A Ntanyiwa Mubweletse Umboni Pasanathe 72 Hrs - Agape Khombe

On Nyasa VoiceBox, Agape Khombe responds to allegations that he is a drug dealer and is implicated in the death of Ralph Kasambara in Lilongwe. He also warns Comrade Ntanyiwa of Limpopo FM, who made the allegations, about legal action if he does not provide evidence to support his claims.
Ku Nyasa VoiceBox, Agape Khombe akutsutsa phekesela yoti ndi wogulitsa mankhwala ndipo akukhudzidwa ndi imfa ya Ralph Kasambara ku Lilongwe. Iye akuchenjezanso Comrade Ntanyiwa wa ku Limpopo FM, yemwe wanena izi, za milandu ngati sapereka umboni wotsimikizira zomwe akunenazo.
#malawi

Пікірлер: 273

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn13 күн бұрын

    Mtanyiwa amanenatu zoona,paja anatumiza audio kut ndege yagwa ndipo anthu afelatu onse koma inu mumkalesa lero ndizabodzaso? Mulekeni mtanyiwa we love mtanyiwa❤

  • @KellyHart-pi4hd

    @KellyHart-pi4hd

    13 күн бұрын

    Ayi asamuleke awayaluse Ntanyiwa ndakharapo naye gulu limodzi akafuna kutulutsa Nkhani amakhara wasunga maumboni onse ndiye awayike pambarambanda

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i13 күн бұрын

    Ok we are waiting for the serious action you mentioned, this is how we know you people,but nothing is hidden on earth.

  • @John-to8gl
    @John-to8gl13 күн бұрын

    Utsi sufuka popanda moto bwana!!

  • @augustMag
    @augustMag12 күн бұрын

    Mtanyiwa is the best like Bakili Muluzi TV ❤❤❤❤

  • @user-ky4ce9gb6j

    @user-ky4ce9gb6j

    12 күн бұрын

    Ndipo kwambiri tu mmm

  • @JohnBanda-ux9fy
    @JohnBanda-ux9fy13 күн бұрын

    72h ikatha bwera udzaone ngati udzazikonde galu mbuzi manu kumusi ..biry malata ali ndi ntchito yanji wamisala ngati ameneyo galu wachabechebe

  • @JohnConar-kq4hi
    @JohnConar-kq4hi13 күн бұрын

    This is mcp. Chilima still living we need true story about Chilima that's 🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼home land

  • @Mussa-qs7km
    @Mussa-qs7km13 күн бұрын

    Mukfuna mumuphenso ntanyiwa.sabwera

  • @khoviwaedward
    @khoviwaedward13 күн бұрын

    Iiiii ndalama ndi yoopsa kwambiri,dziko lathu la Malawi chipwirikiti pwirikiti kufuna ndalama. Ana anjoka inu

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm13 күн бұрын

    Agape Khombe ndi mfiti kapena kuti nthakati oyipa kwambiri.

  • @user-lt9xb8sq1r
    @user-lt9xb8sq1r13 күн бұрын

    Mwagwidwa basi inu

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe821413 күн бұрын

    Ubwino wake muli ku Boma nde mkona kuyankhula motha mawu unagwilira anamutsekera natuluka nde olo utapha munthu sukuopadi.. Bola unakangokhala. Osayankha..

  • @JohnOmar-mf2pu
    @JohnOmar-mf2pu12 күн бұрын

    Uyamba iweyo kufa bro unapangiranji I we ,oipa iwe kwambiri anaazako ndiamasiye pano chifukwa chaiwe umusiye wa Limpopo apitirize kuurura zomwe mumpanga agaru inu

  • @user-zj1xx1ic2m
    @user-zj1xx1ic2m11 күн бұрын

    Iweyo ndi galu ndipo ndiwe m'modzi mwa anthu akuphawo ndipo ukunama sungawowopseze mbuzi ya munthu😢😢😢

  • @sahasalanje4786
    @sahasalanje478613 күн бұрын

    Munthawi inoyo muzikana koma pachoka nzimu wamunthu chilungamo chizaziwika tizanweza mopweteka zangoyamba

  • @CharlesmakveliNyirenda
    @CharlesmakveliNyirenda12 күн бұрын

    Mtanyiwa the best

  • @LawrenceMsopa-ym1gf
    @LawrenceMsopa-ym1gf13 күн бұрын

    USAOPSEZE ANTHU KUTI TISIYE KUKAKAMBA CHILUNGAMO BIG

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm13 күн бұрын

    Khombe ndi Chigawenga.

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx13 күн бұрын

    Ntanyiwa adali oyamba kunena kt ndege yapezeka ndipo onse afa mudatsutsa a aaaa a kupha inu

  • @user-ms8tm3yf7d
    @user-ms8tm3yf7d13 күн бұрын

    Onjeza kwambili moto Ntanyiwa ayamba kubwera okha pammbalambanda atchulana onseeeee🔥🔥🔥

  • @user-si7po9sd5i

    @user-si7po9sd5i

    13 күн бұрын

    Kkkkkkkkkkkkkkkkk

  • @alfredjosen8207

    @alfredjosen8207

    12 күн бұрын

    😂😂😂😂😂

  • @wittinessnkhokwe
    @wittinessnkhokwe12 күн бұрын

    Chilungamo chotani popeza here in Malawi we have corrupt judicial system

  • @MCDONALDTHENGENDE
    @MCDONALDTHENGENDE12 күн бұрын

    Wakupha naye azafa pomwe wakhalapo ndi pamanda usanyadire Thanks

  • @wilsonfelix6559
    @wilsonfelix655913 күн бұрын

    Nkhanga ziona ❤❤❤❤mntanyiwa on limpopo fm

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred653912 күн бұрын

    Thanyiwa koma sanama please mumati mwabisala koma muli pantente

  • @MrMwambananji-tx8jt
    @MrMwambananji-tx8jt13 күн бұрын

    Choka!! Wokonda ndalama iwe.

  • @KellyHart-pi4hd
    @KellyHart-pi4hd13 күн бұрын

    Iwe usanene zambili tangobwera anyamata azakuthudzule ndi Chipolopolo

  • @AudreyMwangonde
    @AudreyMwangonde12 күн бұрын

    Ndinu achifwamba agape khombe

  • @KassimIssa-bn3od
    @KassimIssa-bn3od13 күн бұрын

    Pot amalamulowo munagula

  • @hassammaulana4529
    @hassammaulana452913 күн бұрын

    Koma ngati mukuziwa kathu mlungu azakuyalusani komaso no matter what koma muziwe zoti mlungu akukuonani nonse

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma461512 күн бұрын

    Amazitenga kwanu ku Malawi 🇲🇼 koko unachita kutumidwa ulibe umunthu iwe choka apa za zii

  • @Luxemaven8686
    @Luxemaven868613 күн бұрын

    He sounds so defensive like a guilty man kkkkk #TeamNtanyiwa

  • @user-fg7xx7gq5b
    @user-fg7xx7gq5b13 күн бұрын

    Opusa iwe u cant intimated mr Ntanyiwa bro

  • @CharlesmakveliNyirenda

    @CharlesmakveliNyirenda

    12 күн бұрын

    Kkkkk zoona bro

  • @PatrickMulangala-os4by
    @PatrickMulangala-os4by2 күн бұрын

    He talks truth

  • @user-zg8rt3tz9g
    @user-zg8rt3tz9g12 күн бұрын

    Anthu okupha inu.. what serious action you're talking about kwa ntanyiwa?

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal3 күн бұрын

    Wavomelezatu kuti ndiwe wakupha 😢😢

  • @Luxemaven8686
    @Luxemaven868613 күн бұрын

    Ine I believe Antanyiwa as there is no smoke without fire.

