That's good l dea God be with you we love you pangani gwilidzano Ife tili pa mbuyo Pano
@chrispinechirwa2655Ай бұрын
Vyakuyoghoya vya mtambo ni boza lekha😢😢
@LuwisKaigwaze-gr6cgАй бұрын
Musayembekeze kuti mudzalamulira dziko lino aford
@WatipaCawingaАй бұрын
Magufuli wathu kupoto
@user-qp8kh2hj9oАй бұрын
Alliance tapanga kale ndi UDF musavutike ❤❤❤❤
@marthaphiri3600Ай бұрын
Join hands with all the opposition parties, gawani mipando molingana campaign wisely win 2025.
@user-qp8kh2hj9oАй бұрын
Utm & UDF Boma 2025 ❤❤❤❤❤❤❤❤
@johnussenu2848Ай бұрын
Utm and udf boma
@YasinMusa-ym8lpАй бұрын
Bomo ylo ❤
@IshmailDukuturuАй бұрын
Mbuzi iyi Timothy
@chrisboyce2Ай бұрын
UTM ikuyenera ibwerele ku DPP ndipo Ife angoni a ku Ntcheu tili ready kudzawavotera DPP Pamodzi ndi UTM ngati alliance
@KikaImran
Ай бұрын
You re very right. Sindinavoteko and if DPP coraborate with UTM i ll vote for them though am 100% sure that andale ndi oipa onse, they re there for their empty bellies
@user-hh4wn4vf9eАй бұрын
Amen 🙏
@jamessoko9480Ай бұрын
Aaaaaaa....,ndimo mukuyowoyela mwa wandyale. Pa mupando khale waka,kujikuzga kwake uko,mwaluwa ivyo mukapangana.
@actuarialscience2283Ай бұрын
Chihana is my vote
@JumaGadaffАй бұрын
Mulungu wamakamu kanthani onse omwe adzunza nzimu wa skc lest in peace ndipo chauta langani ndithu
Aford akuwona kuti ku UTM kulibe utsogoleri komabe sizingatheke chifukwa a Aford akufuna mpando and UTM nayo yikufina mpando 🤣🤣🤣🤣
@user-qp8kh2hj9o
Ай бұрын
Ife tapanga kale ndi UDF musavutike 😂😂😂😂😂
@SyakinongwaАй бұрын
Team up and cartel leadership positions within your team. Otherwise forget individual-party leadership as there is no way you can beat MACOPA.
@yassinn5634Ай бұрын
Chipani cha UTM chija ayamba kuchikanganirana. Chizungu chake SCRAMBLE FOR UTM. Ena apita kwa Aford, DPP ndipo ena atsala ku MCP. Thats my opinion. You got yours take it or leave it.
@emmanuelsambo1158Ай бұрын
It was only SKC
@user-jn9tz3li3vАй бұрын
Mtambo mpaka kumuziwa Mulungu kkkkkkkkk ndale ndizovuta
@BestonChagalaАй бұрын
Koma a Enock muchenjere ndi mtambo,mugawana zida 2025 isanafike chifukwa aliyense akuyankhula ngati ndi president payekha.Nanga mmene akuyankhulira mtambomo akuyankhula ngati vice president wa chipani ngati?Akudziwa kuti kupatula Ku hrdc sangayambitsenso gulu lina lotchuka paokha,nchifukwa chake asankha AFORD.Akuti safuna mpando chonsecho amayankhula ndi zodiak kuti afuna Udindo ngati platform yoti adzikhala influential
@user-wk7ut7ld1xАй бұрын
Mtambo you are Malawian julias malema and your party aford you get 9% of the votes that is my prediction
@BrightNyoni-yd4ipАй бұрын
Mumakwana a hot 265 watching you from lusaka Zambia twatotela sana
@PangolinimwАй бұрын
🫡🫡🫡🫡🫡🫡
@BestonChagalaАй бұрын
Regionalism inamkanika chihana ,you can't win the national presidency without people from other regions.Nthawi zina musanayankhula mudzikhala Kaye pansi nkuuzana kuti kodi izi ndizoyenera kudziyankhula pagulu?Mukuti unduna simukuufuna chonsecho mukudziwa kale kuti simungadzawine u president wa 2025.Ngqkhale iwe mtambo pa ticket ya AFORD sungawine kuchitipa u mp ,nthawi imene munali nduna palibe chomwe munawathandidza anthu aku chitipa
@HappyAntenna-sf9qxАй бұрын
iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela
@user-im7sc2my4wАй бұрын
I don't trust NTAMBO ,NTambo vuto nngosamudalila Komanso nkovuta kumukhulupilila uyu . Ife aMalawi mukanakhala Ngati Bingu ,mmali ndi munthu wosavuta ,kungomupangila njira ya chakudya basi ,President ameneyo adzakhala WA muyaya. Ngati dziko Lili ndi chakudya ,ma business amayenda BWINO .Koma aaaaa uyuyu ayi mwina
@actuarialscience2283
Ай бұрын
Ngakhale banja limayenda bwino ngati chakudya chikupezeka. Zovala ndi zina zimaphweka kugula.
