastoneАй бұрын
The Politics Behind This Is Very Barbaric.Some DJs Are Not Happy Seeing Some Pipo Other Than Them Promoting Singers And Artists. This Is Very Barbaric And Must Stop For The Betterment Of The Arts Industry.
@Doreen-gp6kqАй бұрын
Eya jetu amatha kuyimba pa size yake musiyeni eeeee kambani zina jetu ndi no 1
@EmmanuelNedieАй бұрын
Kodi akamati satha kuimba kodi iwowo ndiomwe anayambisa zoimba .Iwowo ndindani ali ndi mbiri yoyimba
Tiyeni timpatse support Gogo wathuyu, Jetu ndi msangalatsi wathu, kaya kuyankhula kapena kuyimba zonse zili bwino,, Stop compare Jetu ndi Anyamata owimba enawo, Mayi wabwera kudzakhala.
@HugoOrthoCamera-ec7vc
2 ай бұрын
Jetu amatha ndidoro
@user-fs3wc8ue8b
Ай бұрын
Jetu❤❤❤❤❤❤❤❤
@TimothyJere-yb4lzАй бұрын
Jetuu❤❤❤
@FatimaPhirihАй бұрын
Nice woman
@user-hl3st3cc4v2 ай бұрын
Mukunyasidwa gogo kumasangalasa anthu koma kukanakhala kuti ndikutchuka kophudzitsa ana ufiti mukamva nazo kukoma
@ThokoSalim
Ай бұрын
Eead amafuna azmva zot agogo aja akiphunzitsa ana kutamba ndye iwo ku mtima kwao mbeee zkakoma kumayamikla ine chetee pa mbuyo pa jetu
@bmbboymstyles58942 ай бұрын
Ine nd JETU....! 🔥🔥🍒❤
@edwardedo6798Ай бұрын
JETU samatha kuimba ziribe kanthu Bola iye akupanga ndalama and mbiri yake pa Malawi pano iri paliponse, zikumgowapweteka azitsiruwa chifukwa iwowo sakutchuka and they just wanna be famous ponyoza JETU,Iwe ndi ndani? iye ndi JETU, Yomweyo Galu iwe
@taniamanenafavouriteneezam8510Ай бұрын
Jetu she,s the musician by mistake I hope you understand,,,what I saw is,there is someone behind her,she is used to make someone money
@user-bp5po7rt8e2 ай бұрын
Mmmm koma akudawo amalankhula uyipa
@tadalangozo5167Ай бұрын
Adani okuda ndi mtima omwe,, we love jetu 3 sitopu
@user-ck7eb7tb7v
Ай бұрын
tiadani tolimbana ndi magogo aluso😀😀
@user-fp5qn5ci2vАй бұрын
Jetu ndiwoimba basi nsanje basi?
@doublepmw5497Ай бұрын
Jetu ❤❤
@user-gd3jx7tr1p2 ай бұрын
Amatha jetu chabe ndinu anthu ajerous basi
@user-ox8cx8xt6bАй бұрын
Ndipo uyo amati jetu is like a puppet mumuuze pachiphwisi Pake ndipo uyo amati I feel nothing mumuuze pamayake... Agalu anthu oyipa mtima....
@JalasiLucasJalasiАй бұрын
Onse oimba chamba chamapiyano sioimba including boyfriend wa bossladie
@malawimuahmmed59412 ай бұрын
🔥🔥
@ThomsonMusowaАй бұрын
Jetu is one ❤❤❤❤
@kelvinngwira3648Ай бұрын
Sogolo lamuthu Amaliziwa ndi Ambuye.Ngati inu simungapite ku show nde kuti enawo sangapite apita amalawi nsanje basi
@user-bb5iy7ry5h2 ай бұрын
Samatha kuyimba koma ndiwongosangalatsa mtundu wa malawi basi
@MasharPabloАй бұрын
Samatha,vuto amalawi amadana ndi chilungamo basi, iyaaah
@CharlesMillion-bt9suАй бұрын
Jetu amatha
@Hlehle719Ай бұрын
❤❤❤❤❤
@user-rd2td7bg4cАй бұрын
❤❤❤❤adani okuda
@AlexManuelMisomali-sv1vnАй бұрын
Amalawi njiru komanso ufiti
@RachelPhiri-lm6evАй бұрын
ayi mayiwa mbali yawo akuyesesa ndi mmene tsikhu wawo asiyeni ndimmene akupezera ndalama mmalo mophemphapha
@tenexchikumbaАй бұрын
Koma mpaka kuzinza nkhalamba? Koma a Malawi, wina nde akut sangasambe😂😂
@AndrewChabadwa-xl3ffАй бұрын
Jetu umakwana iweyo
@AbdirahmanWllsonkey385Ай бұрын
Amanta kuyimba jetu chifukwA chake timamusiwa
@PatieKatesАй бұрын
Sam malvitha iwe mapwala ako nditu
@BaulenPatisonАй бұрын
Pasikhu wajetu amatha ameneyo Ena ku Malawi Kuno msikhu wakewo amathawa ngakhale kuyakha 4n
Пікірлер: 128
I am a musician,producer and professional sound engineer This woman has changed music in Malawi
She's not artist accept that fact.. there's someone behind her but that can't be fact to hate her..we must love what she's doing
@PeterNakhutu-tp1ns
Ай бұрын
Uku nde kulankhula..
