AMENE ALOWE M'MALO MWA ACHILIMA KU UTM/ NKHANI

Пікірлер: 58

  • @BestonMakochera-qk4sz
    @BestonMakochera-qk4sz12 күн бұрын

    UTM president Tikufuna brian banda wisy man

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i11 күн бұрын

    Chakwela asowe fiti yothelatu UTM ganizani mofasa musakonde ndalama kumbukani tsogoleli wanu chilima upangili omwe analinawo sitikufuna kuti kupita kwachilima ndizinalake lithe ayi mukuziwabwino zomwe amafuna chilima still I remember S K C ambuye sungani mizimuyawo 😭😭😭💔💔💔

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d12 күн бұрын

    Chakwera pamtumbo pakę anaba ndalama za fertilizer asamatipusitse azipusitsa zitsiru zake zomwezo

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q12 күн бұрын

    Malawi is lacking good leadership that's why is the poorest country in the world.

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r8 күн бұрын

    Chakwela satana wohipa ziko lamu nyeraaa

  • @user-xu9rh1lm8o
    @user-xu9rh1lm8o12 күн бұрын

    Asamango namidzila covid19

  • @WestonGawaza
    @WestonGawaza12 күн бұрын

    UTM,mapulezident awa mayi chirima, mwana wachilima , Brayani Banda UTM awa ndi mapulesident a malawi, mukawasiya awa chipani chapita ndimazi, kongo kabira analowa ali ndi 31 years mundinkhulupirire , yeremiya, davidi, anali ana kaliyati ankhale muzati wa UTM, BY BY

  • @saadisadie3125

    @saadisadie3125

    11 күн бұрын

    Ayi kabira analowa Ali ndi28

  • @DanielVictor-pi5fj
    @DanielVictor-pi5fj12 күн бұрын

    Tikufuna Timothy mtambo

  • @sharifujoe7633
    @sharifujoe763311 күн бұрын

    Fredo yomweyo

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r8 күн бұрын

    Chakwela mbuzi yamuthu

  • @kubengovender6996
    @kubengovender699612 күн бұрын

    Big up brother man!!

  • @TiyanjaneLuka-e2l
    @TiyanjaneLuka-e2l9 күн бұрын

    😢😢😢😢Hey

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace32112 күн бұрын

    Am still worried about Chilima, Chakwela Anapaga Zolakwa Kwambili, Sangamuphe Munthu Chonchija

  • @user-qp8kh2hj9o

    @user-qp8kh2hj9o

    12 күн бұрын

    Kwambiri ndipo ine zimandiwawa mpaka lero pano bwenzi chilima atatiyankhula zokhuza comvension imeneyi hmm😢

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf12 күн бұрын

    chakwera asanamizire zimenezo chakwera ndi chitsiru chamunthu chigawenga

  • @user-jn2oc3cn3q
    @user-jn2oc3cn3q10 күн бұрын

    Mwakweza ferteleza tsopano mukuti tizigwilitsa ntchito manyowa ayi zikomo Bola la chakwera

  • @goodwilljeza8419
    @goodwilljeza841912 күн бұрын

    Adah iweyo Bass limenero bwanji Koma?????

  • @user-ii2sh1mz3r
    @user-ii2sh1mz3r12 күн бұрын

    President Chakwera akanabwera ndi chipani china osati MCP , nichifukwa chake mbiri yakale ya MCP ikumukhuza, but instead of kutukwana a president let us pray for our country, kutukwana sikusintha zinthu guys,

  • @MisheckNtanbalika
    @MisheckNtanbalika12 күн бұрын

    Mukufuna kt azaimile chifukwa mukuziwa kt Ali ndi mphavu xokupha aliyese odana ndichipanichi

  • @brainsmkumbwa6267
    @brainsmkumbwa626712 күн бұрын

    Wathamanga kukasiya ma pepela opikisana nawo pa udindo wapulezidenti chifukwa akudziwa kuti munthu yekhayo amene akanalimba mtima kuti apikisane naye wamupha kale (Chilima)changucho sichina koma kusangalala

  • @user-sd3cl2dq7v
    @user-sd3cl2dq7v11 күн бұрын

    Mwalephera kuyendetsa boma osanyengezela COVID 19

  • @marryphili5419
    @marryphili541911 күн бұрын

    Covid 19 mupaka liti bwanji simukufuna kuvomereza kuti mwalemphera

  • @user-sd3cl2dq7v
    @user-sd3cl2dq7v11 күн бұрын

    Mwalephera osanyeng ezela COVID 19

  • @user-co3wr3rn4h
    @user-co3wr3rn4h11 күн бұрын

    Chakwela akangokhala pamupando basi mcp yathela pomwepo ndithu galu uyo wakupha achoke

  • @MisheckNtanbalika
    @MisheckNtanbalika12 күн бұрын

    Komas osamanena kt covid 19 wasokoneza kd matendawo anagwela ife tokha komwe zinayambilako zithu zikuyenda bwanji