@MercyNkhoma-b6hАй бұрын
Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk
@samdiverson9733Ай бұрын
Kkkkk mtambo sungatunamize adah ndife a utm we are together with DPP
@spargomw
Ай бұрын
I agree with you 100%❤❤
@MercyNkhoma-b6hАй бұрын
Koma chaka chino ziliko ndithu.
@BestonChagalaАй бұрын
Vuto ndiloti ena pa imfa ya chilima afuna kutchukirapo.Aford yakhala zaka 30 but no progress koma pano they are claiming to be friends of chilima just to capitalise on the direction less supporters of utm.Ku AFORD kuli ndani odziwa ndale kuposa kaliati?And in terms of popularity utm ili pa mwamba kwambiri kuyerekeza ndi AFORD
@chrispinechirwa2655Ай бұрын
Ili ni lirombo yayi 😂😂😂😂
@VungaQueen
Ай бұрын
Kkkk😂😂😂😂😂
@MosesNyalugwe-ll8hhАй бұрын
Maloto achumba
@chrisgremu740Ай бұрын
Ndiye Chakwera akawinaso 2025 Mutani?
@petertaulo8014
Ай бұрын
Sangawine mark my words
@TiyesNayumaАй бұрын
Chitsilu iweyo you failed as a minister
@user-eh1gn1nj9dАй бұрын
Kodi imfa ya Chilima mukupangira campaign Mulungu akukanthani ndithu
@HappyAntenna-sf9qxАй бұрын
iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela
@MercyNkhoma-b6hАй бұрын
Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk
Пікірлер: 66
Amen 🙏 mawu amphavu Mulungu akutetezeleni azitsogoleli amene mukuimila a Malawi osaopa Mulungu alinafe
@BlessigsChabzola
Ай бұрын
😊09
MTAMBO kakhaleni kunyumba...tinatopa nanu.AFORD SIYINGAWINE MWANA WAWUPANDU IWE..UMVE ZIMENEZI KOMWE ULIKO
@jameshuwanzulu
Ай бұрын
ubwino wake simukavota nokha
@user-fl6zc5gz5r
29 күн бұрын
Ndilibe lawyer mkanakuyankha
Utm udf my vote
That's good l dea God be with you we love you pangani gwilidzano Ife tili pa mbuyo Pano
Vyakuyoghoya vya mtambo ni boza lekha😢😢
Musayembekeze kuti mudzalamulira dziko lino aford
Magufuli wathu kupoto
Alliance tapanga kale ndi UDF musavutike ❤❤❤❤
Join hands with all the opposition parties, gawani mipando molingana campaign wisely win 2025.
Utm & UDF Boma 2025 ❤❤❤❤❤❤❤❤
Utm and udf boma
Bomo ylo ❤
Mbuzi iyi Timothy
UTM ikuyenera ibwerele ku DPP ndipo Ife angoni a ku Ntcheu tili ready kudzawavotera DPP Pamodzi ndi UTM ngati alliance
@KikaImran
Ай бұрын
You re very right. Sindinavoteko and if DPP coraborate with UTM i ll vote for them though am 100% sure that andale ndi oipa onse, they re there for their empty bellies
Amen 🙏
Aaaaaaa....,ndimo mukuyowoyela mwa wandyale. Pa mupando khale waka,kujikuzga kwake uko,mwaluwa ivyo mukapangana.
Chihana is my vote
Mulungu wamakamu kanthani onse omwe adzunza nzimu wa skc lest in peace ndipo chauta langani ndithu
MuKufuna alliance mukuopa chani
Munthu oyipisitsa mtima Timothy sitingakumvere
Wabodz uyu Mumater mukamafun mavot Mumakhal ngat anthabwino Chilimanso amater Chakweranso amater
Iwe Mtambo leka bodza unatiputsitsa padzana kulankhula ngt zamzeru kma sitingakhulupilire munthu ngt iwe
Yambani zomwe mukunenazo musanalowe muboma ,kenako Anthu adzakhulupilila Kuti mukufuna kutukula dziko. Anthu Andale inu mumangotizunza,Anthu wovota kumabvutika inu Ana anu akuphunzila kunja
Join
Mtambo NDI MBUZI...mavuto alipo panowa,anyani akulamulira panowa..mesa anawathandizila kukhala pampando ndi iyeyo😂😂
Tiyeni tikavote mwanzeru mcp must go.