Respect what the old woman is doing guys , paka sindingapite ku show kwa jetu Malawi tusungira anthu opondera love each other , pake zinthu zimativuta kuti zizitiyendera
Jetu amatha kungoti kumalawi umbuli umatipweka sitimaziwa kupangana support km kunyoza. I love you Grandma jetu i'm watching you from south Africa capetown
Kuli ambiri kuimba saata koma antu amawakondera moraro basi, ena angomukondera chisoni ndikufuna kumunyoza Joy Nathu, but the fact will remain the same and can not change the song, saatha
Mayi wapeza chochita, let's congratulate her , mumafuna kt azikupemphani . Muziwalambila omwewo omwe amakupatsani ndalamawo kt muziwachemerela. At that age but she managed to come up with a song , that's great achievement. This is very sad to hear that people who have many followers discouraging someone coz of the age.What a roll model .Mwakhumudwitsa dziko
Amatha Jetu,am one of her top fan❤️❤️❤️🔥🔥🔥
@user-ie8ed5zm3g
Ай бұрын
Amatha kuyimba kwambiri ndipo ndidolo wa azimai kuposaso makape Inu mukumunyozanu nyimbo zanu sitimazira
Adani okuda nd mitima yomwe a Malawi podcast akumva pain nd Chakwaza Akakhala oyera kungu lokhayu nde amangofuna achina ujeni aja ampatse chibanzi chikankwana azibudikulisa mma social media mu zaziiii Akhalitse Jetu 💪🔥
Amatha kuyimba kwambili ndipo ndichitsazo chabwino kwa anthu wonse wokalamba kuti wokalambaso alindikuthekela kuzitha zinthu chifukwa tonse ndi anthu wolengedwa kuchokela kwa Mlengi wamakolo anthu Over !!!!!🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉
Pass my humbly respect to her Manager for doing good example potiwonetsa ndikutiphuzitsa kuti Agogo ndim'dalitso komanso tinayenera tiwasamale ndikuwathokona pantchito yobeleka makolo athu
aMalawi timakondwa tikamawona anthu achikulire akutonzedwa kuti ndi mfiti that's Y now tikunyasibwa ndi Jetu but to my side am very grateful to see Jetu being happy,healthy and enjoying lifestyle if U could listen to her when she was saying ine pamoyo Wanga sindiname ndadyapo KFC or Ku Nando's Pano ndikutokoza kubeleka ndikwabwino ,I hope munavapo
She is doing well, let's support her.
Amatha Jetu ....asiyeni.asanje a podcast
We are bangweans and being proud of our talented grand ma Jetu
Jesus akuyimba bwino moti apitilize luso lake kuti ngati pali Ena okalamba Aliso ndi luso Lina abwele poyela I love ❤ Jetu anthu awo ndi afiti kwawo usawavele
Amene akuti samatha ameneyu chitsilu kwabasi 😂😂
She is the best in what she does no need to compare with others she is being Jetu..... she is being her...
