Afford yati siyokondwa ndi zochitika za Mkasa Chifukwa cha Nyimbo iyi.
Жүктеу.....
Пікірлер: 224
@ThomasSibale-dx6bg2 күн бұрын
Mumakwana amphungu Joseph I like your songs
@user-uc1pd1tc2xАй бұрын
Big up Nkasa umaimba zoona zokhazokha zounikira anthu❤❤❤❤❤ APM pachiongolero basi wina afune ❤❤❤
@patrickzembani4315Ай бұрын
❤❤❤❤❤❤❤ very powerful mr favourite Mkasa💪💪
@user-ri8em6my2eАй бұрын
Kung'alura kung'alura basi mkasa wabwera ngati coming ADad My vote 🔥🔥
@geofreydzinyemba6107Ай бұрын
Good song Mr nkasa keep it
@GiftFredohАй бұрын
Ndakwela yomweyo ankasa mumakwana inuyo ❤❤❤
@OjessAndisoni
26 күн бұрын
Mumakwana.ambuye nkasa
@SirpromiseMatabwa15 күн бұрын
🎉🎉🎉 respect mkasa
@chrismezalumo56986 күн бұрын
Mr Nkasa deserve a degree of honor Dr Nkasa on his musical journey which which sheds a light to those who are in the darkness
@Thewarrior70938 күн бұрын
What a beautiful song it is. Agalu a mcp munya muona
@LysonMtalika-tb6fkАй бұрын
Big up Nkasa kuswakuswa, chilungamo kuyenda ngati madzi 🔥🔥🔥🔥
@BittonRashid4 күн бұрын
Kuyankhula mudayamba kale Mr mkasa ndife osanva achina tione zina koma zoonazi tizaona nazo mkamwa mwankango mcp izipita abale anga kuba kwanyanya.
@warrenmwambazi834213 күн бұрын
Nice tune 😊
@user-fr9ss6lc2t27 күн бұрын
Nyimbo yabwino heavy. Munthu ukachemelera chinthu chabwno zimachita kukoma chonchi
@agreementphiri5416Ай бұрын
This guy is good always. Don’t be jealous of him please. Nkasa,💪💪
@lucianojames7555Ай бұрын
Inuyo ndi akatundu Ulemu Wanu Mr mkasa keep it up wina aphulika ndithu 😂😂
@user-qg4it7my9nАй бұрын
i love this song watching from cape town
@user-pd4ru7sg2s14 күн бұрын
Dolo kmb namiyambi sopano m'bwalo. God give you a long live
@LacksonChikho-ow5kwАй бұрын
Big up mr nkasa
@AmandaConstance-fx8crАй бұрын
Amen 🙏 🙏 🙏 Nice song
@BhekiMavundla-po2bqАй бұрын
Mkasa eish! ndikatundu omanga ndimawaya/mashini,mfundo pamaimbidwe ake palibenso,uyu ndi dolo woganiza bhoo heavy kkk ❤❤❤
@user-fx4pp2xt7gАй бұрын
Nice song Dpp my vote 🗳
@HannaAsima-t4f15 күн бұрын
Wow 😍 that's great advice
@frezarphiri3480Ай бұрын
Koma mkasa machine 😂😂
@chakakachaka-man26 күн бұрын
More fire 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
@abdullalajabu5871Ай бұрын
inuyo ndi big basi mbambande akuti olo kuyifusa mizimu ikanakana kuti tambala wakuda asabweleso 💪💪💪😅😅😅
@fredsemu7136Ай бұрын
This is prophetic song
@MustafaHenderson25 күн бұрын
Mkasa keep it up singing trye
@vitumbikokamanga5869Ай бұрын
Nkasa ndi machine ❤❤❤❤
@user-ik5sz8hc6f8 күн бұрын
Sangakondweletse onse.Ndibwino amuleke chifukwa nayenso mpomwe akupezela mchere wake
@johnbakali278 күн бұрын
Chipani chantendele on repeat 🎉😂😅❤
@TiongeChirwa-kz1ubАй бұрын
DPpppppppppp woyeeee ❤❤❤❤❤❤
@jonathanmbewe4246Ай бұрын
Nkasa always unpredictable osamukhulupilila
@wilisonbornface4282Ай бұрын
Nice song
@KennedyPhiri-h9h9 күн бұрын
Nkansa sawopa naye tili kumbuyo kwako masa we still remember azibale athu anaphedwa ndi mcp zaka zambuyomu sitilora kuti mcp izawinenso 2025 never
@Henry-vw2czАй бұрын
Nice one ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
@blessingsnyalo-rp9ko9 күн бұрын
Nyimbo yamphanvu kwambiri moto kuti buuuuuuuuuuuuuu 🔥 🔥
@ZekezekeNjalaАй бұрын
Odana ndi nyimbo iyi usiku amawuluka ndithu nkasa never give up
@JohnmarkNazombe-hi9xd
Ай бұрын
😂😂
@JohnKanjete3 күн бұрын
Uyu wangonena zabwinozo basi ndipo palibe vuto apaaa😂😂
@user-ji4xn6me8dАй бұрын
Amatha uyu siza a Lucius Banda ai
@blessingsnyalo-rp9ko
9 күн бұрын
Ndipo live
@gibbohtrust611824 күн бұрын
Ameneyu sazatheka
@user-oz1ts3yi7dАй бұрын
Nkasa youre number one 🎉🎉
@PaulBanda-wm2kqАй бұрын
Ndine zambian ❤ndimati ndingofunsa AFFORD ndi chanico🙏🙏
@chekiamaabdul5083
Ай бұрын
Afford ndi chiwelesye cha achakorwa nivipuwa wanvela ka iwe chifukala
@PrinceKachimanga
Ай бұрын
they want to.get back in power
@petermanMitambo14 күн бұрын
Nichikali ichi panyimbo kkkk long live phungu Joseph mkasa
@samdiverson9733Ай бұрын
Apa ndiye wabwera mkasa umasiya kuti nyimbo ngati izizizi
@samdiverson9733Ай бұрын
Apm ikulowa Malawi wafikapa sakufuna azitsogoleri a try and error apm only hope for Malawians
@MarvellousTech-kz6no
Ай бұрын
Uyu ndiye mkasa amene ndimamudziwa ine , na pankhani yoyimba , amathira mbalume, adzaima naye ndindani , !
@Okalekale
Ай бұрын
Anapanga chani uyu?,Bingu yekha,awa ndimanyaka palibe chimene anapanga.Chiyambire cha democracy munthu anapanga zooneka ndi Bingu yekha,zinazi ndimbava zokha-zokha,dziko la Malawi linapita ndi Kamuzu ndi Bingu.Nkasa waona kuti chifukwa anthu akuganiza kuti Chakwera wapha Chilima ndiye kuti DPP idzawinaso wayamba kale kuseteka matako a Peter,opportunist iwe ndale za pa Malawi mwazilowetsa umbuli kwambiri,dzikoli lalowa chintabwalala zoti lingatukukenso ndakayika pokhapokha zipani zonse zitakhala pansi ndikupanga government of national unity.
@DennisWachepaАй бұрын
Nthawi ya kongelesi eeish. I am speachless
@user-sb2mw3xz4jАй бұрын
Munthu odana ndi chilungamo ndi choncho, Nanga lero si izi chilima ndi anthu kulibe, Nkasa volume 🎉please
@AlexMthunziChimpeni23 күн бұрын
Pa yekha Dpp siyingawine zizachitike za ku south Africa
@rashidsabwe16169 күн бұрын
Mkasa umakwana❤
@user-tb9wn1hb3mАй бұрын
Mkasa umativetsa kukoma ndi nyimbo zako
@FrankKalako-tm1bp11 күн бұрын
Nkasa big up❤❤❤❤
@MphimbaMphimbaАй бұрын
Kkkk koma nkasa mpaka "kuthila madzi pasimenti kut akolope ndimatako" kkkk
@IsaacKachimangagamahАй бұрын
Big Man mumatha kukwenza kamba muntengo
@chifundocharles2348Ай бұрын
Koma nkasa ndi nkasadi😂😂😂😂❤
@BiquitoniNsandamilaАй бұрын
Nyimbo imeneyi ndi 2018 musayidadwe lero . Nyimbo za nkasa zimapereka ulosi ameneyu ndi phuuuungu jooooseeephhh nnnnkasssssaaaaaa
@thomasphiri7799
Ай бұрын
really 2018?
@user-ri2vi2fd5v
Ай бұрын
Uzikanamiza banja lako wamva galu iwe, moti tonse pano 2018 tikalephere kuimvera ukamve iwe wekha
@AmossAkbar-bt1ks
Ай бұрын
Yes nyimbo iyi anayiyimbadi mu 2018 ndithu musayiware chikumbusa nkhwangwa ndi chisanu
@AdsonNamakonjeАй бұрын
Wamenya kwambili kasa, piter akangoliwa boma galimoto ukwela
@isaackaisi86235 күн бұрын
Mkasa ndi machine opangira machine azake
@KenuelIyanMarcus3 күн бұрын
Amuna awa
@user-kx4og4mv5yАй бұрын
😢😢😢😢 Lero Chilima ndimbiri
@AlexHenere-r6l5 күн бұрын
Mkasa waimba bwino. Imenei taikonda zikmo
@PaulDaka-dc3reАй бұрын
Kuganiza mwakuya Big man paja tisaiwale ndi phungu
@CharlesChambo-uz9pfАй бұрын
Umakwana Mr Nkasa
@RicardoManuelEstivin18 күн бұрын
Nkasa umaitha kwambili ❤
@EDSONMAKIYI-mu8yeАй бұрын
Powerful
@AlfredNazombe-me2lyАй бұрын
Uyuu akumwa ambuye ntengeni straight kkkk
@Gift-gt8em6 күн бұрын
No jealous Nkasa.umatha
@PhillipNyaugweАй бұрын
Nkasa umachita bwino koma takhalani pachimozi please yehova akusamalire
@user-lb6ek3ee6dАй бұрын
Zina kambu zina leku DPP MORE FIRE i like you Mr Mkasa taziwona tokha Malawi MCP mukozeke kuti tsopo mukukakha zaka 100 muli kunja simudzalowsso boma ayi dzitsiru dzawathu
@ChiefJustin-cl8jlАй бұрын
Zakumwa za mtundu wanji tikubweletsele mfumu mkasa ❤
Пікірлер: 224
Mumakwana amphungu Joseph I like your songs
Big up Nkasa umaimba zoona zokhazokha zounikira anthu❤❤❤❤❤ APM pachiongolero basi wina afune ❤❤❤
❤❤❤❤❤❤❤ very powerful mr favourite Mkasa💪💪
Kung'alura kung'alura basi mkasa wabwera ngati coming ADad My vote 🔥🔥
Good song Mr nkasa keep it
Ndakwela yomweyo ankasa mumakwana inuyo ❤❤❤
@OjessAndisoni
26 күн бұрын
Mumakwana.ambuye nkasa
🎉🎉🎉 respect mkasa
Mr Nkasa deserve a degree of honor Dr Nkasa on his musical journey which which sheds a light to those who are in the darkness
What a beautiful song it is. Agalu a mcp munya muona
Big up Nkasa kuswakuswa, chilungamo kuyenda ngati madzi 🔥🔥🔥🔥
Kuyankhula mudayamba kale Mr mkasa ndife osanva achina tione zina koma zoonazi tizaona nazo mkamwa mwankango mcp izipita abale anga kuba kwanyanya.
Nice tune 😊
Nyimbo yabwino heavy. Munthu ukachemelera chinthu chabwno zimachita kukoma chonchi
This guy is good always. Don’t be jealous of him please. Nkasa,💪💪
Inuyo ndi akatundu Ulemu Wanu Mr mkasa keep it up wina aphulika ndithu 😂😂
i love this song watching from cape town
Dolo kmb namiyambi sopano m'bwalo. God give you a long live
Big up mr nkasa
Amen 🙏 🙏 🙏 Nice song
Mkasa eish! ndikatundu omanga ndimawaya/mashini,mfundo pamaimbidwe ake palibenso,uyu ndi dolo woganiza bhoo heavy kkk ❤❤❤
Nice song Dpp my vote 🗳
Wow 😍 that's great advice
Koma mkasa machine 😂😂
More fire 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
inuyo ndi big basi mbambande akuti olo kuyifusa mizimu ikanakana kuti tambala wakuda asabweleso 💪💪💪😅😅😅
This is prophetic song
Mkasa keep it up singing trye
Nkasa ndi machine ❤❤❤❤
Sangakondweletse onse.Ndibwino amuleke chifukwa nayenso mpomwe akupezela mchere wake
Chipani chantendele on repeat 🎉😂😅❤
DPpppppppppp woyeeee ❤❤❤❤❤❤
Nkasa always unpredictable osamukhulupilila
Nice song
Nkansa sawopa naye tili kumbuyo kwako masa we still remember azibale athu anaphedwa ndi mcp zaka zambuyomu sitilora kuti mcp izawinenso 2025 never
Nice one ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Nyimbo yamphanvu kwambiri moto kuti buuuuuuuuuuuuuu 🔥 🔥
Odana ndi nyimbo iyi usiku amawuluka ndithu nkasa never give up
@JohnmarkNazombe-hi9xd
Ай бұрын
😂😂
Uyu wangonena zabwinozo basi ndipo palibe vuto apaaa😂😂
Amatha uyu siza a Lucius Banda ai
@blessingsnyalo-rp9ko
9 күн бұрын
Ndipo live
Ameneyu sazatheka
Nkasa youre number one 🎉🎉
Ndine zambian ❤ndimati ndingofunsa AFFORD ndi chanico🙏🙏
@chekiamaabdul5083
Ай бұрын
Afford ndi chiwelesye cha achakorwa nivipuwa wanvela ka iwe chifukala
@PrinceKachimanga
Ай бұрын
they want to.get back in power
Nichikali ichi panyimbo kkkk long live phungu Joseph mkasa
Apa ndiye wabwera mkasa umasiya kuti nyimbo ngati izizizi
Apm ikulowa Malawi wafikapa sakufuna azitsogoleri a try and error apm only hope for Malawians
@MarvellousTech-kz6no
Ай бұрын
Uyu ndiye mkasa amene ndimamudziwa ine , na pankhani yoyimba , amathira mbalume, adzaima naye ndindani , !
@Okalekale
Ай бұрын
Anapanga chani uyu?,Bingu yekha,awa ndimanyaka palibe chimene anapanga.Chiyambire cha democracy munthu anapanga zooneka ndi Bingu yekha,zinazi ndimbava zokha-zokha,dziko la Malawi linapita ndi Kamuzu ndi Bingu.Nkasa waona kuti chifukwa anthu akuganiza kuti Chakwera wapha Chilima ndiye kuti DPP idzawinaso wayamba kale kuseteka matako a Peter,opportunist iwe ndale za pa Malawi mwazilowetsa umbuli kwambiri,dzikoli lalowa chintabwalala zoti lingatukukenso ndakayika pokhapokha zipani zonse zitakhala pansi ndikupanga government of national unity.
Nthawi ya kongelesi eeish. I am speachless
Munthu odana ndi chilungamo ndi choncho, Nanga lero si izi chilima ndi anthu kulibe, Nkasa volume 🎉please
Pa yekha Dpp siyingawine zizachitike za ku south Africa
Mkasa umakwana❤
Mkasa umativetsa kukoma ndi nyimbo zako
Nkasa big up❤❤❤❤
Kkkk koma nkasa mpaka "kuthila madzi pasimenti kut akolope ndimatako" kkkk
Big Man mumatha kukwenza kamba muntengo
Koma nkasa ndi nkasadi😂😂😂😂❤
Nyimbo imeneyi ndi 2018 musayidadwe lero . Nyimbo za nkasa zimapereka ulosi ameneyu ndi phuuuungu jooooseeephhh nnnnkasssssaaaaaa
@thomasphiri7799
Ай бұрын
really 2018?
@user-ri2vi2fd5v
Ай бұрын
Uzikanamiza banja lako wamva galu iwe, moti tonse pano 2018 tikalephere kuimvera ukamve iwe wekha
@AmossAkbar-bt1ks
Ай бұрын
Yes nyimbo iyi anayiyimbadi mu 2018 ndithu musayiware chikumbusa nkhwangwa ndi chisanu
Wamenya kwambili kasa, piter akangoliwa boma galimoto ukwela
Mkasa ndi machine opangira machine azake
Amuna awa
😢😢😢😢 Lero Chilima ndimbiri
Mkasa waimba bwino. Imenei taikonda zikmo
Kuganiza mwakuya Big man paja tisaiwale ndi phungu
Umakwana Mr Nkasa
Nkasa umaitha kwambili ❤
Powerful
Uyuu akumwa ambuye ntengeni straight kkkk
No jealous Nkasa.umatha
Nkasa umachita bwino koma takhalani pachimozi please yehova akusamalire
Zina kambu zina leku DPP MORE FIRE i like you Mr Mkasa taziwona tokha Malawi MCP mukozeke kuti tsopo mukukakha zaka 100 muli kunja simudzalowsso boma ayi dzitsiru dzawathu
Zakumwa za mtundu wanji tikubweletsele mfumu mkasa ❤
Ulemu wanu mr Nkasa kunyimboyi osati manyaka timava aja osapota mcp agaluu
This is exactly what was really happening in those days now again but this is really worse
Kuma yamikila m,zathu akapanga chabwino nkasa patsogolo
Nkasa timakukondani bwana nyesani ina mcp imve pain
Bg up mkasa
nkasa amatha. kuvunga mbili yonse ya mcp.. Koma akut vuto amalawi stimachedwa kuiwala 😭😭😭😭😭😭
Nde mwati mcp ndima chani😂😂😂😂😂km zoona2
Mukamaika zithunzi za a dad anuwo muziika za mmene akuonekera panopa osati zakale kalezi
Mbuyanga taponyani number yanu plz tiponyeko ya cold drink plz
Mesa nyimbo iyi ndiyakalekale?
Big up mkasa
nde afford yakwiyanso chani😂😂😂😂😂😂😂munthu asanene chilungamo???
Chilima adaferanji mkasa more 🔥
Big up mkasa that's the fact
Zoonadi Simukunamana Mr Mkasa ulemu
Padulidwa mtengo waminga sipathekadi kumera wa papaya eeeish nkasa ka volume kakwezedwe pang'ono
DPP NDI MORE FIRE...RESPECT
Number one
Big man muzetikumbusa pafupipafupi
Zoooooona❤❤❤❤!!!!!
Mamuna oziwa kuyimba nkasa
Eeeeee koma nkasa aaa inu ndi bigy mawu ndilibe mmatha kulinganiza eee
Mkasa ndi big uyu amaimba
Kkkkkkkkkkkkk amkasa sadzatha 😂😂
Taponya nambala yako ndikupatse ya tea
@MalawianCamera
Ай бұрын
😂😂😂😂 Boss
Fact! 👍👍👍👍👍👍
Umenyenso inanso yomuza live chakwera kuti siwe mfumu ayi koma zinango lakwika
Zoona Malu mkasa
Umakwana bro
❤❤
Wina afune asafune APM akulamula, mkasa ndi katundu Dpp more fire ✅😜😜😜