  • @MkandawireKennedye
    @MkandawireKennedye12 күн бұрын

    Zaboza zimenezo kugwa kwa kwacha nanga. Zautsilu bas

  • @allansili-rc9gc
    @allansili-rc9gc11 күн бұрын

    Covid 19 mpaka liti kod akuba inu

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi11 күн бұрын

    Hahaha covid

  • @user-kg5lf6bd1g
    @user-kg5lf6bd1g12 күн бұрын

    Patumbo pake chakweyo nyelo wake

  • @user-ti8ds7iq8z
    @user-ti8ds7iq8z12 күн бұрын

    Mmene anayambila za covid Muja mpaka liti

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe395812 күн бұрын

    Pongopha Chilima uja basi, Chakwera waluza, Chakwera must go

  • @user-em1qi8kj9h
    @user-em1qi8kj9h12 күн бұрын

    Inu mudzikhala ndi manyazi ponena za covid....palibe anthu opasa manyazi ngati inu every statement of economics development....koma mukafuna Kuba ndalamazo Palibe za covid anthu onyansa mitima

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y12 күн бұрын

    MCP ndiyakupha

  • @user-nb8wg3fh4u
    @user-nb8wg3fh4u12 күн бұрын

    Patumbo pako chakwela

  • @user-yq1mc3nm1f
    @user-yq1mc3nm1f12 күн бұрын

    Utm uchitsiru mmmm

  • @HarryKandani
    @HarryKandani12 күн бұрын

    Blaming covid 19 mpaka pano? Abusa aku bagamoyo alibe nzeru za usogoleri

  • @phillipphiri2119
    @phillipphiri21199 күн бұрын

    Next time go straight to the point,Tizionera Zama parish Mmalo mwa za UTM

  • @WestonGawaza
    @WestonGawaza12 күн бұрын

    UTM BALIBE MUGWILIZANO MAONA NONKHA AYIMASO AZANU AJA MAYI CHIRIMA KAPENA MWANA WACHIRIMA AYIME AMENE AGWILE NCHITO NDINU MAMUZUNGULILA KABILA 31 ANALOWA UPULESIDENT MUWINO MUSAKAYIKE MUKAPHONYA APO BRAYANI BANDA, MUKASIYA AWA CHIPANI MALUZA.

  • @user-ti9yk4eg2l

    @user-ti9yk4eg2l

    11 күн бұрын

    Mayi chilima ayime basi atha kuwina

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi12 күн бұрын

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣

  • @user-kg5lf6bd1g
    @user-kg5lf6bd1g12 күн бұрын

    Mapwala abambo ake chakwelayo

  • @user-fh3dn8kt2j
    @user-fh3dn8kt2j12 күн бұрын

    MCP moto kuti buu patsogolo ndi Chakwera olo mutukwane zopanda phindu izo mutopa nokha

  • @user-ww9rj2wx8d

    @user-ww9rj2wx8d

    12 күн бұрын

    Za ziiiii basi

  • @user-vh3gq2tp2l

    @user-vh3gq2tp2l

    12 күн бұрын

    Misala etiii

  • @user-fh3dn8kt2j

    @user-fh3dn8kt2j

    12 күн бұрын

    Mukhaulatu inuyo ndipo simunatiii MCP mpakampaka

  • @vinceynyone6693
    @vinceynyone669312 күн бұрын

    I wish Timothy Ntambo alowe UTM party to mlowamumalo a later president SCK

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h12 күн бұрын

    Kkkkkk koma MCP kovid Wake uti shame on you anthu adayamba bwino kuvala buluku ndiye abwelerenso kupampaz 😂😂 you are not serious bullshit

  • @user-oq5rg5mz7q
    @user-oq5rg5mz7q12 күн бұрын

    A MCP chimene chikwalimbitsa mtima ndichani?

  • @brainsmkumbwa6267

    @brainsmkumbwa6267

    12 күн бұрын

    M.C.P kudzungulira mutu ndikuzabela ma vote ndi zimene zikuwalimbitsa mtima

  • @user-xx4jb9se3z

    @user-xx4jb9se3z

    12 күн бұрын

    Kkķkk kupha kuba ndi nkhaza bro zomwe zikuwalimbitsa kulimba mtima ndipo mcp sidzawinanso

  • @user-xx4jb9se3z

    @user-xx4jb9se3z

    12 күн бұрын

    Kkķkk kupha kuba ndi nkhaza bro zomwe zikuwalimbitsa kulimba mtima ndipo mcp sidzawinanso

  • @EllahChikwatu

    @EllahChikwatu

    12 күн бұрын

    Ndpo inu zikudabwisatu

  • @user-xx4jb9se3z

    @user-xx4jb9se3z

    12 күн бұрын

    2025 ambuye MULUNGU akukasesa ku state house

  • @GodisoneNoel
    @GodisoneNoel11 күн бұрын

    Kovidi inali ku malawi kokha katangale ndi amenewakura mboma

Келесі