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu13 күн бұрын

    Ok

  • @josephphiri7481
    @josephphiri74814 күн бұрын

    It's seems like true because of response

  • @user-uw3sp6rq8m
    @user-uw3sp6rq8m12 күн бұрын

    😢unapha ndiwe osewa angakhale abodxa

  • @ebenezerkamanga6016
    @ebenezerkamanga601613 күн бұрын

    Apolisi ake ati anafufuzawo panyo pako sopano pote unamata mmawindo uja machende ako

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri851713 күн бұрын

    Muyaluka agalu ojiya

  • @ReubenMuhuwa
    @ReubenMuhuwa13 күн бұрын

    He confess what he is

  • @user-ti8ds7iq8z
    @user-ti8ds7iq8z13 күн бұрын

    Zaziiii

  • @HendersonSalanje
    @HendersonSalanje11 күн бұрын

    Mtanyiwa kweza volume

  • @Sabina-hw4js
    @Sabina-hw4js6 күн бұрын

    God knows the truth

  • @elishathomson6083
    @elishathomson608312 күн бұрын

    Inuyo mukunena zimenezo ,poti mukudziwa kuti anapanga delete cc tv yonse

  • @user-jm5bs9uk5k
    @user-jm5bs9uk5k13 күн бұрын

    Utsi ukachuluka ku uwuna wa mbewa, mbewazo zimasaka malo otulukira ndipo zimatuluka zokha

  • @KassimIssa-bn3od
    @KassimIssa-bn3od13 күн бұрын

    Ndiye iweyo ukukana galu iwe

  • @innocentjackson2003
    @innocentjackson200310 күн бұрын

    Eeeeh moto wabukatu apa 😢

  • @SumaniMtenje
    @SumaniMtenjeСағат бұрын

    Tikudikirani debeni muno basi borani mubwere ndimakwacha ambiri

  • @coastersRob
    @coastersRob13 күн бұрын

    kodi chidzungu ukuyakhulacho

  • @SothiniPhiri-tk5eh
    @SothiniPhiri-tk5eh10 күн бұрын

    Agape Khombe ndi mfiti and no doubt atha kupanga izi. Kupemphera kwachani apaaa. Bwenzani ndrama munadyera mnzanu zija

  • @Luxemaven8686
    @Luxemaven868613 күн бұрын

    Ati ngozi, ngozi ya man made yo yoti wanzeru aliyese akuona.

  • @user-lk8kj9zv6x
    @user-lk8kj9zv6x13 күн бұрын

    Ea ali ndi umboni tu

  • @CharityMhone-uk9ym
    @CharityMhone-uk9ym12 күн бұрын

    Aaaa sukaaa ndichizungu chosamveka ndi sound yabwino, bwanji kuopseza do you think anthu angakuope asatana inu tsek

  • @RebeccaWalusa-lb5yi
    @RebeccaWalusa-lb5yi13 күн бұрын

    Billy Kaunda anaimba oyenda ndilupanga azafa ndilupanga ?

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y13 күн бұрын

    Akugwilani

  • @AufiThera
    @AufiThera7 күн бұрын

    Tive zoonad chomwe chapha anthu awa

  • @SumaniMtenje
    @SumaniMtenjeСағат бұрын

    Musapase 72yo tazingo onesa azizanu sapangaizi

  • @enifamussa3151
    @enifamussa315112 күн бұрын

    Mumabisala mmbatata lero dziko lamva😢😢😢

  • @TalinesLwanda-xg5vi
    @TalinesLwanda-xg5vi12 күн бұрын

    Honestly saying mtanyiwa sakunama anthu Inu ndinu akupha 😢,,mkulimba mtima coz mkuziwa that u do it under secret nde mumatamikano not knowing that they are people like mtanyiwa

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma4 күн бұрын

    Osasiya kuulutsa umanena zoona usawaope akuphaamenewa

  • @serakillo8668
    @serakillo866813 күн бұрын

    Mukuopa mulandu mudikire kaye utsi tsufuka popanda moto. ..munanyanya kuyera maso kunya ndalama zamangazi ku mcp munyera matumvi....tiye nazo tanyiwa ipatse moto azingokwera ma bp onkha. ..agalu afiti awa opephera chakwera muthu opanda chibwano ndi anyani ake.