My vote afod
Zimenezo2 zithera konko mwene
Mtambo ndikhuluku...u minister unamurephera
I hope if all mupoto must vote for AFORD
@yassinn5634
Ай бұрын
Mtamboyu akunena zoona nthawi Chihana Senior UDF imamunyengerera chifukwa Chihana anali ndi MP ambiri anali ndi mphamvu koma chifukwa chakugawanikana alibenso mphamvu
Timothy sangatinamize for the second time.....
Move
Komatu mtambo munthawi ino ukanankhala chete kaye munalumbwa kwabili nthawi inja ife kukopeka nanu lero munagopita kukamuphetsako chilima inu kumabwerako ndiye muliena nthawi inoyo mukanadenkha kuyamba kulingalira pazomwe munachita aaa
Aford akuwona kuti ku UTM kulibe utsogoleri komabe sizingatheke chifukwa a Aford akufuna mpando and UTM nayo yikufina mpando 🤣🤣🤣🤣
@user-qp8kh2hj9o
Ай бұрын
Ife tapanga kale ndi UDF musavutike 😂😂😂😂😂
Team up and cartel leadership positions within your team. Otherwise forget individual-party leadership as there is no way you can beat MACOPA.
Chipani cha UTM chija ayamba kuchikanganirana. Chizungu chake SCRAMBLE FOR UTM. Ena apita kwa Aford, DPP ndipo ena atsala ku MCP. Thats my opinion. You got yours take it or leave it.
It was only SKC
Mtambo mpaka kumuziwa Mulungu kkkkkkkkk ndale ndizovuta
Koma a Enock muchenjere ndi mtambo,mugawana zida 2025 isanafike chifukwa aliyense akuyankhula ngati ndi president payekha.Nanga mmene akuyankhulira mtambomo akuyankhula ngati vice president wa chipani ngati?Akudziwa kuti kupatula Ku hrdc sangayambitsenso gulu lina lotchuka paokha,nchifukwa chake asankha AFORD.Akuti safuna mpando chonsecho amayankhula ndi zodiak kuti afuna Udindo ngati platform yoti adzikhala influential
Mtambo you are Malawian julias malema and your party aford you get 9% of the votes that is my prediction
Mumakwana a hot 265 watching you from lusaka Zambia twatotela sana
🫡🫡🫡🫡🫡🫡
Regionalism inamkanika chihana ,you can't win the national presidency without people from other regions.Nthawi zina musanayankhula mudzikhala Kaye pansi nkuuzana kuti kodi izi ndizoyenera kudziyankhula pagulu?Mukuti unduna simukuufuna chonsecho mukudziwa kale kuti simungadzawine u president wa 2025.Ngqkhale iwe mtambo pa ticket ya AFORD sungawine kuchitipa u mp ,nthawi imene munali nduna palibe chomwe munawathandidza anthu aku chitipa
iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela
I don't trust NTAMBO ,NTambo vuto nngosamudalila Komanso nkovuta kumukhulupilila uyu . Ife aMalawi mukanakhala Ngati Bingu ,mmali ndi munthu wosavuta ,kungomupangila njira ya chakudya basi ,President ameneyo adzakhala WA muyaya. Ngati dziko Lili ndi chakudya ,ma business amayenda BWINO .Koma aaaaa uyuyu ayi mwina
@actuarialscience2283
Ай бұрын
Ngakhale banja limayenda bwino ngati chakudya chikupezeka. Zovala ndi zina zimaphweka kugula.
Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk
Kkkkk mtambo sungatunamize adah ndife a utm we are together with DPP
@spargomw
Ай бұрын
I agree with you 100%❤❤
Koma chaka chino ziliko ndithu.
Vuto ndiloti ena pa imfa ya chilima afuna kutchukirapo.Aford yakhala zaka 30 but no progress koma pano they are claiming to be friends of chilima just to capitalise on the direction less supporters of utm.Ku AFORD kuli ndani odziwa ndale kuposa kaliati?And in terms of popularity utm ili pa mwamba kwambiri kuyerekeza ndi AFORD
Ili ni lirombo yayi 😂😂😂😂
@VungaQueen
Ай бұрын
Kkkk😂😂😂😂😂
Maloto achumba
Ndiye Chakwera akawinaso 2025 Mutani?
@petertaulo8014
Ай бұрын
Sangawine mark my words
Chitsilu iweyo you failed as a minister
Kodi imfa ya Chilima mukupangira campaign Mulungu akukanthani ndithu
iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela
Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk