😂😂😂 kodi guys ndiye kuti simungakomentepo za ubwinoko wa MCP 😂😂😂😂 ndiye kutidi anthu amenewadi ndioipa eti😂😂😂😂 kumanya mundu kutama najo eti😂😂😂 my son give me sima let me simaring myself 😂😂😂😂 ndiye mwati chikatere madolowa akunva bwanji😂😂😂ndikuivunga pa mukuru vote yanga ku ppd😂😂😂 ayi ndalakwisa ku fdu😂😂😂 ayi ndalakwisanso koma ku MTU 😂😂😂 this week mpaseni mpata akalape😂😂😂 chifukwa ijayo ya mchinga ija yandikwana kwabasi.
@AlexManuelMisomali-sv1vn20 күн бұрын
Munaika nokha MCP m'boma lero MCP yakuchangamutsani and you have nowhere to go
@JacksonMoyo-tm8dv21 күн бұрын
Chakwera kulibe chake 2025
@Kasiya-gp7fm23 күн бұрын
Wozugurira mitu nde iwetu😅
@user-ev6bi7jr7g23 күн бұрын
Za m'mbuyo mwa alendo zimenezi munayenera kuzichita chaka chatha ena asanaluze myoyo yao
@IssacMateyo22 күн бұрын
Musamanamepotu apa kunyumba kwa vp angaloweko chotcho kulibe asitkali zazi kkkkkkk
@louisbonongwe8537
19 күн бұрын
Ur thinking and sight has boundaries i can witiness....unaona zinachitika ku kenya?anthu anakaphwanya ku parliament.....anthu akakwiya bwana mfut ija samainva.
@ephraimkadamika23 күн бұрын
No alliance with mcp period
@user-uc1pd1tc2x23 күн бұрын
😂😂😂😂
@Kenmoney-xp7tz23 күн бұрын
Ngati simukuopa nde mukugwada chani zitsiru za amalawi
@inessmsiyambiri8517
23 күн бұрын
Chitsiru ndi iweyo
@hanifahmponda871123 күн бұрын
Zowona galu modzi tsakukuma kawili kuluma koyamba ndi mistake ya galu koma kukuluma kachiwili ndi mistake yaiwe munthu nde MCP yakuphelani chilima It's ok kuti munayiwala kuti MCP yokupha KOMA PANO MUKALOLATSO KUKALATSO KHASU LA MCP DZIMU WACHILUMA UKUSWANI DZIDI MUKOMANA NDI NYENKWEEEE AKWENI CHENJELANI MCP SICHIPANI CHOPANGA NACHO UBALE MAWONATSO NOKHA manganya uyutu wamitsala mutsamutengele dzelu zaka tiyene nadzo paja muti sutuluka akulowa TIYENI TIDZILOWANO KKKKLL
@CHIWSABINYAMBOSE18 күн бұрын
No zithe basi
@user-bd5kw8oq1r23 күн бұрын
Zopanda pake mbuli zokhazokha
@KhooMadex
23 күн бұрын
Ukati what are you trying to say, anthu sakufuna alliance ndi mcp so akhala bwanji mbuli?
@user-bd5kw8oq1r
23 күн бұрын
@@KhooMadex ndi malingalilo awo woti chilima amachita kuphedwa ndi omwe ali mmutu mwawo komaso achita kutumidwa ndi ena a mumchipanimo omwe sakufukondwa ndi kusankhidwa kwa a Michael usi ndi ndale izi zimafunika mbuli zizimva mabodza awo ine ayi 😊😊😊
@user-le9su3mt7r23 күн бұрын
Mcp chipani chakupaa
@user-bd5kw8oq1r
23 күн бұрын
Ndipo inu 😅 Ngati DPP imaphaso ma lubino,isa njaunju ,chasowa,ndi ena bola yesu basi ndi more Fire yesu ossti andale ayi koma ine ndikavotera MCP mnkhani zopanda umboni sitichita nawo ngozi ya ndege ndimayidziwa ine mkovuta kupulimuka 😅😅😅😅
@AbdulKaswiri22 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
@CatherineKumwex23 күн бұрын
😂😂😂
@AbdullahaziziAmoswalala23 күн бұрын
?😂😂😂😂😂
@officialturfrican_ent23 күн бұрын
Sorry i saw white woman, correct me😢
@officialturfrican_ent
23 күн бұрын
This black dude humbled himself for a reason,,,kumalawi kulibe kape if u oppose kape ndi iweyo nyini yamako
@ManifoldPhiri22 күн бұрын
Anthu akumamkhalabe ndi nthawi ya zimenezi mmalo mokonza mtima wanu kuyanjana ndi mulungu. Kodi simunawelenge bible zochitika mmasiku otsiliza?
@stevenoah4578
22 күн бұрын
Komatu ngati inu mwaika comment ndekuti mwatayanso nthawi ndi zomwezi. Simukusiyana ndi winna aliyense. Don't pretend to be spiritual.
@ManifoldPhiri
22 күн бұрын
@@stevenoah4578 kkkkkkk koma achinyamata akunyanya
@SaidiMbawa-st6bj23 күн бұрын
Achita kutumidwa Mcp ndi chipani cha mphavu pachokha
@ShalifahKasimu
23 күн бұрын
Mphavu yake itiso nanuso
@innocentmusuli7380
23 күн бұрын
Kkkkkk mukutanthawuza kuti a UTM atuma anyamata a UTM ku mtsokhano wa UTM zosekesa kwabasi anthu ena mitu sigwira
@SaidiMbawa-st6bj
23 күн бұрын
@@innocentmusuli7380 a Dpp akufuna utm kuti achoke ku gwilizano koma sizitheka chifukwa akulu akulu oziwika bwino sakufuna ndiye munthu ulibe ndalama ungatani ndiposo sokhano walero cholinga chake sichimenecho
@SaidiMbawa-st6bj
23 күн бұрын
@@ShalifahKasimu ndichimene chikulamula iwe sukuziwa utm iri ndi mphavu zanji ku mcp
@InessMchenga
23 күн бұрын
Mphamvu zake zitizo paiwo okha anakawina amene aja za zodza basi
@user-qq3ip1od6i22 күн бұрын
Comedian is not patriot to the movement
@yowasschitsosa534823 күн бұрын
Apupuluma sakuganiza bwino achinyamawa dziko si anthu 50 ndi mamilion
Пікірлер: 126
Madam kaliyati ankhale president wa UTM
Osaopa 💪 Osatopa 💪 Osafooka 💪 SKC FOREVER IN OUR HEARTS 💕 NO! Alliance with MCP ndi chipani ca kupha!
@AaronzoAaron
20 күн бұрын
Aaaaa kokaaaaa
No alliance with MCP ndiakupha amenewo ng'ona dzimenedzo
Good achinyamata a utm munthu oipa aziwoneka poyera osati ena amene akubisa anthu oipa kuti aziwoneka abwino. Osaopa osafoka. I
Alliance ithe basi
I agree 100% NO ALLIANCE WITH MCP
Ndipo mwayitha, wina asowa wopanga naye alliance.
@CeniaMayeni
23 күн бұрын
😂😂😂😂😂😂
Good excellent that is my bro
🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥 achinyamata!!!moto kuti bhu! achinyamata aneneo,wachinyamata ndi wachinyamata ndi kawawa
Very good
More fire youth men,big up
That's the spirit guys. Fight for our rights
No alliance with Chikangawa party
@user-ww4ei5fb7d
22 күн бұрын
😅😅😂
Moto kuti 🔥🔥Osawopa,Osatopa, osafooka
UTM, DPP, AFORD ndi UDF udzakhala mgwirizano wa mphamvu kuchotselatu nyansi zili mu bomazi.
@IssacMateyo
22 күн бұрын
Ndiye zopusazo zimenezo akapangeso gwilizo wina apange okha kaya ndiye kumeneko sakanamizaso
@user-pv9uk6sc3w
22 күн бұрын
@@IssacMateyo no brother, pawokha sangafike 50+1, kungoti all leaders akhale ndi maudindo in government.
Good news for ever🎉
Ngati usi sakufuna akhale Ku MCP sivuto tizamumangira limozi iyeyoso akuziwa zonsr
Yaaaa, Ukunde kuganizaa bhoooo kujaa ukuuuu.
Big up Guys
Kuli Yehova kumwamba
Yes I gree ❤100%
Kkkkkkk 😂, MCP idaotcha CV pa 10 June
Ndipo asakupusiseni muthetse m, gwilizano umenewo osakonda ndrama anamusasa kale Tate wanu m,pakana. Amupha chokhalila kumeneko ndi chani
Ehhhhe No Alliance Iyyyah Makape a MCP akhale okha
Zilikotu zilikotu.....halayansi must end sure...aliyense adzadutse yenkha....
Asaopa osafooka I'm miss chilima
I like this
Mayi kaliyati ulemu wanu
More fire
Very good utm
That's great move😂😂
Anyamata ipatseni moto tatopa ife
alliance ithe MCP ilibe pabwino
Good job
Viva skc ...RIP..
Go deeper
Osawopa
Utm moto unandi mwachita bwino mama kaliat😊
Kkkkkkkk dziko la pansi
Achinyamata Saulosi adapita komano presidential immunity ichoke tikwanilise masophenya a SKC referendum basi . Achinyamata dziko lino Palibe angalikoze koma ife. Chakwera adati azachepesa phamvu koma kuti .
Anyamata akunena zoona osapanga mgwirizano ndi MCP .
Mphamvu zokuphatu osati kulamulila dziko
Yaa ineso ndagwilizana nazo asiyeni agaluwo
No alliance with mcp
Zayamba bwino
🎉🎉🎉😂 good luck utm
Gwadani guys, no Alliance at all
Sitirora
We follow u guys no mo alliance
More fire youths
Osaopa... Osafooka osatopa
Ndimayembekeza kuva zimenezo
Tienaoni amenewo alliance yathapo basi apa
Wabodza uyu kunali ku office ya UTM ku area 10 kulilongwe tsiku lothesa mgwilizano lija osati zomwe akunamazo
Wow osaopa
Bora pamenepo
Amalawi ake si amasiku ano
Mphamvu zokuphatu osati kulamulila dziko 0:05
inthe Alliance.
Zofunikira kuipasa moto osaopa
Zikathela mapenateee
Za alliance zatha apapa hiyaaa
Uthe kumene
Kkkkk km kuki kugwadatu
🔥🔥🔥🙌
Kwavuta
Powerful!!!!
Mcp ndikachaniso
Kapena kumene amakhala Kale kuja mwina kapena
💪💪💪💪💪
Osaopa ndithu
Calculated move
But be care some are thieves u never know
Mwachitabwino muyime panokha ifenso ku DPP sitikukufunani agalu achabechabe inu zoti mubwelela ku DPP sizitheka Mesa mumatitukwana inu chonsecho chilima kupanda DPP bwezi ataziwika kuziko la Malawi mwana oti tinachita kuntola nkumatitembenukila kutiyimila pachulu chifukwa choti kaliyati amamupusisa yendelani yanu tikuoneleni
Mbola kkkkkk Mudya ndalama koma movutikila 😂😂😂😂
Mmmm
Kusowa zochita mumakomomu
Kkkkkkkk 😂😂😂😂😂😂😂 Amen
Usi Munthu oipa
😂😂😂 kodi guys ndiye kuti simungakomentepo za ubwinoko wa MCP 😂😂😂😂 ndiye kutidi anthu amenewadi ndioipa eti😂😂😂😂 kumanya mundu kutama najo eti😂😂😂 my son give me sima let me simaring myself 😂😂😂😂 ndiye mwati chikatere madolowa akunva bwanji😂😂😂ndikuivunga pa mukuru vote yanga ku ppd😂😂😂 ayi ndalakwisa ku fdu😂😂😂 ayi ndalakwisanso koma ku MTU 😂😂😂 this week mpaseni mpata akalape😂😂😂 chifukwa ijayo ya mchinga ija yandikwana kwabasi.
Munaika nokha MCP m'boma lero MCP yakuchangamutsani and you have nowhere to go
Chakwera kulibe chake 2025
Wozugurira mitu nde iwetu😅
Za m'mbuyo mwa alendo zimenezi munayenera kuzichita chaka chatha ena asanaluze myoyo yao
Musamanamepotu apa kunyumba kwa vp angaloweko chotcho kulibe asitkali zazi kkkkkkk
@louisbonongwe8537
19 күн бұрын
Ur thinking and sight has boundaries i can witiness....unaona zinachitika ku kenya?anthu anakaphwanya ku parliament.....anthu akakwiya bwana mfut ija samainva.
No alliance with mcp period
😂😂😂😂
Ngati simukuopa nde mukugwada chani zitsiru za amalawi
@inessmsiyambiri8517
23 күн бұрын
Chitsiru ndi iweyo
Zowona galu modzi tsakukuma kawili kuluma koyamba ndi mistake ya galu koma kukuluma kachiwili ndi mistake yaiwe munthu nde MCP yakuphelani chilima It's ok kuti munayiwala kuti MCP yokupha KOMA PANO MUKALOLATSO KUKALATSO KHASU LA MCP DZIMU WACHILUMA UKUSWANI DZIDI MUKOMANA NDI NYENKWEEEE AKWENI CHENJELANI MCP SICHIPANI CHOPANGA NACHO UBALE MAWONATSO NOKHA manganya uyutu wamitsala mutsamutengele dzelu zaka tiyene nadzo paja muti sutuluka akulowa TIYENI TIDZILOWANO KKKKLL
No zithe basi
Zopanda pake mbuli zokhazokha
@KhooMadex
23 күн бұрын
Ukati what are you trying to say, anthu sakufuna alliance ndi mcp so akhala bwanji mbuli?
@user-bd5kw8oq1r
23 күн бұрын
@@KhooMadex ndi malingalilo awo woti chilima amachita kuphedwa ndi omwe ali mmutu mwawo komaso achita kutumidwa ndi ena a mumchipanimo omwe sakufukondwa ndi kusankhidwa kwa a Michael usi ndi ndale izi zimafunika mbuli zizimva mabodza awo ine ayi 😊😊😊
Mcp chipani chakupaa
@user-bd5kw8oq1r
23 күн бұрын
Ndipo inu 😅 Ngati DPP imaphaso ma lubino,isa njaunju ,chasowa,ndi ena bola yesu basi ndi more Fire yesu ossti andale ayi koma ine ndikavotera MCP mnkhani zopanda umboni sitichita nawo ngozi ya ndege ndimayidziwa ine mkovuta kupulimuka 😅😅😅😅
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
😂😂😂
?😂😂😂😂😂
Sorry i saw white woman, correct me😢
@officialturfrican_ent
23 күн бұрын
This black dude humbled himself for a reason,,,kumalawi kulibe kape if u oppose kape ndi iweyo nyini yamako
Anthu akumamkhalabe ndi nthawi ya zimenezi mmalo mokonza mtima wanu kuyanjana ndi mulungu. Kodi simunawelenge bible zochitika mmasiku otsiliza?
@stevenoah4578
22 күн бұрын
Komatu ngati inu mwaika comment ndekuti mwatayanso nthawi ndi zomwezi. Simukusiyana ndi winna aliyense. Don't pretend to be spiritual.
@ManifoldPhiri
22 күн бұрын
@@stevenoah4578 kkkkkkk koma achinyamata akunyanya
Achita kutumidwa Mcp ndi chipani cha mphavu pachokha
@ShalifahKasimu
23 күн бұрын
Mphavu yake itiso nanuso
@innocentmusuli7380
23 күн бұрын
Kkkkkk mukutanthawuza kuti a UTM atuma anyamata a UTM ku mtsokhano wa UTM zosekesa kwabasi anthu ena mitu sigwira
@SaidiMbawa-st6bj
23 күн бұрын
@@innocentmusuli7380 a Dpp akufuna utm kuti achoke ku gwilizano koma sizitheka chifukwa akulu akulu oziwika bwino sakufuna ndiye munthu ulibe ndalama ungatani ndiposo sokhano walero cholinga chake sichimenecho
@SaidiMbawa-st6bj
23 күн бұрын
@@ShalifahKasimu ndichimene chikulamula iwe sukuziwa utm iri ndi mphavu zanji ku mcp
@InessMchenga
23 күн бұрын
Mphamvu zake zitizo paiwo okha anakawina amene aja za zodza basi
Comedian is not patriot to the movement
Apupuluma sakuganiza bwino achinyamawa dziko si anthu 50 ndi mamilion