  • @LovelyBlini-cu3iu
    @LovelyBlini-cu3iu13 күн бұрын

    Zaziii

  • @PayesaPatrick-px1ob
    @PayesaPatrick-px1ob12 күн бұрын

    Ndiye utani akupha inu

  • @user-mf8fi8wt5d
    @user-mf8fi8wt5d12 күн бұрын

    The MCP will never cover this up

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba12 күн бұрын

    Ntanyiwa sakubwela kuno mumugwila mumuphe ndipo siwamisala ziko loseli watchula inuyo bwanji mukuziwana

  • @rashidadan2533
    @rashidadan253312 күн бұрын

    Mukufuna mtanyiwa mumudyenso akabwela , mwatchukatu ndikumwamba komwe , Olo angelo ayamba kukuthawani a MCP.

  • @PraiseLister
    @PraiseLister13 күн бұрын

    Mmmmm mwayamba kale kunjenjemelatu kkkk tchimo liZuza ochitanu

  • @ChawingaMwaseteza
    @ChawingaMwaseteza13 күн бұрын

    Akulu kambani za issue yanu zinazo muchedwa,,

  • @stevenmalirana8156
    @stevenmalirana815612 күн бұрын

    Kutsutsaku kuperekabe mafunso

  • @kelvindickson
    @kelvindickson10 күн бұрын

    Mwatambisisa mu Lilongwe mo

  • @user-oj7uc5kw7w
    @user-oj7uc5kw7w3 күн бұрын

    Ndaletu nzoopsya, ukalowa umakhala wasainira mabvuto

  • @ThokohKalonga
    @ThokohKalonga13 күн бұрын

    Inu mukudzibvuta chani akuwalephera boma mukakwanitse inu 😂😂😂😂

  • @ebenezerkamanga6016

    @ebenezerkamanga6016

    13 күн бұрын

    Kkkk ndipo ase awa ndi mbuzi

  • @ThokohKalonga

    @ThokohKalonga

    13 күн бұрын

    @@ebenezerkamanga6016 apenga awa kkk

  • @SildaKatundu
    @SildaKatundu12 күн бұрын

    Ku Malawi kulibe police,army ,court yachilungamo .Mulungu ekha akudziwa chilungamo chimene chaapha a Ralph ndi onse omwe anakwera ndege aja Not zomwe alengeza a boma zija

  • @user-zk5nu5fh6l
    @user-zk5nu5fh6l12 күн бұрын

    Palibe chinsisi

  • @phillipchiotcha3197
    @phillipchiotcha319712 күн бұрын

    Ntanyiwa adali oyamba kulengeza kuti ndege yagwa onse afa uyu sanama

  • @SamukLungu-zg7fl
    @SamukLungu-zg7fl12 күн бұрын

    Yikuti 72hrs yantha bwera kuno mbuzi iwe umawona ngeti 72hrs ndikutari bwera

  • @jackiendlovu9564
    @jackiendlovu956412 күн бұрын

    Ndiye ngati anatengedwa ndi transport inu mukuganiza zoti transport amenewo amadziwa komwe anthuwo amakhala, afiti okupha mukufunanso mumuphe Ntanyiwawo afiti inu ngozi yake yochita kulengayo

  • @richmwar7880
    @richmwar78809 күн бұрын

    Koma nde #nglish ya Chichewa esh... Mot kumapetoko angoziwululatu

  • @eliotchigona7959
    @eliotchigona795912 күн бұрын

    Very simple Comrade Ntanyiwa says ask the owner of the Lodge to provide the Camera's footage ku ma hours omwe zinachitika izi if you are failed to then you are not clean. Just prove yourself

  • @user-wu4tl2yn9e
    @user-wu4tl2yn9e12 күн бұрын

    Palibe kuopsezana aise,,,, ntanyiwa ipatse motooo malawi ndiwathu palibe kupepetsa boma linatenga ma radio onse ndinu nokha our last hope

  • @user-wb9ji3oe5o
    @user-wb9ji3oe5o12 күн бұрын

    Kunyankhula kwanu kungosonyeza kuti ndinu a MCP anthu akupha.

