No video

A Chakwera Ndi A Mutharika Onse Ndi Olephela - Samuel Lwara

On Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara says neither His Excellency Dr Lazarus McCarthy Chakwera nor former president Prof Peter Mutharika are fit to rule this country. They are both failures.
Pa Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara wati Olemekezeka Dr Lazarus McCarthy Chakwera kapena pulezidenti wakale Prof Peter Mutharika sayenera kulamulira dziko lino. Onsewo ndi olephera.
#Malawi

Пікірлер: 208

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756Ай бұрын

    Samuel you are right ✅ 👌....Chakwera ndi Muntharika...tiwaona zintchito zawo....Onsewa olephwera we.Need New Blood....Mkulu uyu akalankhula chilangamo....zoona zokhazokha......More Fire 🔥 Samuel...👍👍👍👏👏👏👏👏👏

  • @Mahmoodwargison-op2gm
    @Mahmoodwargison-op2gmАй бұрын

    Vuto munthuu akalakhula ngamo mumamuda kma chilungamo chimawawa keep it up nr Rwala

  • @Extratremendouszeus

    @Extratremendouszeus

    Ай бұрын

    Ukhale president iweyo

  • @user-qp8kh2hj9o

    @user-qp8kh2hj9o

    Ай бұрын

    Zoona ndithu zimene a kunena Rwara

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wtАй бұрын

    Ofcz munthalika failed somehow but these one eeeh aonjezaa

  • @OMEXTWAIBU
    @OMEXTWAIBUАй бұрын

    I'm really agree with you Samuel , keep it up and don't fear. True true big.

  • @Littlefair7
    @Littlefair7Ай бұрын

    Chilungamo chosatenga mbalin keep up the good job, zitseguleni mitu mbuli zimene zimavotera atsogoleri olephera, 80% ya anthu ovota ndi mabulutu, akufuna Chakwera olephera kubweretsa Mutharika olepheranso.

  • @MasterMwandira-q8v
    @MasterMwandira-q8vАй бұрын

    Ndizoonadi. APM, CHAKWELA, awa ndi anthu olephela, bwanji tiyeseko afford nawoso tione kulephela kwao

  • @anniedennis7127
    @anniedennis7127Ай бұрын

    That's very true , only a patriotic Malawian cannot vote for failed leaders Chakwela and muthalika.

  • @FrancoKaunga-rq2ki
    @FrancoKaunga-rq2kiАй бұрын

    Mr lwara you are number one! Apm and chakwera same what's up group both are fools. Malawi is a cursed country leader ship is worse.

  • @DIRECTORJARVMACK
    @DIRECTORJARVMACKАй бұрын

    Ndizoona onse ndi olephela koma devaluation mmmmmmmm ndiyopweteka kwa achinyamata ogwila maganyu ife APM my vote

  • @BrightPhiri-bt6ev
    @BrightPhiri-bt6evАй бұрын

    Apa mwalankhulapo za nzelu lero.peter is not a solution to our problems tinamuyesa kale

  • @GiftPhiri-tt7nn
    @GiftPhiri-tt7nnАй бұрын

    Chipani cha dpp bingu anapanga chitukuko kwambiri and ndimachikonda koma president amayenera kukhala wina ku dpp ko , sankhani president wachinyamata ife tikamuvotela , dpp bola singafanane ndichakwera koma ma president tiyese atsopano

  • @VeronicaChirwa-ct4os

    @VeronicaChirwa-ct4os

    Ай бұрын

    Mwayankhula bwino kwambiri, anthu amadana ndi chilungamo

  • @haneefmuyaya7472

    @haneefmuyaya7472

    Ай бұрын

    I prefer, Muthalika ataimanso ndi Atupele, Zikhiza kukhala bwino, akazatopa, mwana azapitirize, Koma zomatenga anthu isaziwika bwinozi, 5yrs it's not a joke guys

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gyАй бұрын

    Pa Peter pokhapo ndie wapenga Peter sungamufanizilire ndi chakwera APM akufunika than any one

  • @user-st6bt5vv9c
    @user-st6bt5vv9cАй бұрын

    Lawala is looking for chihana but AFORD alone can't win how old was mandera both are candidates let them exercise their freedom

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5iАй бұрын

    Unaonako dpp ikugula fertilizer ku butchery,kwatsala iweyo akumange mpamene utadziweno kuti pakati pa awiriwa Pali kusiyana.

  • @user-ee6be5kl5o
    @user-ee6be5kl5oАй бұрын

    Lwala Mutu wako sakugwila waoneka kale omwe amasankha ndi anthu iweyo sungafanizile Mutharika ndi chakwera , Mutharika anthu amasangalala kwambili kuposa pano ndi chifukwa anakuthamangitsa mnyumba ya Malawi housing, iweyo ziyankukula zako zopusazo amalawi Peter Mutharika wooyee

  • @YNOTGEORGE8
    @YNOTGEORGE8Ай бұрын

    Yes Mr Lwarwa thus fact APM thus not a solution

  • @MenciaMadex
    @MenciaMadexАй бұрын

    Apm my vote 2025

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5iАй бұрын

    Mr. Lwara is a chaotic person, he wants people to applaud whatever he says, Mr. Lwara learn to be quiet sometimes, you are missing the point

  • @MacphersonJuma

    @MacphersonJuma

    Ай бұрын

    opepela uyu mbuzi ya munthu

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7eАй бұрын

    Apm amalize term yake munamulandila nsanje upresident l support Dpp 100%

  • @MosesTangwe
    @MosesTangweАй бұрын

    Naweso larwa izi ife ai. chifukwa a Peter mutharika sungafanizire chakwera never. Pali zambiri zomwe simungafananitse

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5iАй бұрын

    Pena pake nanuso Mr Lwara mumaganiza moperewera kwambiri,inuyo mungafanizire Peter ndi chakwera? Like seriously?

  • @TheresaKuluwemba

    @TheresaKuluwemba

    Ай бұрын

    Kkkk mwina akufuna aime iyeyo kukhala president kkk

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3iАй бұрын

    Inu ndiye mu kuwona owina ndi ndani, plz musapange zoti wina mungomuioitsa mbiri koma mudzilankhula kuti zinthu zisinthe. Pano tikufuna kuti tisinthe dziko ndiye osinthayo ndi APM zisiyeni zikhale chonho

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENANАй бұрын

    Ndiyambe chochi,Neleson mandela uja sanalamulire dziko ali otha msinkhu?? chikhala kuti peter anthu akumuda bwezi kumaliro kuja anthu akumulira kut ayimile?? so iwe ukamat peter ayi what do you mean so tayimilatu iweo tione ndi mkamwa modambanamo aaarrriii. iwe do you compare chakwela nd peter,chambaaa chani,ngat sukufuna khala usavote uzidya soya peices bass kumpotoko ndi atumbuka azakowo bwanji? pita ukooooo

  • @Littlefair7

    @Littlefair7

    Ай бұрын

    Akunena zoona, koma mbuli ngati inuyo simungaone.

  • @user-es4jt6ds8m

    @user-es4jt6ds8m

    Ай бұрын

    Ayi osanena Kuti stumbuka pliz zichepezo tseka Chikamwa icho

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3hАй бұрын

    Ndinu achitsilu alwara sungafanizile MCP ndi DPP aaaaa anyamata alipo muboma akupanga chani

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3wАй бұрын

    Bola APM kusiyana ndi chakwera, nthawi ya APM zinthu zinaliko bwino kusiyana ndi chakwera.

  • @user-iu6mr5xu6r
    @user-iu6mr5xu6rАй бұрын

    Kodi bambo Lwara, amene afuna nzake pakati pa Peter ndi Saulosi ndani? Khalani ndi cipani canuco. Kuposa kunena zopusa ngati cidakwa. Kodi wanzeru? Nanga ulikuti ndipo ukutani?

  • @user-ti2ct8ts8d
    @user-ti2ct8ts8dАй бұрын

    Iwe mutharika ungafanize mbudzi ngati chakwela? Iwenso ndi kape kwambiri

  • @spargomw
    @spargomwАй бұрын

    Akulu ngat Mfundo zakutheran ndibwino kukhala osayankhula kalikonse, inuyo pangan Alliance nd Lyton Mangochi muyambitse chipani chanu coz apapa mwaonetsaso uchitsiru ofanana nd Lyton Mangochi.

  • @Emmanuelmw603
    @Emmanuelmw603Ай бұрын

    mutharika akuwinaso mufune musafune.....APM my vote ✊

  • @JumaKachala
    @JumaKachalaАй бұрын

    Koma.lero ndee mwayankhula zopepelatu Peter angafanane ndi chakwera

  • @isaaczuze
    @isaaczuzeАй бұрын

    Kodi a lwara muli mbali iti President wanu pano ndi mdani ....jnutu mwasowa kolowera .. .mmene chakwera waonongela zikoli mungayerekeze ndi apm....inuyo mukukhala ngati mbuli bwanji Mmene peter amasiya upresident katundu anali pati.....iweyo lwara wangosowa kolowera .....osachita support Enock chihana bwanji monga wakwanu.....usiletu kuyankhula za peter......amalawi chiyembekezo chimene tasala nawo ndi peter

  • @user-iu6mr5xu6r
    @user-iu6mr5xu6rАй бұрын

    Inu ndi munthu amene amanena zinthu zimene sadzidziwa. Munapha zipani 9 kukhala ndi kusunga MCP. Lero mulalata?

  • @VuyolwethuMbabani
    @VuyolwethuMbabaniАй бұрын

    Iwe uzilimbana ndi chakwela otsati Peter ngati wapasidwa ndalama ukazibwedze uyaluka komanso uchita manyanzi 2025

  • @TypexTikita
    @TypexTikitaАй бұрын

    Lwara zopela zomwe walankhula za APM chifukwa munthu wanzeru sangayerekeze mavuto tilinawowa ndi APM

  • @QueneteCatundulo
    @QueneteCatunduloАй бұрын

    Asowa choyankhula awa

  • @samsonhavenoyayshonga2609
    @samsonhavenoyayshonga2609Ай бұрын

    Koma pa ma President onse mu Malawi yemwe aliko bwino kuposa onse ndi Mutalika.

  • @RitaDickson-ls7ol

    @RitaDickson-ls7ol

    Ай бұрын

    Palibe zabola apa change position peter and chakwela out 2025

  • @OweniMalokooweni-es9qx
    @OweniMalokooweni-es9qxАй бұрын

    Ndipo kwambii timufuna atupele mulunzi😊

  • @MaryChavula-jz3di
    @MaryChavula-jz3diАй бұрын

    Lwara ndi wa ganyu sasamala za amalawi akungifuna kuti amupatse ndalama koma APM sangamupatse ndalama n'gooooo ozavotela APM ndife amalawi akumudzi amene tikudziwa ubwino wa APM tikufuna feteleza ontchipa ife

  • @user-nd9cm3yl7e
    @user-nd9cm3yl7eАй бұрын

    Muthalika satukwana muthu olomodzi ndiwante ndele zd

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWiliАй бұрын

    Lwala wayamba kukhumudwitsa wanthu chakwera ungafanizire ndi Apm?

  • @AlfredSteven-v9m
    @AlfredSteven-v9mАй бұрын

    Yes ur right koma mukananena oyenera muzipanimo

  • @PeterPhiri-di1ux
    @PeterPhiri-di1uxАй бұрын

    ndimakupanga follow koma lero wangomunyoza muthalika panya pako ndipo ndakutuluka

  • @lucianogeoffrey4275

    @lucianogeoffrey4275

    Ай бұрын

    Atumidwa awa, akuona ngat titha kusankha iwowa

  • @marcuswalker2613
    @marcuswalker2613Ай бұрын

    Mbuli iwe Mtumbuka opanda mfundo atakulanda nyumba ndiye wowowoooo. Ndale zako zilibe tsogolo "mark my word"

  • @BertharrySecurity
    @BertharrySecurityАй бұрын

    Mnthalika inde analephela Koma anayesesa, kusiyana ndiwomwe alipowa

  • @MaryChavula-jz3di
    @MaryChavula-jz3diАй бұрын

    Mulilanaye APM chomwe timadziwa APM sanaluzepo ndewu akamamenyana 1 to 1 kukanikana ndiye mubweletse 1 to 5 ndiye 5 a wine muziti m'modziyo walephela? Anthu adyela Inu tandiyankheni alwara komanso kamenyedye ka m'modzi uyo sikanasithe 40 pelesenti ndiyomweyo anapezanso pa 1 to 1 mulila ndi APM 2025 APM boma

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6sАй бұрын

    Alwala mwayamwa tikutulukani mwayambaz,inu nthawi ya DPP mungayerekezere ndinthawi inu. Inu nthawi ya DPP anthu amamangidwa chonchi or kukwera kwazinthu zinafika apa? Njara,kusowa kwamankhwala mzipatala,kukwera kwa zinthu mungayelekeze ndinthawi ya DPP

  • @StevenDastan
    @StevenDastanАй бұрын

    Apm ndimunthu wankulu kwambili kuliphika dziko lino

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWiliАй бұрын

    Apm my vote

  • @user-ln3zx6wo4w
    @user-ln3zx6wo4wАй бұрын

    As itikut peter alibwino koma tikut apm alikobwino kusiyana ndi chakwera basi

  • @EllahChikwatu
    @EllahChikwatuАй бұрын

    Iweyo suzakalamba omwe anakubala nd sikana wina nyamata sibwino kwanu kulibe agogo

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7tАй бұрын

    2020 mumanenaso Chocho kut alowe anyamata lelo bwanji

  • @user-zx3pz2wy1j
    @user-zx3pz2wy1jАй бұрын

    Kodi osalephela ndi ndani ngati ukutiso peter ndiwolephela iweyo wachitapo chiyani ?

  • @RitaDickson-ls7ol
    @RitaDickson-ls7olАй бұрын

    That is true Peter ngati anachoka pampando analephela tiwoneko zna asatinamize agogo l love your point keep it up mr🙏🙏🙏

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873Ай бұрын

    Peter mutalika ndi simungayerekeze ndi Chakwera. Vuto amalawi timaziwa kuyankhula koma mopanda zeru. Mcp udf ppp dpp mukhale pasi muone kuti kodi ndichipani chiti chimwe chapangapo zabwino muona kuti dpp inayesesa. Chinthu chimozi poti mutalika wakalamba koma still ali ndi zeru . Chilima sanawinise dpp. Dpp nditimene anayitana chilima. Chilima anawinisa mcp ndiyime isamanyade .

  • @MarriamBakalie
    @MarriamBakalieАй бұрын

    Wayambatu ku khota tidana nawetu uziyankhula za chakwela nt APM wamva machende ako galu

  • @DeliaKaduya

    @DeliaKaduya

    Ай бұрын

    😂😂😂😂 yomweyo galu iweee

  • @FionaKhoma
    @FionaKhomaАй бұрын

    Ulibe mfundo nzimayi pachinyero chako dppp ikulowabe m,boma panyero pako

  • @user-or7ng3fj8f
    @user-or7ng3fj8fАй бұрын

    Ndiwe kapolo wamundu Peter again in 2025 🔥

  • @Samu-q3z
    @Samu-q3zАй бұрын

    Apm ❤❤❤❤

  • @jonas-xh4hz
    @jonas-xh4hzАй бұрын

    a rwara zikambani zanzeru musiye kuyankhula zopusa zanuzo

  • @retirementtoafrica
    @retirementtoafricaАй бұрын

    Nkhani yodya mabanzi ndiyovuta, chilungamo chimasowa ndikumagoyankhula mozungulira opanda solution.

  • @HendresonLubano
    @HendresonLubanoАй бұрын

    Kuyambila pano usazanyozeso muthalika ndimunthu watendele

  • @ibrahimbamusi109
    @ibrahimbamusi109Ай бұрын

    Lwara tikutulukatu ali ndi chibwana

  • @DesmondKanguwe
    @DesmondKanguweАй бұрын

    Reality yowawa...odana ndzomwe ukunenazi sadziwa zomwe akufuna

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3prАй бұрын

    Ndipo a samuel lwara mumandiwaza nsaname kkk everytime ndikamamvera ma audio anu ndimamva sugar 😂 ndimafuna ndikumvelani daily cz mumabudula mpunga wanyama, kamba simugawa. Izizi akunena apazi akutsutsa amadya thewera lamwana 😅😅😅

  • @user-qp8kh2hj9o

    @user-qp8kh2hj9o

    Ай бұрын

    Zoona ine munthu uyu ndimafuna kumamumvera daily fact ndiyomwe akunenayi😂😂😂😂

  • @FionaKhoma
    @FionaKhomaАй бұрын

    Galu nzimayiiwe athu anzeru avotera dppp pitamuthalika amayesetsa kuti athu tizidya chakwera anabwera kudzaba njara yavuta km muthalika zakudya zimatsika ntengo

  • @VincentNgabuhvincent
    @VincentNgabuhvincentАй бұрын

    Ada awawo Samuel Lwara mumuuze ma chende ake palibe chomwe wakamba chamzeru wamva ukalimbana ndi DPP poliyako wamva iwe ndy ndindani. kd nanunso Amalawi munthu kungoti wangobwera ndi ka audio kake bs mungoti that's true km akukamba zopanda munthu Amalawi mulibe mzeru kwa amene mungoyamikira zopanda pake zausichilu bs. MCP ukafanizire ndi DPP mutu wako ukugwira iweyo kd nthawi imene APM anali pa mpando kd ena inu timakuziwani kd chifkwa nthawi zina APM munangokhala chete chifkwa zinthu zikayenda bwino ngakhale zimavuta km sangafike pa mbudzi iyi chakwera . Samuel lwara machende ako mpaka uzafe ndiza DPP kuipa kwake ok.

  • @kondwanbanda2671
    @kondwanbanda2671Ай бұрын

    Alekeni anthu akasakhe okha

  • @user-hd7wq2yc6m
    @user-hd7wq2yc6mАй бұрын

    A Lwara ndinu odwala mumutu nzeru mulibe ukuganiza kuti anthu angasithe maganizo awo pazimene ukuyankhulazo Inu a Lwara mukufina kisokoneza anthu Malawi muno iwe nzeru ulibe ndiposo anthu asakumvere iyayi foseki mahala ulije ulichindere chomene palije zakusintha Peter wayomenge ndiposo wazamuwina u activist wa iwe Lwara ngwauzereza mwawanthu ngati iwe Lwara ndimweikunanga Charu Chaalawi foseki ulichindere so iwe unamahala Lwara? Vyakuyowoyeka vyako vikuchita kuwonekerathu kuti ndiwe miulwali mumutu zimene ukuyankhula ndizonyoza sopano ndalere zonyozana monga mumene ukunyozera iweyo, anthu sangakimvere aMalawi simuwaziwa iweyo anasukusula ,ulichindere chomene ndicho chifukwa ukunyoza mafumu ghakuno kwithu ku Mzimba ngati nawe uli mongonl .ikuchimanya chiyowoyero na chikhalidwe chachingoni iwe foseki zako uwaleke wazakayime wene Peter Mtharika uzamuvota ndiwe chlmunthu chasanje ichi wati iwe ungalingananayo zeru Peter? Ulichindere

  • @MaxwellSakwata-wb8ep
    @MaxwellSakwata-wb8epАй бұрын

    We never voted out APM may be you did.....

  • @thondoyaenterprise3795

    @thondoyaenterprise3795

    Ай бұрын

    Dpp cheated

  • @michaelkallyz2425

    @michaelkallyz2425

    Ай бұрын

    No, DPP was cheated by judges

  • @user-nd9cm3yl7e
    @user-nd9cm3yl7eАй бұрын

    Wanamaiwe sudziwa ndale

  • @SofiyanoMayuni
    @SofiyanoMayuniАй бұрын

    Peter ndiwabwino

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348Ай бұрын

    Nyamata wa chilima wasowa kolowera kkkkk

  • @MastonWatson-g7g
    @MastonWatson-g7gАй бұрын

    Iwenso mmutu mwako nzeru mulibe nzeru chakwera ungamufanizile ndi mutharika? kape iwe wosowa chonena.

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6dАй бұрын

    Abambo inuyo timakukondani panopa tisiya kuvela ma odio anu inu satana ameneu chakwela mungamufanize ndi peter muthalika muthu salephela kukhala ndi zofooka koma peter muthalika anali muthu oyesesa ndipo akatengaso boma adzalamulila bwino kwambili chifukwa wadziwa zomwe amalawawi amafuna Moyo wautali adad ❤❤

  • @Mahamudu-q6b
    @Mahamudu-q6bАй бұрын

    ❤❤ zowona

  • @paulmanyamba5437
    @paulmanyamba5437Ай бұрын

    Ndichifukwa achichotsa ntchito ndiwamisala wakutumayo akupusitsa koopsa 😂😂😂

  • @lucianogeoffrey4275
    @lucianogeoffrey4275Ай бұрын

    Mwayambatu uchitsiru madala. Muthalika ndi Chakwera you cant put then together. Ya Chilima ija timakupangani support koma mwayamazi ayi

  • @VuyolwethuMbabani
    @VuyolwethuMbabaniАй бұрын

    Udani wako ndi a Peter usasokonedze nao anthu omukonda Peter Ife Peter ndi chiyembekezo chathu usiye kuyankhula manyi

  • @OsmanPatrick
    @OsmanPatrickАй бұрын

    Machende ako iwe abambo akowo

  • @KennyPhiri-zg1kr
    @KennyPhiri-zg1krАй бұрын

    Peter anayendesapo analephera chakwera walephera you are true pezani wina

  • @user-qg4it7my9n
    @user-qg4it7my9nАй бұрын

    Akulu fodya tamazimisiraniko a peter simungafanizire ndi mbuzi ya mu2 ngat chakwera