Anthu inu ndiwomvuta kwabasi, mwini wake anayankhula momveka bwino kuti amasangalala nazo chifukwa sakhalanso akuganiza kuti ndi gogo wamasiye inu ndiye muzichuluka nzeru, kuli oyimba ambirimbiri kunjaku wosatha kuimba koma timakhala tikumvelabe nyimbo zawo ndiye inu yambisani nkhani ina
@GanizaniTime
Ай бұрын
Mmmm mzovuta kwaine saimbadi
Amalawi munazolowera jealousy panya panu pangani zanu zukukanikani zikanakhala kuti ama jealousy mumalandila ndalama mukanalemera koma mulemera mapwala anu
Amalawi tinazolowera kuona agogo mtown mu akupemphetsa ndie jetu pa level yake akuitha let's support her , tikumudikira pa 26 apa kuno ku island kuti azaipatse moto
Iiiiiiiii! Amatha jetu ndi gogo wathu ameneyu wa chi malawi, enawo alibe ntima wa chikondi that's why samankonda to me si-kuti ndimazikonda kwenkwen koma zimangondipasa moti ndithakhala kuti kuthekela kwa chuma ndili nako nditha kungonthandiza bsi , posatengela kuti ndimazikonda olo ai why ndi olimbikila kusiyana ndi kumangokhala anapeza zochita jetu bsi let's support her kunyoza si sikungathandize kwa gogoz ngati imenei
Jetu emweyo kuti waaaaaaaaaaaaa
Salute agogo jetu🎉🎉
Akulu inu a man u.nsanje izakuphani ndithu. Kodi inu ndi agogo anu munachitapo zoterezi kupatula pa ufiti agogo anu aja?
Yes Jetu nice woman ad she can sing
Jetu kusaizi yake amatha kuimba ndpo nyimbo zake timazifira kwambili
vuto amalawi kuphempha salufuna kuvutisa anthu akuchita bwino aliyese akunena za jetu mutu wake kkkkkk mpaseni ulenu
The Politics Behind This Is Very Barbaric.Some DJs Are Not Happy Seeing Some Pipo Other Than Them Promoting Singers And Artists. This Is Very Barbaric And Must Stop For The Betterment Of The Arts Industry.
Eya jetu amatha kuyimba pa size yake musiyeni eeeee kambani zina jetu ndi no 1
Kodi akamati satha kuimba kodi iwowo ndiomwe anayambisa zoimba .Iwowo ndindani ali ndi mbiri yoyimba
Jetu amatha akut jetu santha akango nyela basi😅😅 ife akukwan kwabas 🔥
Jetu amatha kuyimba l love you jetu❤
Very nicely
Mupaseni sport osati kumubweza buyo pamene akulakwisa mukhozeni
Jetu akupha sound pa level yake ❤
Amene Ali ndi mpila ndi amene amamakidwa
😂😂😂😂zantiiiii sanje yopanda nzeru kuda biiiiiii
Asiyeni ambc ndikudzikondakwaoko athu ambili akusangalalanaye
kaya amatha kasa satha zanu km ife cape town tikufira
Guyz agogo aja pachilungomo chake samaziwa kunyumba mungowapopa auzeni chilungamo ,amwenewa akunena zoona sikuti akuwada ayi amalawu tatiyeni tiphunzile kunena zoona,olo mayiko oyandikana nawo akutiseka
I love Jetu
Jetu ndi 1❤❤❤❤❤
JetuNo 1❤
Onyoza getu azipanga zake
Anthu muli ndi nsange mpaka eeeee anyamata chitani manyazi live here alone yilipambuyo pa jetu
Amalawi sanje sipindula wokalamba amene alindikuthekela apange zinthu zoti akhoza kuthandizika pa moyowake kodi amalawi mumafuna wokalamba opephapempha?
Ine l love jetu
Chokani amalawi oyipa inu amalawi asanje inu musiyeni jetu aziyimba ndipo akuyimbabwino ndithu komaso anyamataake awo akuvinabwino ndithu Vuto amalawi sanje imakuvutandi ndithu iya mbori zanu.ndithu
Agogowo alimbikiseni pa size yawo amatha amene mumanyoza ndichifukwa chake si ndinu Jetu . Inu ndi inu Jetu ndi Jetu ngati kuwona kuti sakufika mlingo wanu pitilizani kuchokela pamathela Jetupo.
Kuteloko athu Ngati awawa mulungu aziwakhululukila chifukwa ndichiwanda chikwapangisa Kuti ayakhule momunyoza jetu ndichimodzi modzi mmene Alili agogo awo iwoso Ngati alinawo agogo awapangile chochita mulekeni mumuone kumene athele osati zomusisila pas ayiiiiiiiiii ziwanda zaathu inu ofunika tikuyitanilen amulelemba akuphepheleleni amulelemba 🗣️🗣️🗣️ mulikuti pephelelani ziwanda zaathuzoo
Tiyeni timpatse support Gogo wathuyu, Jetu ndi msangalatsi wathu, kaya kuyankhula kapena kuyimba zonse zili bwino,, Stop compare Jetu ndi Anyamata owimba enawo, Mayi wabwera kudzakhala.