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole12 күн бұрын

    Bwera adzakutumbule wayaluka chitsilu.

  • @augustMag
    @augustMag6 күн бұрын

    Nanga komatu mmmmmhu Mulungu kumwambako akuwona maso Ake akuyang'ana pansi pano Mulungu alibe kumubisira kanthu zonse iye amdziyika poyera

  • @JohnsonRannel18
    @JohnsonRannel1812 күн бұрын

    Akuyakha wosadandaula

  • @EliasKawuwa
    @EliasKawuwa11 күн бұрын

    Ntanyiwa ndi wamusala,munthu opanda zeru,if anything amene amamuuza nkhaniwo nawoso mitu yawo ndiyoduka, Raph basi kungomuponyera basi iyeyo kumwa zoona? Iyeyo chinyama,kapena galu? Zoona

  • @ShackluSymon-cq7et
    @ShackluSymon-cq7et11 күн бұрын

    72hs yachuluka witness we found after one minutes mbuzi iwe

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN12 күн бұрын

    Ooh right,you have never taken a strong drugs as such,but fake drugs mesa!!! Ndie mukanaila zchan baba.

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp12 күн бұрын

    Anthu akudkila kuika malilo ndy Kut inuyo ngakhale mukuyankhulazo mulibe mzelu anzanu akulila inu mukufuna umbon kusonyeza Kut malilo mulibe nawo ñtchito mulungu akuoneni aliyense adzafa

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e13 күн бұрын

    Mwakwiyatu muziwika ili nd dziko 😮

  • @LeendaDeborah2005
    @LeendaDeborah200513 күн бұрын

    Ubwino wake chilungamo chichokela kukhomo kwako. Tsiku la chilungamo likazakwana malamulo anuwo zasatha kukuombolani. Palibe chomwe muzachite ndipo muzayaluka chaka chake nchino ndi cha mawamawali

  • @JustinLipipa
    @JustinLipipa13 күн бұрын

    Mmmmmm Mcp singasinde, crocodile 🐊 ndi crocodile 🐊

  • @user-jd9yz5hp7y
    @user-jd9yz5hp7y13 күн бұрын

    AGAPE musathe mau Antanyiwatu ali ndi ma Audio anu bwinotu mukutha mawu muyalukatu zakuwawanitu mphakana kumuwopyezanso ndi za imfa? Anthu a MCP inu oyipa kwambiri nchito yanu kukhetsa mwazi basi

  • @Luxemaven8686
    @Luxemaven868613 күн бұрын

    Warning of a guilty person. Ma threat zomwezi?

  • @CtvnMpina
    @CtvnMpina12 күн бұрын

    Kod iweyo ungavomele zoti udapanga?Mesa ukuwopa kumangidwa,kuwawona anthu kupusa?

  • @MphatsoIshmaeladam
    @MphatsoIshmaeladam12 күн бұрын

    Padziko lapatsi palibe bwenz lokonda,umati ukuchita chinthu in secret koma wina momo amazemba mkukuuza for example ena amati ndege yasowa while people were died koma mthanyiwa anabwera mkutiuza ndipo ndimomo

  • @KereeditseMotsetse
    @KereeditseMotsetse11 күн бұрын

    Mtanyiwa usasiye kunena musamuphe akuntchulanibe mukangomupha muona agaluinu palibe 72 hrs machendako

  • @user-ww9rj2wx8d
    @user-ww9rj2wx8d12 күн бұрын

    Iwe gape nawonso akuthila msembe anthu a MCP kuti ganyu unapanga okupha athu kt siku lina usazawulule usamale MCP ikupha ngati mene amuphela chilima

  • @HakeemJossam
    @HakeemJossam12 күн бұрын

    ichi mchakuphadi aaaaah

  • @PhillspicJere
    @PhillspicJere12 күн бұрын

    Mumamusewelesa maneneyi pambuyo pake azizapepesa pa court, ameneyu akalowe kuti Anthu ena atengelepo phunziro

Келесі