  • @user-jj3oo6jh1l
    @user-jj3oo6jh1lАй бұрын

    Mr samuel.pachimanga choola timasankhako.kt ichi ngankhale chili choola km.ndinkhonza kukazinga nde anthu tikuona kt bola peter

  • @blessingmanda
    @blessingmandaАй бұрын

    change the system, anyone who has been who is who will be the president of malawi nothing has change and will change eccept if the system is changed. scrap the constition book

  • @EmmanuelMaxon
    @EmmanuelMaxonАй бұрын

    Iwe aliyese akavota yekha usati nyase usamat amalawi sakufuna dpp uziti iweyo sukufuna koma ine ndikufuna zako zimenezo mesa chilima anadziwa ndale chifukwa cha apm

  • @michaelkallyz2425

    @michaelkallyz2425

    Ай бұрын

    Auzeni koma awa. Khala ngati ntawi yaPita analikuLwanda

  • @AlfredSteven-v9m
    @AlfredSteven-v9mАй бұрын

    Mwangolongolora 18 min osanenapo oyenera anthu tigwire ziti ndiye

  • @Spaw-BTheGogoBoy
    @Spaw-BTheGogoBoyАй бұрын

    Lwala nde tivotere ndanino kulephera kulitu ma stage stage enawo nde ndi zero

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4scАй бұрын

    100% light show ndi olephela.tiyetsele,utm UDF or afford.amagona,ali pa mpando.ziko,amayemdetsa,ndi chisale.ndi,amayi akunyumba kwao.just, remember akazi awo,amachita kupita ku reserve bank kumangotenga, ndalama kumeneko,atiudza za change for what corrupt our nation? that's sheet 'we can no sitting here watching this happen.amalawi,kodi,timadziwa akamati democracy?tili kutali,ndi chitukuko mu ziko lathu.

  • @charlesmasauko4651
    @charlesmasauko4651Ай бұрын

    Woooozaaaaaaa sir Lwara

  • @EllahChikwatu
    @EllahChikwatuАй бұрын

    Iweyo olo ungafanane nd APM ,,,,, ku pepera bas cisiru lwara

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2ofАй бұрын

    Apeter ndiye ndiokanika bola namkhumwa osati peter aaaa ngati zili chotcho basi alipowa angopitiliza

  • @user-lw4hw9ce4w
    @user-lw4hw9ce4wАй бұрын

    Chi luwara ndichimbuzi APM will win you can't compare with chakwera suka ng'undu

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zbАй бұрын

    Auzeni zoona bwana

  • @frezarphiri3480
    @frezarphiri3480Ай бұрын

    Iwe luwala iwe APM siwungamufanizile ndi chakwela ayi iwe watanikodi

  • @marryphili5419
    @marryphili5419Ай бұрын

    Ndiwe galu Kwa basi mbuzi DPP fertilize wunaliko mapassport analiko makhwara amapezeka muzipatara ndiye zingananane Ndi MCP kagwere wuko

  • @samsonhavenoyayshonga2609
    @samsonhavenoyayshonga2609Ай бұрын

    P M munthu odziwa kulamulila munthu wanzeru akuziwa ,Larwa udakiwe

  • @JuniorHala-vf9ov
    @JuniorHala-vf9ovАй бұрын

    Akulu mwayowoya makola chomene ineso palije uyo angasanga vote yane anthuwa palibedi munthu ofunikila Peter anapangitsa kut kuyambe ma dembo tisaiwale ulamuliro wao

  • @OMEXTWAIBU
    @OMEXTWAIBUАй бұрын

    APM wakalamba akapume, akakhala akungozikodzela ndiye angalamule ndani? Kwake kunatha petulo tiwone zina, munthu osadziwa kulankhula kkkkkk akagwele ndi family party yakeyo, Tiyeni amalawi tiyese Atupele ❤

  • @Extratremendouszeus
    @ExtratremendouszeusАй бұрын

    Rwala ndi opusa Chisiru iwe...chitsiru kwabasi

  • @user-fq4kv8dj4t
    @user-fq4kv8dj4tАй бұрын

    Koma peter ungamufanize ndi lazalo ukunama zikatere nde kt basi kulibe wabwino

  • @JamesMalango
    @JamesMalangoАй бұрын

    Akulu awanso,,,,