@HugoOrthoCamera-ec7vc
2 ай бұрын
Jetu amatha ndidoro
@user-fs3wc8ue8b
Ай бұрын
Jetu❤❤❤❤❤❤❤❤
Jetuu❤❤❤
Nice woman
Mukunyasidwa gogo kumasangalasa anthu koma kukanakhala kuti ndikutchuka kophudzitsa ana ufiti mukamva nazo kukoma
@ThokoSalim
Ай бұрын
Eead amafuna azmva zot agogo aja akiphunzitsa ana kutamba ndye iwo ku mtima kwao mbeee zkakoma kumayamikla ine chetee pa mbuyo pa jetu
Ine nd JETU....! 🔥🔥🍒❤
JETU samatha kuimba ziribe kanthu Bola iye akupanga ndalama and mbiri yake pa Malawi pano iri paliponse, zikumgowapweteka azitsiruwa chifukwa iwowo sakutchuka and they just wanna be famous ponyoza JETU,Iwe ndi ndani? iye ndi JETU, Yomweyo Galu iwe
Jetu she,s the musician by mistake I hope you understand,,,what I saw is,there is someone behind her,she is used to make someone money
Mmmm koma akudawo amalankhula uyipa
Adani okuda ndi mtima omwe,, we love jetu 3 sitopu
@user-ck7eb7tb7v
Ай бұрын
tiadani tolimbana ndi magogo aluso😀😀
Jetu ndiwoimba basi nsanje basi?
Jetu ❤❤
Amatha jetu chabe ndinu anthu ajerous basi
Ndipo uyo amati jetu is like a puppet mumuuze pachiphwisi Pake ndipo uyo amati I feel nothing mumuuze pamayake... Agalu anthu oyipa mtima....
Onse oimba chamba chamapiyano sioimba including boyfriend wa bossladie
🔥🔥
Jetu is one ❤❤❤❤
Sogolo lamuthu Amaliziwa ndi Ambuye.Ngati inu simungapite ku show nde kuti enawo sangapite apita amalawi nsanje basi
Samatha kuyimba koma ndiwongosangalatsa mtundu wa malawi basi
Samatha,vuto amalawi amadana ndi chilungamo basi, iyaaah
Jetu amatha
❤❤❤❤❤
❤❤❤❤adani okuda
Amalawi njiru komanso ufiti
ayi mayiwa mbali yawo akuyesesa ndi mmene tsikhu wawo asiyeni ndimmene akupezera ndalama mmalo mophemphapha
Koma mpaka kuzinza nkhalamba? Koma a Malawi, wina nde akut sangasambe😂😂
Jetu umakwana iweyo
Amanta kuyimba jetu chifukwA chake timamusiwa
Sam malvitha iwe mapwala ako nditu
Pasikhu wajetu amatha ameneyo Ena ku Malawi Kuno msikhu wakewo amathawa ngakhale kuyakha 4n
amalawi kungozelera chilichonse ndale agogo ndiwabwino akakhala kuti ndi ambuyanu mukanatani mukumbukire paja inunso kuti mufike pamenepo ndi anthu anakupanga push tidzipuzizira kutukulana tokha tokha, anathu oipa
Akuimba bwino kwambiri apitilize lunso lake osamukhomelera ayi iiii Amalawinso aaa
Komano to be honest amayiwa kuyimba amatha,kumalawi kuno kulinkhalamba zambiri koma ndinkhalamba zingati zingakwanitse kuyimba olo atazipanga managing?
Pajatu aliyese akupanga zomusangalatsa nde musiyeni jetu
Nyimbo za gogo yu ine sinamvereko chifukwa sindimazikonda ka palibe cha nzeru chomwe sindimachiona ata
Amatha kuimba ,akunyozao makolo awo angaimbe chomchi
Palibe chanzeru apa
Kaduka msanje zagokula bas
Jetu alibho heavy achina joy ndi awa a Malawi podcast ma views awo sangapose Jetu 😂😂
Adani okuda ngati ntchende lakumamzere
Nd dolo kwambili zed jetu
Ineso amandibowa😩
Zaboza alibho
Jetu akuyimba Koma athu jerasi apitilizeeeee
Aliye ali ndi nthawi yake
zisiluu za anthuu zimenezoooo
Jetu alibho kwambili
Getu ndi dolo kusiyana ndi gidezi pano kuli piano angamamvele za chigogo ndini anthu nsanje izakuphani
Ndizonadi sikuzuza iyayi Pali ndalama osati ulesi tiyenayo jutu bane ikhoza kukhala Sanje
Makape awa ngakhaleso ndalama zomwe wapeza jetu iwo alibe
I think joy is jelous